< 1 Sa:miuele 11 >
1 Oubi afae baligili gomane, A:mone hina bagade Na: iha: sie da ea dadi gagui dunu bisili asili Gilia: de fi ganodini Ya: ibese moilai bai bagade fi ilima gegemusa: asi. Ya: ibese dunu da Na: iha: siema amane sia: i, “Dia ninima gousa: su hamoma. Amasea, dia da nini ouligima: mu.”
Nahasi, Mwamoni anapita ndi kuzungulira mzinda wa Yabesi Giliyadi. Tsono anthu onse a ku Yabesi anapempha Nahasiyo kuti, “Muchite nafe pangano, ndipo tidzakutumikirani.”
2 Na: iha: sie da bu adole i, “Na da dilima gousa: su hamomu be hou afae fawane fa: no bobogemu. Na da dilia dunu huluane ilia lobodafadini si duga: le fasima: ne sia: sea fawane, na da dilima gousa: su hamomu. Amasea Isala: ili fi huluane da gogosiamu!”
Koma Nahasi Mwamoni uja anayankha kuti, “Ndidzachita nanu pangano pokhapokha nditakolowola diso lakumanja la aliyense wa inu kuti ndichititse manyazi Aisraeli onse.”
3 Ya: ibese ouligisu hina ilia da amane sia: i, “Ninima eso fesuale ima! Amo esoga ninia da Isala: ili fi ganodini amo sia: sisa: i lamu. Amasea, ninia da fidisu dunu hame ba: sea, dima dia sia: i defele gousa: su hamomu.”
Akuluakulu a mzinda wa Yabesi anati kwa iye, “Utipatse masiku asanu ndi awiri kuti titumize uthenga mu Israeli monse. Ngati sipapezeka wodzatipulumutsa, ndiye ife tidzadzipereka kwa iwe.”
4 Amo sia: da Gibiaga Solo ea esaloba amoi doaga: i, amola amo sia: ilia sia: noba, dunu ilia da amo sia: nababeba: le hedolo dafawane heawini didigia: i.
Amithenga aja atafika kwawo kwa Sauli ku Gibeya ndi kufotokoza nkhaniyi kwa anthu onse, iwo analira motaya mtima.
5 Amogalu, Solo hi bugi sogeanini ea bulamagau amola daeya hi diasu guda: mana didigia: be nababeba: le, e da adole ba: i, “Abuli hamoi? Abuliga dunu huluane da didigia: sala:” Ilia da sia: Ya: ibeseganini gaguli misi sia: amo adodole i.
Pa nthawiyo nʼkuti Sauli akubwera kuchokera ku munda, ali pambuyo pa ngʼombe zake za ntchito ndipo anafunsa. “Nʼchiyani chawavuta anthuwa kuti azilira motere?” Ndipo anamufotokozera zomwe anthu a mu mzinda wa Yabesi ananena.
6 Solo da amo sia: nababeba: le, Gode Ea A: silibu Hadigidafa da ema aligila sa: ili amola Solo da bagadewane ougi.
Sauli atamva mawu awo, Mzimu wa Mulungu unabwera pa iye mwa mphamvu ndipo anakwiya kwambiri.
7 E da bulamagau gawali aduna fane, fofonobone dadamui. Amalu bulamagau dadamui amo huluane sia: adola ahoasu dunu ilima i. Solo da sia: adodola ahoasu dunu ilima, amo bulamagau dadamui agoane Isala: ili fi soge huluanema olelela lama: ne iasi. Amoga ilia da dawa: digima: ne, e da amo sisasu sia: si, “Nowa dunu da Solo amola Sa: miuele elea gegena ahoabe amoga hame madelasea, ilia ohe fofoi amoga da agoane hamomu.” Sia: adola ahoasu dunu ilia da agoane sisia: Isala: ili soge ganodini lai. Isala: ili dunu ilia da Hina Gode Ea ilima adi hamoma: bela: le beda: i, amola ilia huluanedafa Soloma gilisili mafia: i.
