< 1 Hou Olelesu 16 >

1 Ilia da Gode Ea Gousa: su Sema Gagili amo gaguli asili, Da: ibidi ea hamoi Abula Diasu amo ganodini sali. Amalalu, ilia da gobele salasu amola Hahawane Gilisili Olofole Iasu Godema nodoma: ne hamoi.
Iwo anabwera nalo Bokosi la Mulungu ndipo analiyika pamalo pake mʼkati mwa tenti imene Davide anayimika ndipo iwo anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano pamaso pa Mulungu.
2 Da: ibidi da ilia iasu liligi huluane gobele sanawene, e da Hina Gode Ea Dioba: le, Gode da Isala: ili dunuma hahawane dogolegele ima: ne sia: ne gadoi.
Davide atatsiriza kupereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano, iye anadalitsa anthu mʼdzina la Yehova.
3 E da ilima ha: i manu sagoi. E da Isala: ili dunu amola uda afae afae ilima agi ga: gi afae, hu dadamoi afae amola hafogai waini fage sagoi.
Kenaka anagawira Mwisraeli aliyense, wamwamuna ndi wamkazi, aliyense buledi mmodzi, nthuli yanyama ndiponso keke yamphesa zowuma.
4 Da: ibidi da Lifai fi dunu mogili, Isala: ili fi ilia Hina Gode Ea Gousa: su Sema Gagili amo midadi, Godema nodone sia: ne gadosu amola gesami hea: su amo ouligima: ne, ilegei.
Iye anasankha Alevi ena kuti azitumikira pamene panali Bokosi la Yehova, kuti azipemphera, azithokoza ndi kulemekeza Yehova Mulungu wa Israeli.
5 E da A: isa: fe ouligisudafa ilegei (A: isa: fe da giga: mesa duma: ne ilegei). Ea fidisu dunu da Segalaia. Eno ouligisu dunu da, Yiaiele, Similamode, Yihaiele, Ma: didaia, Ilaia: be, Bina: ia, Oubede Idome amola Yiaiele. Amo dunu da sani baidama duma: ne ilegei.
Mtsogoleri wawo anali Asafu, wachiwiri anali Zekariya, kenaka Yeiyeli, Semiramoti, Yehieli, Matitiya, Eliabu, Benaya, Obedi-Edomu ndi Yeiyeli. Iwo amayimba azeze ndi apangwe, Asafu amayimba ziwaya za malipenga,
6 Da: ibidi da gobele salasu dunu aduna amo Bina: ia amola Yaha: isiele, eso huluane Gode Ea Gousa: su Sema Gagili midadi dalabede fulaboma: ne ilegei.
ndipo ansembe Benaya ndi Yahazieli amawomba malipenga nthawi zonse pamaso pa Bokosi la Chipangano la Mulungu.
7 Amo esoga, Da: ibidi da degabo agoane, A:isa: fe amola Lifai fi dunu eno, amo Godema nodone gesami hea: ma: ne ilegei.
Tsiku limeneli Davide anayamba nʼkusankha Asafu ndi anzake kuti ndiwo apereke nyimbo iyi ya matamando kwa Yehova:
8 Hina Godema nodone sia: ma! Ea gasa bagade hou olelema! Fifi asi gala huluane ilima Ea hamobe olelema!
Yamikani Yehova, itanani dzina lake; lalikani za ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu.
9 Hina Godema nodone gesami hea: le ima! Amola liligi noga: idafa Ea hamoi amo adodoma.
Imbirani Iye, muyimbireni nyimbo zamatamando; nenani za ntchito zake zonse zodabwitsa.
10 Nini da Ea fi dunuba: le, Ema nodoma. Amola dunu huluane Ema fa: no bobogebe da nodone sia: ma: ma.
Nyadirani dzina lake loyera; ikondwere mitima ya iwo akufunafuna Yehova.
11 Hina Gode Ea fidima: ne masa, amola Ema mae yolele nodonanoma.
Dalirani Yehova ndi mphamvu zake; funafunani nkhope yake nthawi zonse.
12 Dilia da Gode Ea hawa: hamosu dunu A: ibalaha: me amola Ya: igobe, Hi ilegele lai, egaga fifi mana. Dilia da Gode Ea musa: degabo hame ba: su hou hamoi amo dawa: ma, amola se imunusa: fofada: su Ea hamoi, amo bu dawa: ma.
Kumbukirani ntchito zodabwitsa wazichita, zozizwitsa zake, ndi kuweruza kwa mʼkamwa mwake,
inu zidzukulu za Israeli mtumiki wake, inu ana a Yakobo, osankhidwa ake.
14 Hina Gode da ninia Gode. Ea hamoma: ne sia: i, E da osobo bagade fifi asi huluane ilima sia: i.
Iye ndiye Yehova Mulungu wathu; chiweruzo chake chili pa dziko lonse lapansi.
