< 1 Hou Olelesu 24 >
1 Elane egaga fi da agoane galu. Elane egefelali da Na: ida: be, Abaihiu, Elia: isa amola Idama.
Magulu a ana a Aaroni anali awa: Ana a Aaroni anali Nadabu, Abihu, Eliezara ndi Itamara.
2 Na: ida: be amola Abaihiu da elea ada mae bogole, ela hidadea bogoi. Elagaga fi hameba: le, elea eya Elia: isa amola Idama da gobele salasu dunu hamoi.
Koma Nadabu ndi Abihu anamwalira abambo awo asanamwalire, ndipo analibe ana aamuna. Kotero Eliezara ndi Itamara ankatumikira monga ansembe.
3 hina bagade Da: ibidi da Elane egaga fi ilima ilia hawa: hamosu defele momogili ilegei. Sa: idoge (Elia: isa egaga fi dunu) amola Ahimelege (Idama egaga fi dunu) ela da Da: ibidi fidi.
Mothandizidwa ndi Zadoki chidzukulu cha Eliezara ndi Ahimeleki chidzukulu cha Itamara, Davide anawagawa mʼmagulu molingana ndi ntchito yawo yotumikira.
4 Da: ibidi da Elia: isa egaga fi dunu momogili, gilisisu gilisi agoane hamoi, amola Idama egaga fi dunu momogili, gilisisu godoane agoane hamoi. Bai Elia: isa egaga fi dunumusu ilia idi da Idama egaga fi dunumusu ilia idi baligi.
Atsogoleri ambiri anapezeka pakati pa zidzukulu za Eliezara kusiyana ndi zidzukulu za Itamara ndipo anagawidwa moyenera: atsogoleri 16 a mabanja ochokera kwa Eliezara, ndipo atsogoleri asanu ndi atatu a mabanja ochokera kwa zidzukulu za Itamara.
5 Elia: isa amola Idama elagaga fi dunu mogili da Debolo Diasu ouligisu dunu amola Gode Ea hou ouligisu dunu esalu. Amaiba: le, ilia da ilia hawa: hamosu ilegema: ne, ululuasu.
Anawagawa mosakondera pochita maere, pakuti iwo anali akuluakulu a ku malo opatulika ndi akuluakulu a Mulungu pakati pa zidzukulu za Eliezara ndi Itamara.
6 Elia: isa amola Idama elagaga fi dunu huluane da afae afae ululuala heheda: fusu. Amalalu, Lifai sia: dedesu dunu Siemaia (Nida: niele egefe) da ilia dio dedene legei. Hina bagade Da: ibidi, ea eagene ouligisu dunu, gobele salasu dunu Sa: idoge, Abaia: da egefe Ahimelege amola gobele salasu sosogo fi amola Lifai fi ilia fada: i, amo huluane da ba: su dunu hamoi.
Mlembi Semaya mwana wa Netaneli, Mlevi, analemba mayina awo pamaso pa mfumu ndi akuluakulu ake: wansembe Zadoki, Ahimeleki mwana wa Abiatara ndi atsogoleri a mabanja a ansembe ndiponso Alevi, banja limodzi kuchokera kwa Eliezara kenaka limodzi kuchokera kwa Itamara.
7 Ilia da sosogo fi 24 ilima hawa: hamosu agoane ilegei. Yihoialibi da bisili ilegei. Amalu, Yedaia, Ha: ilime, Sioulimi, Ma: lagaia, Midiamini, Ha: gose, Abaidia, Yesua, Sieganaia, Ilaiasibi, Ya: igimi, Haba, Yisiebia: be, Biliga, Ime, Hise, A:fasisi, Bedahaia, Yihesigele, Ya: igini, Ga: imale, Dila: iya, Ma: iasia.
