< 1 Hou Olelesu 17 >

1 Hina bagade Da: ibidi da hina bagade diasu amo ganodini esalu. Eso afaega, e da balofede (Gode Sia: Alofesu Dunu) Na: ida: ne ema misa: ne sia: ne, ema amane sia: i, “Na da diasu noga: i amo dolo ifaga hamoi, amo ganodini hahawane esala. Be Gode Ea Gousa: su Sema Gagili da udigili abula diasu ganodini diala!”
Davide atakhazikika mʼnyumba yake yaufumu, anawuza mneneri Natani kuti, “Ine pano ndikukhala mʼnyumba yaufumu yomanga ndi mitengo ya mkungudza, pomwe Bokosi la Chipangano la Yehova lili mu tenti.”
2 Na: idane da bu adole i, “Dia hanai defele hamoma! Bai Hina Gode da ani esala.”
Natani anayankha Davide kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu, chifukwa Mulungu ali nanu.”
3 Be amo gasia, Hina Gode da Na: ida: nema amane sia: i,
Usiku umenewo mawu a Mulungu anafika kwa Natani, ndipo anati,
4 “Dia asili, na hawa: hamosu dunu Da: ibidi ema amane sia: ma, ‘Di da debolo amo ganodini Na da esalumu amo gaguma: ne, Na da di hame ilegei.
“Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti, sudzandimangira ndiwe nyumba yokhalamo.’
5 Na da Isala: ili fi dunu Idibidi sogea esalu amo gaga: lalu amogainini wali, Na da Debolo Diasu ganodini hame esalu. Be na da abula diasu ganodini fawane esalu.
Ine sindinakhalepo mʼnyumba kuyambira tsiku limene ndinatulutsa Israeli mʼdziko la Igupto mpaka lero lino. Ndakhala ndikuyenda kuchoka mʼtenti ina kupita mʼtenti ina, kuchoka malo ena kupita malo ena.
6 Na da Isala: ili dunu eso bagohame nini ahoanoba, Na da ouligisu dunu amo Na da ilegei ilima, ‘dilia da abuliba: le nama dolo ifa amoga hamoi Debolo Diasu hame gaguila: ?’ amane hamedafa adole ba: su.
Konse ndakhala ndikuyenda ndi Aisraeli onse, kodi ndinanenapo kwa wina aliyense wa atsogoleri awo amene ndinamulamula kuweta anthu anga kuti, ‘Kodi nʼchifukwa chiyani simunandimangire nyumba ya mitengo ya mkungudza?’”
7 Amaiba: le, Na hawa: hamosu dunu Da: ibidi ema amane sia: ma, ‘Na, Hina Gode Bagadedafa, da dia sogega sibi ouligilalu amo lale, Na fi dunu Isala: ili amo ouligima: ne hina bagade hamoi.
Ndipo tsopano umuwuze mtumiki wanga Davide kuti, “Yehova Wamphamvuzonse akuti, Ine ndinakutenga ku busa ukuweta nkhosa, kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga, Aisraeli.
8 Di da habodili ahoanoba, Na da ani galu ahoasu galu. Amola di da gusuba: i mogodigili ahoabeba: le, Na da dia ha lai dunu hasasalisu. Na da di osobo bagade baligili bagade ouligisu dunu defele, dunu eno dima nodoma: ne hamomu.
Ineyo ndinali nawe kulikonse kumene unkapita, ndipo ndachotsa adani ako onse pamaso pako. Tsopano ndidzakuza dzina lako kuti likhale mʼgulu la mayina a anthu otchuka kwambiri pa dziko lapansi.
9 Na da Na fi Isala: ili dunu esaloma: ne sogebi ilegele, ilia hahawane fima: ne hamoi dagoi. Ilia da amogawi enoga mae banenesili esalumu. Ilia da amo soge ganodini golili sa: ili amogainini wali eso, nimi bagade ha lai dunu da ilima doagala: lebe ba: su. Be amo hou da bu hame ba: mu. Na da dia ha lai iliga mae hasalasima: ne, Na da di gaga: ma: ne dafawane ilegesa. Amola Na da dima digaga fi imunu.
