< Aroma 8 >
1 Choncho, tsopano amene ali mwa Khristu Yesu alibe mlandu owatsutsa
Bhai nnaino kwakwa kuukumulwa mboteko kwa bhandu bhalundenenje na a Yeshu Kilishitu.
2 chifukwa mwa Khristu Yesu, lamulo la Mzimu Woyera amene amapereka moyo, lawamasula ku lamulo la tchimo ndi la imfa.
Pabha kweli jika Mbumu jwa gumi guli nkati ja a Yeshu Kilishitu jishing'embuya na mashili ga yambi na shiwo.
3 Pakuti zimene Malamulo sanathe kuzichita, popeza anali ofowoka chifukwa cha khalidwe lathu la uchimo, Mulungu anazichita potumiza Mwana wake mʼchifanizo cha munthu ochimwa kuti akhale nsembe yauchimo. Ndipo Iye anagonjetsa tchimo mʼthupi la munthu,
Annungu bhashitenda ikomboleshe, ikakombolekaga kwa shalia ila, kwa ligongo lya ungakola mashili gwa shiilu. Bhai a Nnungu gubhantumile Mwana gwabho bhayene, ali na shiilu malinga sha bhaatendanga yambi. Kwa nneyo gubhaiukumwile mboteko yambi nshiilu shakwe.
4 ndi cholinga chakuti chilungamo chofunikira cha lamulo chikwaniritsidwe kwathunthu mwa ife amene sitikhala monga mwachikhalidwe chathu cha uchimo koma mwa Mzimu.
A Nnungu gubhatendile nnei nkupinga indu yowe ya mmbone ipinjikwa na shalia itimilile nkati jetu, uwe tukaakagulila ilokoli yangali ya mmbone ya nshiilu, ikabhe ya Mmbumu.
5 Pakuti anthu amene amakhala monga mwa makhalidwe oyipa a thupi amayika malingaliro awo pa zinthu zathupi. Koma amene amakhala monga mwa Mzimu amayika malingaliro awo pa zinthu za Mzimu.
Pabha bhandunji bhaakagulilanga ilokoli yangali ya mmbone ipinjikwa na shiilu, ibhaganishiyanga ilokoli yangali ya mmbone ipinjikwa na shiilu, ikabheje bhaakagulilanga indu ipinjikwa naka Mbumu jwa Ukonjelo, ibhaganishiyanga indu ipinjikwa naka Mbumujo.
6 Kuyika mtima pa zathupi ndi imfa koma kuyika mtima pa za Mzimu ndi moyo ndi mtendere.
Pabha ndumbililo ya shiilu inapeleshela shiwo, ikabhe ndumbililo ika Mbumu jwa Ukonjelo, inapeleshela gumi na ulele.
7 Pakuti mtima umene wakhazikika pa zathupi ndi wodana ndi Mulungu. Sunagonjere lamulo la Mulungu ndipo sungathe kutero.
Na ndumbililo ya shiilu ni kubhika magongo na a Nnungu, pabha shikapinga kukunda shalia ja a Nnungu, na wala shikakombola kukunda shaliajo.
8 Ndipo anthu amene amalamulidwa ndi khalidwe lauchimo sangathe kukondweretsa Mulungu.
Bhene bhaakagulilanga ilokoli ya nshiilu, nngakombola kwaanonyeya a Nnungu.
9 Koma inu simulamulidwanso ndi khalidwe lanu lauchimo koma ndi Mzimu ngati Mzimu wa Mulungu akhaladi mwa inu. Koma ngati munthu aliyense alibe Mzimu wa Khristu, iyeyu si wa Khristu.
Monaga Mbumu jwa a Nnungu anatama nkati jenunji, mmanganya nkaakagulilanga ilokoli yangali ya mmbone ipinjikwa na shiilu, ikabhe shinkagulilanje ya mmbone ipinjikwa naka Mbumu. Ikabheje mundu jwangali Mbumu jwa a Kilishitu, jwenejo nngabha jwabho.
10 Ndipo ngati Khristu ali mwa inu, thupi lanu ndi lakufa chifukwa cha uchimo, koma mzimu wanu ndi wamoyo chifukwa cha chilungamo.
Ikabheje a Kilishitu bhabhaga nkati jenunji, shiilu shenunji shinawa kwa ligongo lya yambi, ikabhe mbumu jwenunji jwankoto kwa ligongo lya aki.