Maere woyamba anagwera Yehoyaribu, achiwiri anagwera Yedaya,
achitatu anagwera Harimu, achinayi anagwera Seorimu,
achisanu anagwera Malikiya, achisanu ndi chimodzi anagwera Miyamini,
achisanu ndi chiwiri anagwera Hakozi, achisanu ndi chitatu anagwera Abiya,
achisanu ndi chinayi anagwera Yesuwa, a khumi anagwera Sekaniya,
a 11 anagwera Eliyasibu, a 12 anagwera Yakimu,
a 13 anagwera Hupa, a 14 anagwera Yesebeabu,
a 15 anagwera Biliga, a 16 anagwera Imeri,
a 17 anagwera Heziri, a 18 anagwera Hapizezi,
a 19 anagwera Petahiya, a 20 anagwera Ezekieli,
a 21 anagwera Yakini, a 22 anagwera Gamuli,
a 23 anagwera Delaya, ndipo a 24 anagwera Maaziya.
19 Amo dunu da ilia Debolo ganodini hawa: hamosu ilegei defele dedene legei ba: i. Ilia aowa Elane da Isala: ili Hina Gode Ea hamoma: ne sia: i nababeba: le, amo hawa: hamoma: ne sia: i.
Umu ndi mmene anasankhidwira kuti azigwira ntchito yotumikira pamene alowa mʼNyumba ya Yehova, motsatira dongosolo limene anapatsidwa ndi kholo lawo Aaroni, monga momwe Yehova Mulungu wa Israeli anamulamulira.
20 Lifai egaga fi ilia sosogo fada: i dunu amo ilia dio da hagudu dedei. Yehedia (Sibiuele egefe. E da A: mala: me egaga fi dunu.) Isihaia (Liha: baia egaga fi dunu) Ya: iha: de (Siloumode egefe. E da Isaha egaga fi dunu) Hibalone egefelali amo da Yilaia (magobo mano), A:malaia, Yaha: isiele amola Yega: mia: me. Sia: ime (Maiga egefe. E da Asaiele egaga fi dunu.) Segalaia (Maiga eya Isihaia amo egefe. E da Asaiele egaga fi dunu.) Malai, Miusiai amola Ya: iasaia (Milalai egaga fi dunu)
Za zidzukulu zina zonse za Levi: Kuchokera kwa ana a Amramu: Subaeli; kuchokera kwa ana a Subaeli: Yehideya.
Kwa Rehabiya, kuchokera kwa ana ake: Mtsogoleri anali Isiya.
Kuchokera ku banja la Izihari: Selomoti; kuchokera kwa ana a Selomoti: Yahati.
Ana a Hebroni: woyamba anali Yeriya, wachiwiri anali Amariya, wachitatu anali Yahazieli ndipo Yekameamu anali wachinayi.
Mwana wa Uzieli: Mika; kuchokera kwa ana a Mika: Samiri.
Mʼbale wa Mika: Isiya; kuchokera kwa ana a Isiya: Zekariya.
Ana a Merari: Mahili ndi Musi. Mwana wa Yaaziya: Beno.
27 Ya: iasaia egefelali da Siouha: me, Sa: ge amola Ibilai.
Ana a Merari: Kuchokera kwa Yaaziya: Beno, Sohamu, Zakuri ndi Ibiri.
28 Malai egefela da Elia: isa amola Gisia. Elia: isa da dunu mano hame galu. Be Gisa egefe afae fawane da Yilamiele.
Kuchokera kwa Mahili: Eliezara, amene analibe ana aamuna.
Kuchokera kwa Kisi: Mwana wa Kisi: Yerahimeeli.
30 Muisiai egefelali da Malai, Ide amola Yelimode. Amo huluane da Lifai egaga fifi misi.
Ndipo ana a Musi: Mahili, Ederi ndi Yerimoti. Awa anali Alevi potsata mabanja a makolo awo.
31 Sosogo fi afae afae ilia fada: i dunu amola ea eya afae, da ilia fi dunu Elane egaga fi gobele salasu dunu ilia hamoi defele, ilia hawa: hamosu ilegema: ne, ululuasu. Hina bagade Da: ibidi, ea eagene ouligisu dunu, Sa: idoge, Ahimelege amola gobele salasu sosogo fi amola Lifai fi ilia fada: i dunu, amo huluane da amo ilegesu hou ba: su dunu hamoi.
Iwonso anachita maere, monga anachitira abale awo, zidzukulu za Aaroni, pamaso pa mfumu Davide, ndi Zadoki ndi Ahimeleki, atsogoleri a mabanja a ansembe ndi Alevi. Mabanja a mwana wamkulu anachita nawo mofanana ndi a mwana wamngʼono.