Ndipo ndidzawapatsa malo anthu anga, Aisraeli ndipo ndidzawadzala pamalo awoawo kuti asadzavutitsidwenso. Anthu oyipa sadzawazunzanso monga ankachitira poyamba paja;
monga akhala akuchitira kuchokera nthawi imene ndinasankha atsogoleri a anthu anga Aisraeli. Ine ndidzagonjetsanso adani anu onse. “‘Ine ndikulengeza kwa iwe kuti Yehova adzakhazikitsa banja lako.
11 Di bogosea amola dia aowalali dunu ilima gilisili uli dogoi ba: sea, Na da diagofe afae hina bagade hamoma: mu. Amola Na da ea hina bagade hou amoma gasa imunu.
Masiku ako akadzatha ndipo ukadzatsatira makolo ako, Ine ndidzawutsa mphukira yako imene idzalowa mʼmalo mwako, mmodzi mwa ana ako, ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wake.
12 E da Na Debolo Diasu gagumu, amola ea ouligisu da eso huluane fifi ahoanoma: ne, amo Na da ilegesa.
Iye ndiye amene adzandimangira nyumba, ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wake kwamuyaya.
13 Na da ea Ada esalumu, amola e da Nagofe esalumu. Na da di hina bagade hamoma: ne, Solo fadegai. Be Na da Soloma Na fuligala: su hou fadegai, amo defele diagofema Na fuligala: su hou hamedafa fadegamu.
Ine ndidzakhala abambo ake, ndipo iye adzakhala mwana wanga. Ine sindidzasiya kumukonda monga ndinachitira ndi amene unalowa mʼmalo mwawo.
14 E amola digaga fi da mae dagole, osobo bagadega esalebe ba: mu. Amola digaga fi ilia hina bagade hou da eso huluane fifi ahoanumu. Amola dia hina bagade hou da hamedafa dagomu.”
Ndidzamuyika kukhala wolamulira nyumba yanga ndi ufumu wanga kwamuyaya. Mpando wake waufumu udzakhazikika kwamuyaya.’”
15 Na: ida: ne da liligi huluane amo Gode da ema olelei, amo huluane Da: ibidima alofele olelei.
Natani anafotokozera Davide mawu onse avumbulutso limene analandira.
16 Amalalu, hina bagade Da: ibidi da Hina Gode Ea Abula Diasu amo ganodini golili sa: ili, amane sia: ne gadosa esalu. “Ouligisudafa Hina Gode! Di da nama hou noga: idafa hamoi dagoi. Be na amola na sosogo fi da Dia fidisu lamu defele hame agoai ba: sa.
Choncho Mfumu Davide analowa mu tenti nakhala pamaso pa Yehova, ndipo anati, “Ine ndine yani, Inu Yehova Mulungu, ndipo banja langa nʼchiyani kuti mundifikitse pamene ndafikapa?
17 Be wali Ouligisudafa Hina Gode! Di da baligili hamosa. Di da nagaga fa: no misunu dunu fi amo noga: le fidima: ne ilegesa. Amola Ouligisudafa Hina Gode! Di da amo na ba: ma: ne hamosa.
Inu Mulungu, kukhala ngati izi ndi zosakwanira pamaso panu, Inuyo mwayankhula zatsogolo la banja la mtumiki wanu. Mwandiyangʼana ndipo mwandiyesa ngati munthu wolemekezeka kwambiri pakati pa anthu, Inu Yehova Mulungu.”
18 Na da Dima adi sia: ma: bela: ? Na da Dia hawa: hamosu dunu! Amola Dia na dawa: !
“Kodi Davide anenenso chiyani kwa Inu, pakuti mwachitira ulemu wotere mtumiki wanu? Pakuti Inu mukumudziwa mtumiki wanu.
19 Di da amo hou hamomu hanaiba: le amola ilegeiba: le hamosu. Di da nama bagade hou misunu amo olelema: ne, amo hou hamosu.
Inu Yehova, chifukwa cha mtumiki wanu komanso mwa chifuniro chanu, mwachita chinthu chachikulu ichi ndipo mwawulula malonjezo anu aakulu onse.