11 Ndipo ngati Mzimu wa Mulungu amene anaukitsa Yesu kwa akufa akhala mwa inu, Iyeyo amene anaukitsa Khristu kwa akufa adzapatsanso moyo matupi anu amene amafa kudzera mwa Mzimu wake amene amakhala mwa inu.
Na monaga Mbumu jwa a Nnungu abhayushiye a Kilishitu bhakaweje, shaiyuye na iilu yenunji ili yawa, kwa mashili gaka Mbumu jwabho atama nkati jenunji.
12 Kotero abale, ife tili ndi zoti tikwaniritse, koma osati za khalidwe lathu lauchimo, kumachita zofuna zake.
Bhai monaga ni nneyo, ashaalongo ajangu tukwete ligambo, ikabheje nngabha lya tenda indu ya nshiilu.
13 Pakuti ngati inu mukhala monga mwa khalidwe lauchimo, mudzafa. Koma ngati mwa Mzimu mupha ntchito zoyipa zathupi, mudzakhala ndi moyo.
Ibhaga, ntamanganaga nkukagulila indu yangali ya mmbone ya nshiilu, kweli shinng'wanganje, ikabheje muibhulagangaga indu yangali ya mmbone ya nshiilu kwa Mbumu jwa Ukonjelo, shinnamanje.
14 Onse amene amatsogozedwa ndi Mzimu wa Mulungu ndi ana a Mulungu.
Pabha bhowe bhaalongoywanga naka Mbumu jwa a Nnungu, bhenebho ni bhana bha a Nnungu.
15 Mzimu amene inu munalandira samakusandutsani akapolo, kuti muzikhalanso amantha, koma Mzimu amakusandutsani ana. Ndipo mwa Iye ife timafuwula kuti, “Abba, Atate.”
Pabha mwangaposhelanga mbumu jwa utumwa akuntendanga nkolanje bhoga, ikabheje mposhelenje Mbumu akuntendanga mmanganje bhana bha a Nnungu, na kwa mashili gaka jwenejo, uwe tunakwaashema a Nnungu, “Atati.”
16 Mzimu mwini amavomerezana ndi mzimu wathu kuti ife ndife ana a Mulungu.
Numbe Mbumu jwa a Nnungu nnyene anakong'ondela pamo na mitima jetu, kuti uwe ni bhana bha a Nnungu.
17 Tsono ngati tili ana ake, ndiye kuti ndife olowa mʼmalo a Mulungu ndi olowa mʼmalo pamodzi ndi Khristu. Ngati ife timva zowawa pamodzi ndi Khristu, tidzalandiranso ndi ulemerero womwe pamodzi naye.
Ibhaga uwe ni bhana bha a Nnungu, bhai uwe ni tubhalishi bha a Nnungu bhaalishinji pamo na a Kilishitu. Tunabha tubhalishi putupata mboteko pamo na bhenebho, nkupinga nneila peila, tukuywe pamo na bhenebho.
18 Ine ndiganiza kuti masautso amene tikuwamva nthawi ino, sakufanana ndi ulemerero umene udzaonetsedwa mwa ife.
Shingubhona nne, mboteko yetu ya nnaino nngabha shindu, kupunda ukonjelo upinga bhoneka kwetu uwe.
19 Pakuti chilengedwe chikudikira ndi chiyembekezo kuonetsedwa poyera kwa ana a Mulungu.
Na nkali indu yowe ipengenywe, inalinda kwa lilaka lya kaje, kumanyika kwa bhana bha a Nnungu.
20 Pakuti chilengedwe sichinasankhe kugonjera zopanda pake, koma mwachifuniro cha Iye amene analola kuti chigonjere. Koma chili ndi chiyembekezo
Indu yowe ipengenywe gwiijonaishe, nngabha kwa pinga iyene, ikabhe kwa pinga kwabho bhayene bhaibhishile kwa ngulupai,
21 chakuti chidzamasulidwa ku ukapolo wa chivundi ndi kulandiranso ufulu ndi ulemerero wa ana a Mulungu.
mbena indu ipengenywe na yalakwe shiitapulwe, nishoywa muutumwa gwa angabhanika, ijinjile muungwana uli na ukonjelo gwa bhana bha a Nnungu.
22 Ife tikudziwa kuti chilengedwe chonse chakhala chikubuwula ndi ululu ngati ululu wa nthawi yobereka mwana mpaka tsopano lino.
