< 1 Hina 9 >

1 Hina bagade Soloumane da Debolo diasu amola hina bagade diasu amola ea gagumusa: dawa: i liligi huluane, amo gagui dagoloba,
Solomoni atatsiriza kumanga Nyumba ya Yehova ndi nyumba yaufumu, ndi kukwaniritsa kuchita zonse zimene ankafuna,
2 Hina Gode da musa: Gibionega ema misi, amo defele ema bu misi.
Yehova anamuonekera kachiwiri, monga momwe anamuonekera ku Gibiyoni.
3 Hina Gode da ema amane sia: i, “Na da dia sia: ne gadosu nabi dagoi. Na da amo Debolo (amo di da dunu ilia amo ganodini Nama sia: ne gadomusa: gagui) amo Debolo da hadigiwane dialoma: ne Na ilegesa. Na da eso huluane, mae fisili, amo Debolo ouligimu amola gaga: mu.
Yehova ananena kwa iye kuti: “Ndamva pemphero ndi pembedzero lako pa zimene wapempha pamaso panga. Ndayipatula Nyumba iyi, imene wamanga, poyikamo Dzina langa mpaka muyaya. Maso anga ndi mtima wanga zidzakhala pamenepo nthawi zonse.
4 Di da moloidafawane, dia ada Da: ibidi defele, Na hawa: hamosu noga: le hamosea, amola Na sema amola Na hamoma: ne sia: i amo nabawane hamosea,
“Kunena za iwe, ukayenda pamaso panga mokhulupirika, mwangwiro ndi moona mtima monga momwe anachitira abambo ako Davide, ndi kuchita zonse zimene ndakulamula ndi kusamalitsa malangizo ndi malamulo anga,
5 Na da dia ada Da: ibidima sia: i ilegei (amo da ea fi da mae fisili, Isala: ili fi ouligibi ba: mu) amo huluane hamomu.
Ine ndidzakhazikitsa mpando wako waufumu pa Israeli mpaka muyaya, monga ndinalonjezera abambo ako Davide pamene ndinati, ‘Sipadzasowa munthu pa mpando waufumu wa Israeli.’
6 Be di, o digaga fi da Nama fa: no bobogelalu yolesisia, amola Na sema amola Na hamoma: ne sia: i dilima i, nabawane hame hamone, eno ogogosu ‘gode’ liligi ilima fa: no bobogesea,
“Koma ngati iwe kapena ana ako mudzapatuka ndi kuleka kusunga malamulo ndi mawu anga amene ndakupatsani ndi kupita kukatumikira milungu ina ndi kuyipembedza,
7 Na da Na fi dunu Isala: ili, amo soge Na da ilima i, amoga fadegamu. Amolawane, Na da amo Debolo (amo Na da wali dili Nama nodone sia: ne gadomusa: eso huluane hahawane dialoma: ne ilegei) Na da amo Debolo fisidigimu. Amasea, fifi asi gala dunu huluane da Isala: ili dunuma gadele amola igabonesisimu.
pamenepo Ine ndidzazula Aisraeli mʼdziko limene ndinawapatsa ndiponso ndidzayikana Nyumba ino imene ndayipatula chifukwa cha Dzina langa. Pamenepo Aisraeli adzasanduka mwambi ndi chinthu chonyozedwa pakati pa anthu onse.
8 Amo Debolo Diasu da mugululi, mebui dagoi ba: mu. Amola dunu huluane amodili baligili ahoasea, ilia da gilulasili, fofogadigimu. Ilia da amane adole ba: mu, ‘Abuliba: le, Hina Gode da amo soge amola Debolo Diasu amoma agoane hamobela: ?’
Ndipo ngakhale kuti tsopano Nyumba ya Mulunguyi ndi yokongola kwambiri, onse amene adzadutsa pano adzadabwa kwambiri ndipo adzatsonya ndipo adzati, ‘Nʼchifukwa chiyani Yehova wachita chinthu chotere mʼdziko muno ndi pa Nyumba ya Mulunguyi?’
9 Amasea, eno dunu ilia da amane adole imunu, ‘Isala: ili dunu ilia Hina Gode da musa: ilia aowalali Idibidi sogega esalu amo fisili masa: ne, ilia hahawane ga masa: ne oule asi. Be ilia da amo mae dawa: le, ilia Hina Gode Ea hou yolesi dagoi. Ilia da ogogosu ‘gode’ma fa: no bobogei amola ilima nodone sia: ne gadosu. Hina Gode Ea ilima gugunufinisisu iabe ea bai da goea.’”