20 Ouligisudafa Hina Gode! Di da bagadedafa! Dunu eno Di agoai da hamedafa! Di fawane da Godedafa! Ninia eso huluane amo dawa: i galu.
“Palibe wina wofanana nanu, Inu Yehova, ndipo palibe Mulungu wina koma Inu nokha monga tamvera ndi makutu athu.
21 Eno fi Isala: ili fi agoai da osobo bagadega hame gala. Isala: ili fi dunu da musa: Idibidi sogega udigili hawa: hamosu dunu esalu. Be Di da ili Dia fidafa dunu hamoma: ne, ili gaga: i. Di da ili fidima: ne, baligili gasa bagade hamobeba: le, osobo bagade fifi asi gala huluane da Dia hou nodone dawa: Dia fi dunu amo Di da Dia Fidafa hamoma: ne, Idibidi sogega fisili masa: ne asunasi, ilia da gusuba: i ahoabeba: le, Di da fifi asi gala eno amo sefasilalu.
Ndipo ndi ndani wofanana ndi anthu anu Aisraeli, mtundu wokhawo pa dziko lapansi umene Mulungu wake anapita kukawuwombola, monga anthu akeake ndi kukadzitchukitsa yekha pochita zinthu zodabwitsa zazikulu, pothamangitsa mitundu ina pamaso pa anthu ake, amene Inu munawawombola ku Igupto?
22 Dia da Isala: ili fi amo Dia Fidafa eso huluane esaloma: ne hamoi dagoi. Hina Gode! Di da ilia Godedafa hamoi dagoi.
Inu munawapanga anthu anu Aisraeli kukhala anuanu kwamuyaya, ndipo Inu, Inu Yehova ndinu Mulungu wawo.
23 Amola wali, Hina Godedafa, Dia nama amola nagaga fi ilima hamomusa: ilegele sia: i, amo huluane hamoma.
“Ndipo tsopano Yehova, sungani kwamuyaya lonjezo limene mwachita ndi mtumiki wanu ndi banja lake, likhazikitseni kwamuyaya. Chitani monga mwalonjezera,
24 Dunu huluane da Dia gasa bagade hou dawa: mu. Amola ilia da amane sia: mu, ‘Ouligisudafa Hina Gode da Isala: ili fi dunu ilia Gode esala’. Amola Dia da na hina bagade ouligisu hou eso huluane dialoma: ne hamomu.
kotero dzina lanu likhazikike ndi kukhala lotchuka mpaka muyaya. Ndipo anthu adzanena kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa woyangʼanira Israeli, ndi Mulungu wa Israeli!’ Ndipo banja la mtumiki wanu Davide lidzakhazikika pamaso panu.
25 Hina Gode Bagadedafa! Isala: ili fi ilia Gode! Na da Dima agoane sia: ne gadobeba: le hame beda: sa. Bai na da Dia hawa: hamosu dunu, amola Di da amo hou huluane nama olelei. Amola nagaga fi dunu da hina bagade hamomu, Di sia: i dagoi.
“Inu Mulungu wanga, mwaululira mtumiki wanu kuti mudzamumangira nyumba. Nʼchifukwa chake ine mtumiki wanu ndalimba mtima kupemphera motere.
26 Wali, Ouligisudafa Hina Gode! Di da Godedafa! Di da nama noga: le ilegele sia: i, amola Dia ilegesu huluane, Di da dafawane hamosa.
Inu Yehova, ndinu Mulungu! Mwalonjeza zinthu zabwinozi kwa mtumiki wanu.
27 Na da Dima edegesa. Di da mae fisili nagaga fi ilima hahawane dogolegele ba: ma: ne, ilima hahawane dogolegele hamoma. Di, Ouligisudafa Hina Gode! Di da amo hamoma: ne ilegei dagoi. Amola Di da eso huluane nagaga fi ilima hahawane dogolegele hamomu.”
Ndipo chakukomerani kudalitsa banja la mtumiki wanu kuti likhale pamaso panu mpaka muyaya. Pakuti Inu Yehova mwalidalitsa, lidzakhala lodalitsika mpaka muyaya.”

< 1 Hou Olelesu 17 >