< Dagiti Salmo 27 >

1 Ni Yahweh ti silaw ken salakanko; siasino ti pagbutngak? Ni Yahweh ti kamang ti biagko; siasino ti pagamakak?
Salimo la Davide. Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa; ndidzaopa yani? Yehova ndi linga la moyo wanga; ndidzachita mantha ndi yani?
2 Idi immasideg kaniak dagiti managdakdakes a mangalun-on iti lasagko, naitibkol ken napasag dagiti mangsupsupiat kaniak ken dagiti kabusorko.
Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane kudzadya mnofu wanga, pamene adani anga ndi achiwembu andithira nkhondo, iwo adzapunthwa ndi kugwa.
3 Uray no agkampo ti armada a maibusor kaniak, saanto nga agbuteng ti pusok; uray no rumsua ti gubat a maibusor kaniak, uray no kasta agtalinaedak a natalged.
Ngakhale gulu lankhondo lindizinge, mtima wanga sudzaopa. Ngakhale nkhondo itayambika kulimbana nane, ngakhale nthawi imeneyo, ine ndidzalimbika mtima.
4 Maysa a banag a dinawatko kenni Yahweh, ket sapulekto dayta: nga agnaedak koma iti balay ni Yahweh iti amin nga aldaw iti panagbiagko, tapno makitak ti kinaimnas ni Yahweh ken tapno utobek ti maipanggep kenkuana iti templona.
Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova, ichi ndi chimene ndidzachifunafuna: kuti ndikhale mʼNyumba ya Yehova masiku onse a moyo wanga, ndi kuyangʼana kukongola kwa Yehova, ndi kumufunafuna Iye mʼNyumba yake.
5 Ta iti aldaw ti riribuk linongannak iti kalapawna; iti abbong ti toldana ilemmengnak. Ipangatonakto iti rabaw ti bato!
Pakuti pa tsiku la msautso Iye adzanditeteza mʼmalo ake okhalamo; adzandibisa mʼkati mwa Nyumba yake ndi kukhazika ine pamwamba pa thanthwe.
6 Ket maipangatonto ti ulok iti ngatoen dagiti kabusorko nga adda iti aglawlawko, ket mangidatonakto iti daton ti panagragrag-o iti toldana! Agkantaak ken mangaramidak kadagiti kankanta para kenni Yahweh!
Kotero mutu wanga udzakwezedwa kuposa adani anga amene andizungulira; pa Nyumba yake ndidzapereka nsembe ndi mfuwu wachimwemwe; ndidzayimba nyimbo kwa Yehova.
7 Denggem, O Yahweh, ti timekko no umawagak! Maasika kaniak ket sungbatannak!
Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova mundichitire chifundo ndipo mundiyankhe.
8 Kuna ti pusok maipapan kenka, “Sapulem ti rupana!” Sapulek ti rupam, O Yahweh!
Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!” Nkhope yanu Yehova ndidzayifunafuna.
9 Saanmo nga ilemmeng ti rupam kaniak; saanmo a dangran daytoy adipenmo iti unget! Sika idi ti katulongak; saannak a baybay-an wenno panawan, Dios ti salakanko!
Musandibisire nkhope yanu, musamubweze mtumiki wanu mwamkwiyo; mwakhala muli thandizo langa. Musandikane kapena kunditaya, Inu Mulungu Mpulumutsi wanga.
10 Uray no ti amak ken inak ket baybay-andak, ni Yahweh awatennak.
Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya Yehova adzandisamala.
11 Isurom kaniak ti dalanmo, O Yahweh! Iturongnak iti nasimpa a dalan gapu kadagiti kabusorko.
Phunzitseni njira yanu Inu Yehova, munditsogolere mʼnjira yowongoka chifukwa cha ondizunza.
12 Saannak nga iyawat kadagiti tarigagay dagiti kabusorko, ta timmakder dagiti palso a saksi a maibusor kaniak, ket iyesngawda ti kinaranggas!
Musandipereke ku zokhumba za adani anga, pakuti mboni zambiri zauka kutsutsana nane ndipo zikundiopseza.
13 Anianto ngatan ti mapasamak kaniak no saanko a pinati a makitak ti kinaimbag ni Yahweh iti daga dagiti sibibiag?
Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi; ndidzaona ubwino wa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
14 Agtalekka kenni Yahweh; pumigsaka, pakiredem ti pusom! Agtalekka kenni Yahweh!
Dikirani pa Yehova; khalani anyonga ndipo limbani mtima nimudikire Yehova.

< Dagiti Salmo 27 >