Anthu adzayankha kuti, ‘Nʼchifukwa chakuti asiya Yehova Mulungu wawo amene anatulutsa makolo awo mʼdziko la Igupto, ndipo akangamira milungu ina ndi kumayipembedza ndi kuyitumikira. Choncho Iye wabweretsa zovuta zonsezi.’”
10 Soloumane da ode 20 amoga Debolo Diasu amola hina bagade diasu gagulalu, gagui dagoi ba: i.
Patatha zaka makumi awiri, ndiye nthawi imene Solomoni anamanga nyumba ziwirizi: Nyumba ya Yehova ndi nyumba yaufumu,
11 Daia soge hina bagade Haila: me da Soloumane ea hanai defele, dolo ifa amola ‘baine’ ifa amola gouli bagade ema iasi. Debolo Diasu da gagui dagobeba: le, hina bagade Soloumane da moilai 20 agoane Ga: lili soge ganodini, amo Haila: mema i.
Mfumu Solomoni anapereka mizinda makumi awiri ya ku Galileya kwa Hiramu mfumu ya ku Turo chifukwa Hiramu nʼkuti atapereka mitengo yonse ya mkungudza ndi ya payini ndiponso golide yense zimene Solomoni ankazifuna.
12 Haila: me da amo moilai abedela asi. Be e da amo moilai huluane higa: i ba: i.
Koma Hiramu atabwera kuchokera ku Turo kudzaona mizinda imene Solomoni anamupatsa, sanasangalatsidwe nayo mizindayo.
13 Amaiba: le, e da Soloumanema bobolele amane sia: i, “Naeya! Di da amo moilai nama i dagobela: ?” Amaiba: le, amo sogega ilia da Ga: ibale dio asuli. Ea dawa: loma: ne da “hamedei soge.”
Iye anafunsa kuti, “Mʼbale wanga, kodi iyi nʼkukhala mizinda yondipatsa?” Ndipo iye anayitcha mizindayo Dziko la Kabuli, dzina lomwe amatchedwa mpaka lero lino.
14 Haila: me da Soloumanema gouli defei ‘dane’ biyaduyale gadenene iasi dagoi.
Koma Hiramu anali atatumiza kwa mfumu golide oposa makilogalamu 4,000.
15 Hina bagade Soloumane da Debolo diasu amola hina bagade diasu gaguma: ne, amola osobo amo moilai gusudili gala gasa: le lelegema: ne, amola moilai gagoi gaguma: ne, udigili hawa: hamosu dunu sesesu. Amola Ha: iso, Megidou amola Gise moilale bai bagade gagai amo ilia gaguma: ne, e da udigili hawa: hamosu sesei.
Izi ndi zimene anachita Mfumu Solomoni: Analamula anthu kuti agwire ntchito yathangata pomanga Nyumba ya Yehova, nyumba yake, malo achitetezo a Milo, mpanda wa Yerusalemu, Hazori, Megido ndi Gezeri.
16 (Musa: Idibidi hina bagade da Gise moilai bai bagade doagala: le fefedei. E da amogai fi huluane medole lelegele, diasu huluane laluga ulagisi. Amalalu, ea uda mano da Soloumanema filiba, e da amo moilai, ea uda manoma i.
(Farao mfumu ya ku Igupto inali itathira nkhondo ndi kulanda Gezeri. Iye anatentha mzindawo. Anapha Akanaani amene ankakhala mʼmenemo ndipo kenaka anawupereka ngati mphatso yaukwati kwa mwana wake wamkazi amene anakwatiwa ndi Solomoni.
17 Amola Soloumane da amo moilai bu buga: le gagui). Amola Soloumane da sia: beba: le, ea udigili hawa: hamosu dunu da Gudu Bede Houlone,
Ndipo Solomoni anamanganso Gezeri.) Iye anamanga Beti-Horoni Wakumunsi,
18 Ba: ila: de amola Da: ima moilale bai bagade gagai hafoga: i soge ganodini, amo bu buga: le gagui.
Baalati ndi Tadimori ku chipululu, mʼdziko lake lomwelo,
19 Amola ilia da moilai bai bagade (amo ganodini Soloumane da ea liligi ligisisu) amo gagui. Amola moilai bai bagade amo ganodini e da ea ‘sa: liode’ amola hosi ouligi, amola liligi huluane e da Yelusaleme moilai bai bagade amola Lebanone soge amola ea ouligibi soge huluane ganodini e gagumusa: dawa: i, amo huluane ilia da gagui.
pamodzinso ndi mizinda yake yosungira chuma ndiponso mizinda yosungiramo magaleta ndi akavalo ake. Anamanganso chilichonse chimene anafuna kumanga ku Yerusalemu, ku Lebanoni ndi ku madera onse amene iye ankalamulira.
