< 1 Hou Olelesu 27 >

1 Isala: ili fi ilia fifi asi bisilua dunu, amola ilia eagene ouligisu dunu amo da Isala: ili soge ouligisu, ilia dio da hagudu dedei. Ode huluane, oubi afae afae amoga, gilisisu afae afae da Isala: ili soge ouligisu. Gilisisu afae afae amo ganodini, dunu 24,000 agoane ba: i. Amola gilisisu afae afae ouligisu, ilia da oubi afae afaega ouligisu dunu ilegei. Ilia da dadi gagui wa: i hou huluane ouligisu.
Uwu ndi mndandanda wa Aisraeli, atsogoleri a mabanja, olamulira asilikali 1,000, olamulira asilikali 100 ndi akuluakulu awo, amene ankatumikira mfumu mʼzonse zokhudza magulu a ankhondo, amene amagwira ntchito mwezi ndi mwezi chaka chonse. Gulu lililonse linali ndi anthu 24,000.
2 Oubiga gilisisu ouligisu dunu ilia dio da: - Oubi Age - Yasioubia: me. E da Sa: badiele egefe amola Bilese sosogo fi dunu. Bilese sosogo fi da Yuda fi ganodini galu. Oubi Ageyadu - Doudai. E da Ahouhaide egaga fi dunu. Ea bisibagia dunu da Migilode. Oubi Osoda - Bina: ia (gobele salasu dunu Yihoiada egefe) E da gilisisu “Gasa Bagade Dunu 30” amoga bisilua galu. E bagia, egefe Amisaba: de da gilisisu “Gasa Bagade Dunu 30” bisilua hamoi. Oubi Biyadu - A: sahele (Youa: be ea eya). Egefe Sebadaia da e bagia ea gilisisu ouligi. Oubi Bi - Sia: mahade (Isala egaga fi dunu). Oubi Gafe - A: ila (Igesie egefe. E da Degoa moilaiga misi.) Oubi Fesu - Hilese (e da Ifala: ime fi dunu. E da Belounaide dunu.) Oubi Godo - Sibigai (e da Sela sosogo fi dunu. Sela sosogo da Yuda fi amo ganodini galu. Oubi Sesege - A: ibisa (e da A: nadode moilaiga misi. A: nadode da Bediamini fi ilia soge ganodini dialu.) Oubi Nabu - Mahala: iai (e da Nidoufa moilaiga misi. E da Sela sosogo fi dunu.) Oubi Gida - Bina: ia (e da Biladone moilaiga misi. Biladone da Ifala: ime f ilia ganodini dialu Oubi Fago - Heledai (e da Nidoufa moilaiga misi. E da Odeniele egaga fi dunu.) Isala: ili Fi Dunu Ilia Gamane Ouligisu Hou
Amene amalamulira gulu loyamba pa mwezi woyamba anali Yasobeamu mwana wa Zabidieli. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
3
Iyeyu anali chidzukulu cha Perezi ndipo anali mkulu wa atsogoleri onse a ankhondo mwezi woyamba.
4
Amene amalamulira gulu lachiwiri pa mwezi wachiwiri anali Dodai Mwahohi; Mikiloti ndiye anali mtsogoleri wa gulu lake. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
5
Wolamulira ankhondo wachitatu, pa mwezi wachitatu anali Benaya, mwana wa wansembe Yehoyada. Iye anali mtsogoleri ndipo pa gulu lake panali ankhondo 24,000.
6
Uyu ndi Benaya uja amene anali wamphamvu pa gulu la anthu makumi atatu ndipo ndiye amatsogolera anthu makumi atatu aja. Mwana wake Amizabadi ndiye amatsogolera gulu lake.