Tsono anatenga ngʼombe ziwiri za ntchito, nazidula nthulinthuli. Ndipo anatumiza amithenga ndi nthulizo dziko lonse la Israeli ndi mawu akuti, “Umo ndi mmene adzachite ndi ngʼombe ya aliyense amene satsata Sauli ndi Samueli.” Ndipo anthu anachita mantha aakulu motero kuti onse ananyamuka ndi mtima umodzi.
8 Solo da dunu huluane Bisege moilaiga gegedolesi, dunu da ba: loba 300,000 agoane da Isala: ili dunu amola 30,000 agoane da Yuda dunu agoane ba: i.
Pamenepo Sauli anawasonkhanitsa ku Bezeki nawawerenga, ndipo Aisraeli analipo 300,000, Ayuda analipo 30,000.
9 Ilia da Ya: ibese dunu sia: adola misi ilima amane sia: i, “Dia dunuma sia: ma. Aya eso dagobe galu ili da gaga: i ba: mu.” Ya: ibese dunu ilia da amo sia: nababeba: le, ilia da baligili bagade nodoi.
Tsono Sauli anawuza amithenga ochokera ku Yabesi aja kuti, “Mukawawuze anthu a ku Yabesi Giliyadi kuti mawa nthawi ya masana adzapulumutsidwa.” Pamene amithengawo anapita ndi kukafotokoza nkhani imeneyi kwa anthu a ku Yabesi, iwo anasangalala kwambiri.
10 Amalu ilia da Na: iha: siema amane sia: i, “Aya da dia nini lama: mu, amalu di adi hanai ninima hamomusa: dawa: sea, hamoma: mu.”
Choncho anthu a ku Yabesi anawuza Nahasi kuti, “Mawa tidzadzipereka kwa inu ndipo inu mudzachite nafe chilichonse chokukomerani.”
11 Amo gasia, Solo da ea dadi gagui dunu udiana mogi. Golale, hahabedafa, ilia da ha lai diasua hehenaia gugudili sa: ili, A:mone dunu huluane doagala: le, eso dogoa, A:mone dunu huluane da medole legei dagoi ba: i. Dunu hame bogogia: i esafulu, ilia da afagogole, dunu hisu hobeale afia: i.
Tsono mmawa mwake Sauli anagawa anthuwo mʼmagulu atatu. Mmamawa kusanache iwo analowa mʼmisasa ya Aamoni ndi kuwapha mpaka masana. Amene anapulumuka anabalalika, aliyense kwakekwake.
12 Isala: ili dunu ilia da Sa: miuelema amane sia: i, “Dunu amo da Solo ea hina hamoma: ne hame dawa: i amo da habila: ? Amo dunu ninia fanelegemusa: , ninima oule misa!”
Kenaka anthu anafunsa Samueli kuti, “Kodi ndani aja ankanena kuti, ‘Kodi Sauli nʼkutilamulira ife?’ Bwera nawoni kuno kuti tidzawaphe.”
13 Be Solo da amane sia: i, “Ninia da dunu afae da wali hamedafa fane legemu. Bai wali eso, Hina Gode da Isala: ili dunu gaga: i dagoi.”
Koma Sauli anati, “Palibe amene ati aphedwe lero, pakuti lero lino Yehova wagwira ntchito yopulumutsa Israeli.”
14 Amalu, Sa: miuele da ilima amane sia: i, “Ninia da bu Giliga: lega gilisili, bu Solo da ninia hina bagade asulimu.”
Ndipo Samueli anati kwa anthuwo, “Tiyeni tipite ku Giligala kuti tikatsimikizenso kuti Sauli ndi mfumu yathu.”
15 Amaiba: le, ilia da huluane Giliga: le moilaiga asili, hadigi sogea amoi Solo da ilia hina bagade asuli. Ilia da Hahawane Gilisili Olofole Iasu gobele salasu hamonanu, Solo amola Isala: ili dunu huluane ilia da hahawane gilisisu hamoi.
Choncho anthu onse anapita ku Giligala ndipo kumeneko Samueli anakalonga Sauli ufumu pamaso pa Yehova. Pambuyo pake anthu anapereka nsembe zachiyanjano pamaso pa Yehova, ndipo Sauli ndi Aisraeli onse anachita chikondwerero chachikulu.