< Tingtoeng 27 >

1 David kah BOEIPA tah kai kah vangnah neh ka daemnah ni. Unim ka rhih bal eh. BOEIPA tah ka hingnah lunghim ni. Unim ka rhih pueng eh?
Salimo la Davide. Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa; ndidzaopa yani? Yehova ndi linga la moyo wanga; ndidzachita mantha ndi yani?
2 Thaehuet ka rhal rhoek neh ka thunkha rhoek loh ka saa caak ham ka taengla halo vaengah paloe uh vetih cungku uh ni.
Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane kudzadya mnofu wanga, pamene adani anga ndi achiwembu andithira nkhondo, iwo adzapunthwa ndi kugwa.
3 Caem loh ka taengah rhaeh cakhaw ka lungbuei loh rhih mahpawh. Caemtloek loh kai taengah a thoh vaengah he khaw ka pangtung ni.
Ngakhale gulu lankhondo lindizinge, mtima wanga sudzaopa. Ngakhale nkhondo itayambika kulimbana nane, ngakhale nthawi imeneyo, ine ndidzalimbika mtima.
4 Ka hingnah khohnin boeih he BOEIPA im ah khosak tih BOEIPA kah mueithen te hmuh ham neh a bawkim ah hnukdawn ham pakhat bueng te ka hue tih BOEIPA taengah ka bih.
Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova, ichi ndi chimene ndidzachifunafuna: kuti ndikhale mʼNyumba ya Yehova masiku onse a moyo wanga, ndi kuyangʼana kukongola kwa Yehova, ndi kumufunafuna Iye mʼNyumba yake.
5 Yoethae hnin ah amah kah po ah kai n'khoem ni. A dap kah a huephael ah kai n'thuh vetih lungpang sola kai n'pomsang ni.
Pakuti pa tsiku la msautso Iye adzanditeteza mʼmalo ake okhalamo; adzandibisa mʼkati mwa Nyumba yake ndi kukhazika ine pamwamba pa thanthwe.
6 Ka kaepvai kah ka thunkha rhoek sola ka lu a pomsang pawn vetih amah kah dap ah hmueih ka nawn ni. Tamlung neh ka hlai vetih BOEIPA te ka tingtoeng ni.
Kotero mutu wanga udzakwezedwa kuposa adani anga amene andizungulira; pa Nyumba yake ndidzapereka nsembe ndi mfuwu wachimwemwe; ndidzayimba nyimbo kwa Yehova.
7 Aw BOEIPA, ka ol han ya lah. Kan khue vaengah n'rhen lamtah n'doo dae.
Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova mundichitire chifundo ndipo mundiyankhe.
8 Ka lungbuei loh nang kawng dongah, “Kai maelhmai tlap lah!,” a ti dongah nang maelhmai ni ka tlap eh BOEIPA.
Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!” Nkhope yanu Yehova ndidzayifunafuna.
9 Kai taeng lamkah na hmai thuh boeh. Na sal kah thintoek dongah mangthong boel mai. Kai aka bomkung la na om tih kai nan phap sut pawt dongah ka daemnah Pathen nang loh kai nan hnoo moenih.
Musandibisire nkhope yanu, musamubweze mtumiki wanu mwamkwiyo; mwakhala muli thandizo langa. Musandikane kapena kunditaya, Inu Mulungu Mpulumutsi wanga.
10 A nu neh a pa long pataeng kai n'hnoo rhoi dae BOEIPA loh kai n'khoem.
Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya Yehova adzandisamala.
11 Kai he na longpuei n'thuinuet lamtah ka lungawn rhoek kongah kai he tlangkol caehlong ah m'mawt lah BOEIPA.
Phunzitseni njira yanu Inu Yehova, munditsogolere mʼnjira yowongoka chifukwa cha ondizunza.
12 A hong kah laipai rhoek neh kuthlahnah kah hil loh kai taengah tlai uh dae ka rhal rhoek kah hinglu dongah kai nan tloeng moenih.
Musandipereke ku zokhumba za adani anga, pakuti mboni zambiri zauka kutsutsana nane ndipo zikundiopseza.
13 Aka hing rhoek kah khohmuen ah BOEIPA kah a thennah te hmuh ham ka tangnah pueng.
Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi; ndidzaona ubwino wa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
14 BOEIPA te lamtawn lah. Thaahuel lamtah na lungbuei ning sak. Te dongah BOEIPA te lamtawn lah.
Dikirani pa Yehova; khalani anyonga ndipo limbani mtima nimudikire Yehova.

< Tingtoeng 27 >