7
Wachinayi pa mwezi wachinayi anali Asaheli mʼbale wake wa Yowabu; ndipo mwana wake Zebadiya ndiye analowa mʼmalo mwake. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
8
Wachisanu pa mwezi wachisanu anali Samihuti, mdzukulu wa Izira. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
9
Wa 6 pa mwezi wa 6 anali Ira mwana wa Ikesi wa ku Tekowa. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
Wa 7 pa mwezi wa 7 anali Helezi Mpeloni wa fuko la Efereimu. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
Wa 8 pa mwezi wa 8 anali Sibekai Mhusati, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000
Wa 9 pa mwezi wa 9 anali Abiezeri wa banja la Anatoti, wa fuko la Benjamini. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
Wa khumi pa mwezi wa khumi anali Mahazayi wa ku Netofa, wa mbumba ya Zera. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
Mtsogoleri wa 11, pa mwezi wa 11 anali Benaya wa ku Piratoni, wa fuko la Efereimu. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
Mtsogoleri wa 12, pa mwezi wa 12 anali Helidai Mnetofa, wa banja la Otanieli. Pa gulu lake panali asilikali 24,000.
16 Gamane eagene dunu amo da Isala: ili fi ouligisu, ilia dio da hagudu dedei. FiEagene Ouligisu Dunu Liubene Elia: isa (Sigalai egefe) Simione Siefada: ia (Ma: iaga egefe) Lifai Ha: siabaia (Gemiuele egefe) Elane Sa: idoge Yuda Ilaihiu (hina bagade Da: ibidi eaola afae) Isaga Omeli (Maigele egefe) Sebiulane Isiama: ia (Oubadaia egefe) Na: fadalai Yelimode (A: saliele egefe) Ifala: ime Housia (A: isasaia egefe) Guma: dini Ma: na: se Youele (Bida: iya egefe) Gusudili Ma: na: se Idou (Segalaia egefe) Bediamini Ya: isiele (A: bena egefe) Da: ne Asa: iliele (Yilouha: me egefe)
Akuluakulu amene amatsogolera mafuko a Israeli ndi awa: Mtsogoleri wa fuko la Rubeni: Eliezara mwana wa Zikiri; mtsogoleri wa fuko la Simeoni: Sefatiya mwana wa Maaka;
mtsogoleri wa fuko la Levi: Hasabiya mwana wa Kemueli, mtsogoleri wa banja la Aaroni: Zadoki;
mtsogoleri wa fuko la Yuda: Elihu, mʼbale wake wa Davide; mtsogoleri wa fuko la Isakara: Omuri mwana wa Mikayeli;
mtsogoleri wa fuko la Zebuloni: Isimaiya mwana wa Obadiya; mtsogoleri wa fuko la Nafutali: Yerimoti mwana wa Azirieli;
mtsogoleri wa fuko la Efereimu: Hoseya mwana wa Azaziya; mtsogoleri wa fuko la theka la Manase: Yoweli mwana wa Pedaya;
mtsogoleri wa fuko la theka la Manase limene linali ku Giliyadi: Ido mwana wa Zekariya; mtsogoleri wa fuko la Benjamini: Yaasieli mwana wa Abineri;
mtsogoleri wa fuko la Dani: Azareli mwana wa Yerohamu. Awa anali akuluakulu a mafuko a Israeli.
23 Hina bagade Da: ibidi da dunu amo lalelegele ode 20 amoga hame doaga: i, ilia dio idimusa: hame dedei. Bai Hina Gode da Isala: ili fi dunu ilia idi da gasumuni muagado lesula ili defele hamoma: ne ilegele sia: i dagoi.
Davide sanawerenge amuna amene anali ndi zaka makumi awiri kapena kucheperapo, chifukwa Yehova analonjeza kuti adzachulukitsa Aisraeli ngati nyenyezi zamumlengalenga.
24 Youa: be (ea eme da Seluaia) e da Isala: ili fi ilia dio dedemusa: mui, be hame dedene dagoi. Amo dio dedesu hou hamobeba: le, Gode da Isala: ili fi ilima se iasu i. Amaiba: le, amo dio bisili idi da hina bagade Da: ibidi ea dedesu buga amo ganodini hame dedene legei ba: i.
