< Psalm 126 >
1 Ein Wallfahrtslied. Als der HERR einst Zions Mißgeschick wandte,
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
2 Damals war unser Mund voll Lachens und unsre Zunge voll Jubels; damals sagte man unter den Heiden: »Der HERR hat Großes an ihnen getan!«
Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
3 Ja, Großes hatte der HERR an uns getan: wie waren wir fröhlich!
Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
4 Wende, o HERR, unser Mißgeschick gleich den Bächen im Mittagsland!
Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
5 Die mit Tränen säen, werden mit Jubel ernten.
Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
6 Wohl schreitet man weinend dahin, wenn man trägt den Samen zur Aussaat; doch jubelnd kehrt man heim, mit Garben beladen.
Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.