15 E da Ea Gousa: su Sema hamoi amo eso huluane mae fisili ouligilalumu. E hamomusa: ilegei da fifi manebe 1,000 agoane bobaligila misunu, ilima dialumu.
Iye amakumbukira pangano lake nthawi zonse, mawu amene Iye analamula, kwa mibado miyandamiyanda,
16 E da A: ibalahame amola Aisage elama hamomusa: ilegele sia: i, amo E da gagui dialumu.
pangano limene anachita ndi Abrahamu, lonjezo limene analumbira kwa Isake.
17 Hina Gode da Ya: igobema eso huluane dialoma: ne gousa: su hamoi.
Iye analitsimikiza kwa Yakobo monga lamulo, kwa Israeli monga pangano lamuyaya.
18 E amane ilegele sia: i, “Na da Ga: ina: ne soge dima imunu. Amo soge da di fawane gaguli dialumu.”
“Kwa iwe, ine ndidzapereka dziko la Kanaani monga cholowa chimene udzachilandira.”
19 Gode Ea fi dunu da bagahame galu. Ilia da Ga: ina: ne soge ganodini ga fi dunu agoane ba: i.
Ali anthu owerengeka, ochepa ndithu, komanso alendo mʼdzikomo,
20 Ilia da soge enoga enogaia udigili lafiadalu.
iwo anayendayenda kuchoka ku mtundu wina kupita ku mtundu wina, ku ufumu wina kupita ku ufumu wina.
21 Be Gode da ili gaga: iba: le, eno fi da ili hame banenesi. Ili gaga: ma: ne, Gode da eno hina bagade dunu ilima amane sia: i,
Iye sanalole munthu aliyense kuti awapondereze; chifukwa cha iwo, Iye anadzudzula mafumu:
22 “Na ilegei hawa: hamosu dunu, ilima mae se nabasima. Na balofede dunuma, mae digili ba: ma!”
“Musakhudze odzozedwa anga; musawachitire choyipa aneneri anga.”
23 Hina Godema gesami hea: le hahawane nodone sia: ma! Osobo bagade fifi asi gala huluanema gesami hea: ma. Eso huluane Ea nini gaga: i sia: noga: idafa amo sia: nanoma.
Imbirani Yehova, dziko lonse lapansi; lalikani za chipulumutso chake tsiku ndi tsiku.
24 Fifi asi galama Ea hadigi amodili ima. E da fifi asi gala huluanema Ea gasa bagade hou amo hamonanebeba: le, ilima sisia: ma.
Lengezani za ulemerero wake kwa mitundu yonse, ntchito zake zonse zodabwitsa kwa anthu onse.
25 Hina Gode da bagadedafaba: le, Ema baligili nodomu da defea. Eno ‘gode’ da gudulisili, Ema fawane da baligili nodone dawa: mu da defea.
Pakuti Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kwambiri kumutamanda; Iyeyo ayenera kuopedwa kuposa milungu yonse.
26 Eno ‘gode’ fifi asi gala amoga galebe da ogogole ‘gode’ fawane, be Hina Gode da mu huluane hahamoi.
Pakuti milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi mafano wopanda pake, koma Yehova analenga kumwamba.
27 Hadigi amola baligili gasa bagade da E sisiga: sa, gasa bagade amola noga: idafa ba: su da Ea Debolo Diasu amo nabale galei.
Ulemerero ndi ufumu zili pamaso pake; mphamvu ndi chimwemwe zili pa malo pokhala Iye.
28 Osobo bagade dunu huluane! Hina Godema nodone sia: ma! Ea gasa bagade hou amola Ea hadigidafa amoma nodone sia: ma!
Perekani kwa Yehova, Inu mabanja a anthu a mitundu ina, perekani kwa Yehova ulemerero ndi mphamvu,
29 Hina Gode Ea hadigi Dio amoma nodone sia: ma. Ea Debolo Diasu ganodini Ema iasu gaguli misa. Hadigidafa Gode da amogawi doaga: sea, Ea midadi beguduma!
perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake. Bweretsani chopereka ndipo mufike pamaso pake; pembedzani Yehova mu ulemerero wachiyero chake.
30 Fifi asi gala huluane! Ema beda: iba: le, uguguma! Osobo bagade da noga: le ligisiba: le, fogomu gogolei.
Njenjemerani pamaso pake, dziko lonse lapansi! Dziko linakhazikika kolimba; silingasunthidwe.
31 Osobo bagade amola mu, ali nodoma! Fifi asi gala huluanema amane olelema, “Hina Gode da Hina Bagadedafa!”
Zakumwamba zisangalale, dziko lapansi likondwere; anene anthu a mitundu ina, “Yehova ndi mfumu!”
32 Hano wayabo bagade amola amo ganodini esalebe liligi huluane! Huma! Amola soge, di ganodini liligi dialebe huluane nodone sia: ma!