Yowabu mwana wa Zeruya anayamba kuwerenga amuna koma sanamalize. Mkwiyo unagwera Aisraeli chifukwa cha zimenezi ndipo chiwerengerochi sanachilowetse mʼbuku la mbiri ya mfumu Davide.
25 Dunu amo da hina bagade ea liligi ouligi, ilia dio da hagudu dedei. Hina bagade ea LiligiOuligisu Dunu Hina bagade ea liligi legesu sesei...A: sama: ifede (A: idele egefe) Dunudafa ilia liligi legesu sesei...Yihonada: ne (Asaia egefe) Ifabi hawa: hamosu dunu...Eselai (Gilabe egefe) Waini efe sagai...Simiai (e da La: ima moilaiga misi) Waini hano legesu sesei...Sa: badai (e da Sifa: me moilaiga misi) Olife amola ‘sigamo’ ifa (guma: dini agolo sogega dialu) ...Ba: ile Ha: ina: ne (e da Gida moilaiga misi) Olife susuligi legesu diasu...Youa: sie Bulamagau Fofoi amo da Sia: lane umiga lesulu...Sidili (e da Sia: lane moilaiga misi) Bulamagau Fofoi amo da fagoga lesulu...Sia: fa: de (A: dala: iai egefe) Ga: mele...Oubili (Isama: ielaide dunu) Dougi...Yediya (Milonodaide dunu) Sibi amola Goudi...Ya: isisi (Ha: gelaide dunu)
Azimaveti mwana wa Adieli ankayangʼanira nyumba zosungiramo katundu wa mfumu. Yonatani mwana wa Uziya ankayangʼanira nyumba zosungiramo katundu wa maboma ozungulira, mizinda, midzi ndi malo olondera.
Eziri mwana wa Kelubi ankayangʼanira anthu ogwira ntchito yolima ku munda.
Simei wa ku Rama ankayangʼanira minda ya mpesa. Zabidi wa ku Sifamu ankayangʼanira mphesa ndi mosungiramo mwake.
Baala-Hanani wa ku Gederi ankayangʼanira mitengo ya olivi ndi ya mikuyu ya ku Sefela. Yowasi ankayangʼanira mafuta a Olivi.
Sitirayi wa ku Saroni ankayangʼanira ziweto zimene amaweta ku Saroni. Safati mwana wa Adilayi ankayangʼanira ngʼombe zakuzigwa.
Obili Mwismaeli ankayangʼanira ngamira. Yehideya Mmerenoti ankayangʼanira abulu.
Yazizi Mhagiri akayangʼanira nkhosa ndi mbuzi. Onsewa anali akuluakulu oyangʼanira chuma cha mfumu Davide.
32 Da: ibidi aeyama Yonada: ne da medenegi fada: i sia: ne iasu dunu esalu. E amola Yihaiele (Ha: gamounai egefe) da hina bagade egefelali ilia adoba: su hou ouligisu.
Yonatani, malume wake wa Davide, anali phungu wake ndipo anali munthu wanzeru komanso analinso mlembi. Yehieli mwana wa Hakimoni ankasamalira ana a mfumu.
33 Ahidoubele da Da: ibidima fada: i sia: ne iasu dunu esalu. Amola Hiusiai (Agaide dunu) da Da: ibidi ea na: iyado dunu amola ema fada: i sia: ne iasu dunu.
Ahitofele anali phungu wa mfumu. Husai Mwariki anali bwenzi la mfumu.
34 Ahidoubele da bogoloba, amogalu Abaia: da amola Yihoiada (Bina: ia egefe) da Da: ibidima fada: i sia: ne iasu dunu hamoi. Youa: be da hina bagade ea dadi gagui wa: i ouligisu dunu esalu.
Ahitofele atamwalira mʼmalo mwake munalowa Yehoyada mwana wa Benaya ndi Abiatara. Yowabu anali mtsogoleri wa gulu lankhondo la mfumu.

< 1 Hou Olelesu 27 >