Panali anthu amene anatsala pakati pa mitundu ya Aamori, Ahiti, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi (anthu awa sanali Aisraeli).
21 Isala: ili dunu ilia da Ga: ina: ne dunu ilia soge gesowaloba, ilia da Ga: ina: ne dunu oda mogili hame medole legei galu. Amo dunu iligaga fi dunu amo Soloumane ea udigili hawa: hamoma: ne sesesu. Amo dunu fi da A: moulaide, Hidaide, Belisaide, Haifaide amola Yebiusaide. Amo iligaga fi da udigili hamonanu, amoganini wali amola, udigili hawa: hamonana.
Zimenezi ndiye zinali zidzukulu zawo zotsalira mʼdzikoli, anthu amene Aisraeli sanathe kuwawononga kotheratu. Solomoni anawatenga ndi kukhala akapolo ake ogwira ntchito yathangata, monga zilili mpaka lero lino.
22 Be Soloumane da Isala: ili dunudafa amo udigili hawa: hamoma: ne hame sesesu. E da ili huluane ea dadi gagui dunu amola eagene ouligisu dunu amola dadi gagui wa: i ouligisu dunu amola ‘sa: liode’ amola hosi fila heda: su dunu hamosu.
Koma Solomoni sanagwiritse ntchito ya ukapolo Mwisraeli aliyense; iwo anali anthu ake ankhondo, nduna zake, atsogoleri a ankhondo, akapitawo ake, olamulira magaleta ndi oyendetsa magaleta ake.
23 Udigili hawa: hamosu dunu da Soloumane ea moilai amola diasu gagubi hawa: hamosu hamoi. Amola ouligisu dunu 550 agoane da ili sesele ouligisu.
Amenewa ndiwo anali akuluakulu oyangʼanira ntchito za Solomoni. Anthu okwana 550 ndiwo ankayangʼanira anthu amene ankagwira ntchitowo.
24 Soloumane ea idua (Idibidi hina bagade ea idiwi) da Da: ibidi Moilai Bai Bagade yolesili, hina bagade diasu amo Soloumane da igili gagui, amoga ahoabeba: le, Soloumane da Yelusaleme moilai bai bagade gusu la: ididili soge amoga osobo gasa: le sali.
Mwana wamkazi wa Farao atachoka mu Mzinda wa Davide, kupita ku nyumba ya mfumu imene Solomoni anamumangira, Solomoni anamanga malo achitetezo a Milo.
25 Ode afae amoga udianane, Soloumane da Wadela: i Hou Dabe Ima: ne Iasu amola Hahawane Gilisili Olofele Iasu, amo oloda e da Hina Godema gagui, amo da: iya gobele sali. Amola e da Hina Gode hahawane nabima: ne, gabusiga: manoma gobele sali. E da agoanewane Debolo gagui dagoi.
Katatu pa chaka Solomoni ankapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano pa guwa lansembe limene anamangira Yehova ndiponso ankafukiza lubani pamaso pa Yehova. Potero ankakwaniritsa zoyenera kuchitika mu Nyumba ya Yehova.
26 Amola hina bagade Soloumane da dusagai gilisi amo Isionegiba moilaiga gagui. Isionegiba da Ila: de moilai bai bagade gadenene amola Ila: de da Idome soge ganodini Agaba Gogomai bega: dialebe ba: i.
Mfumu Solomoni anapanganso sitima zapamadzi ku Ezioni Geberi, malo amene ali pafupi ndi Eloti ku Edomu, mʼmbali mwa Nyanja Yofiira.
27 Hina bagade Haila: me da bagade dawa: su dusagai hawa: hamosu dunu, amo Soloumane ea hawa: hamosu dunu fidimusa: , asunasi.
Ndipo Hiramu anatumiza anthu ake oyendetsa sitima zapamadzi amene ankadziwa za pa nyanja kuti aziyendetsa pamodzi ndi anthu a Solomoni.
28 Ilia amo dusagane gagai amo ganodini foga mini asili, Oufe sogega doaga: i. Amoga ilia da Soloumanema gouli defei 12 ‘dane’ agoane gaguli misi.
Iwo anapita ku Ofiri ndipo anakatenga golide okwana makilogalamu 14,000, amene anamupereka kwa Mfumu Solomoni.

< 1 Hina 9 >