Nyanja ikokome, ndi zonse zili mʼmenemo; minda ikondwere, ndi zonse zili mʼmenemo!
33 Hina Gode da osobo bagade ouligimusa: masea, ifalabo aligi da nodone sia: mu. E da defeledafa Ea moloidafa fofada: su amoga fifi asi huluane ouligimu.
Ndipo mitengo ya mʼnkhalango idzayimba, idzayimba chifukwa cha chimwemwe pamaso pa Yehova, pakuti akubwera kudzaweruza dziko lapansi.
34 Hina Godema nodoma! Hina Godema nodone sia: ma! Bai E da noga: idafa, amola Ea asigi hou da mae fisili dialumu.
Yamikani Yehova, pakuti Iye ndi wabwino; chikondi chake chikhala mpaka muyaya.
35 Hina Godema amane sia: ma, “Hina Gode! Ninia Gode! Nini gaga: ma! Ninia da fifi asi gala amo ganodini esala, amoga nini Isala: ili sogega buhagimusa: oule misa. Amasea, ninia da Dia hadigi Dio amoma nodone sia: mu.”
Fuwulani kuti, “Tipulumutseni, Inu Mulungu wa chipulumutso chathu, mutisonkhanitse ndipo mutipulumutse kwa anthu a mitundu ina, kuti tiyamike dzina lanu loyera, kuti tikutamandeni.”
36 Hina Godema nodoma! Isala: ili ilia Godema nodoma Wali amola eso huluane mae fisili, Ema nodone sia: nanoma! Amalalu, dunu huluane da “Ama” sia: ne, Hina Godema nodone sia: ne gadoi.
Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli, kuyambira muyaya mpaka muyaya. Ndipo anthu onse anati, “Ameni” ndipo “Tikutamandani Yehova.”
37 Da: ibidi da A: isa: fe amola Lifai fi dunu, amo Gode Ea Gousa: su Sema Gagili midadi, eso huluane hamobe nodone sia: ne gadosu hou, amo ouligima: ne, ilegei.
Ndipo Davide anasiya Asafu pamodzi ndi anzake kumene kunali Bokosi la Chipangano la Yehova kuti azitumikira kumeneko nthawi zonse, monga mwa zoyenera kuchita pa tsiku lililonse.
38 Da: ibidi da Oubede Idome (Yediudane egefe) amola ea fi dunu eno68agoane, amo dunu fidima: ne ilegei. Logo ga: su ouligisu dunu da Housa amola Oubede Idome.
Iye anasiyanso Obedi-Edomu pamodzi ndi anzake 68 kuti azitumikira nawo pamodzi. Obedi-Edomu mwana wa Yedutuni ndi Hosa anali alonda a pa chipata.
39 Be gobele salasu dunu Sa: idoge amola ea gobele salasu fi dunu, ilia da Gibione moilai bai bagadega (nodone sia: ne gadosu sogebi eno) Hina Godema nodone sia: ne gadosu hou ouligisu.
Davide anasiya wansembe Zadoki ndi ansembe anzake ku chihema cha Yehova ku malo achipembedzo ku Gibiyoni
40 Ilia da amo dunu hahabe amola daeya, sema amo da Hina Gode da Isala: ili dunuma i, amo defele, ohe gogo gobele salimusa: ilegei.
kuti azipereka nsembe zopsereza kwa Yehova pa guwa lansembe nthawi zonse mmawa ndi madzulo, potsata zonse zimene zinalembedwa mʼbuku la malamulo a Yehova, amene anawapereka kwa Aisraeli.
41 Ilia da amo dunu fidima: ne, amola Hina Gode Ea mae fisili asigidafa hou dawa: ma: ne, Ema nodone gesami hea: ma: ne, Hima: ne, Yediudane amola eno dunu, ilegei.
Anthuwo anali pamodzi ndi Hemani ndi Yedutuni ndi onse amene anawasankha mowatchula dzina kuti apereke mayamiko kwa Yehova, “pakuti chikondi chake ndi chosatha.”
42 Hima: ne amola Yediudane amolawane da dalabede amola giga: mesa amola dusu liligi eno amoga ilia da nodone gesami hea: su fidisu, amo ouligi. Yediudane ea fi dunu da logo ga: su sosodo aligisu hou amo ouligi.
Hemani ndi Yedutuni anali oyangʼanira malipenga ndi ziwaya ndiponso zipangizo zina zoyimbira nyimbo zachipembedzo. Ana a Yedutuni anawayika kuti aziyangʼanira pa chipata.
43 Amalalu, dunu huluane da ilia diasua buhagi. Amola Da: ibidi da ea diasu, ea sosogo gilisili esalumusa: buhagi.
Kenaka anthu onse anachoka, aliyense kupita kwawo. Ndipo Davide anabwerera ku nyumba kwake kukadalitsa banja lake.

< 1 Hou Olelesu 16 >