Pabha tumumanyi kuti mpaka nnaino, indu yowe ipengenywe inabhubhulila pamo malinga mboteko ya nkukola mwana.
23 Si zokhazo ayi, ngakhale ife tomwe, amene tili ndi zipatso zoyamba za Mzimu, tikubuwulira mʼkati mwathu pomwe tikudikira mwachidwi kusankhidwa kwathu ngati ana, kuwomboledwa kwa matupi athu.
Numbe nngabha indu ipengenywe peyo, ikabhe nkali uwe tupatile Mbumu jwa Ukonjelo, ali nnimbu jwa upo ibhapinga kutupa a Nnungu, numbe tunabhubhulila mmunda jetu, tulilolela kutendwa bhana bha a Nnungu, yani na kugombolwa kwa iilu yetu.
24 Pakuti ife tinapulumutsidwa mʼchiyembekezo ichi. Koma chiyembekezo chimene chimaoneka si chiyembekezo ayi. Kodi ndani amene amayembekezera chimene ali nacho kale?
Pabha tushitapulwa nkupinga tutame nkukulupalila, ikabheje shutwashilolelaga shila shibhonekaga, penepo kwakwapi kulolela kabhili. Pabha gani akushilolela shindu sha kushibhona?
25 Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.
Ikabhe putukushilolela shindu shitukakushibhona, tunakushilinda kwa kwiipililila.
26 Momwemonso, Mzimu amatithandiza ife mʼkufowoka kwathu. Ife sitidziwa momwe tiyenera kupempherera koma Mzimu mwini amatipempherera mobuwula ndi mawu osafotokozedwa.
Nneyo peyo na Mbumu jwa Ukonjelo anakutujangutila muungakombola gwetu, pabha tukaamanya kujuga malinga shiikupinjikwa, ikabheje Mbumu jwa Ukonjelo nnyene anakutujujila kwa bhubhula kwa ngakomboleka kutaya.
27 Koma Iye amene amasanthula mitima yathu amadziwa maganizo a Mzimu, chifukwa Mzimu amapempherera oyera mtima molingana ndi chifuniro cha Mulungu.
Na bhene bhaulumila mmitima, bhaimanyi ng'aniyo ika Mbumu, pabha anakwaajujilanga bhandunji bha ukonjelo, malinga shibhaapinga a Nnungu.
28 Ndipo ife tikudziwa kuti zinthu zonse zimathandizana kuwachitira ubwino amene amakonda Mulungu, amene anayitanidwa monga mwa cholinga chake.
Na uwe tumumanyi kuti, indu yowe inatenda liengo pamo kwa pwaida ja bhakwaapinganga a Nnungu, yani bhashemilwenje kwa tumbilila kwabho, nkwaapanganga ya mmbone.
29 Pakuti amene Mulungu anawadziwiratu, anawasankhiratunso kuti akonzedwe mʼchifanizo cha Mwana wake, kuti Iye akhale Mwana woyamba kubadwa mwa abale ambiri.
Pabha bhene bhanganyabho bhamanyikenje na a Nnungu kuumila ndandubho, bhashinkwaagulanga bhalandanywanje naka Mwana gwabho, nkupinga abhe lielo munkumbi gwa bhana bhabhagwinji.
30 Iwo amene anawasankhiratu, anawayitananso. Amene Iye anawayitana anawalungamitsanso ndipo amene anawalungamitsa anawapatsanso ulemerero.
Na bhene bhubhaagwilenje kuumila kundandubho, gubhaashemilenje, na bhene bhashemilwenjebho, gubhabhalanganishiwenje aki, na bhabhalanganishiwenje akibho, nigubhaakushiyenje.
31 Nanga tsono tidzanena chiyani pa izi? Ngati Mulungu ali mbali yathu, adzatitsutsa ife ndani?
Igala tubhelekete nndi? Monaga a Nnungu bhabhaga na uwe, gani shaakombole kututauka?
32 Iye amene sanatimane Mwana wake wa Iye yekha, koma anamupereka chifukwa cha ife tonse. Iye adzalekeranjinso pamodzi naye kutipatsa ife zinthu zonse mwaulere?
Ibhaga a Nnungu bhanganneshelela nkali Mwana gwabho bhayene, ikabhe gubhanshoshiye kwa ligongo lya tubhowe uwe, bhai shibhalepele bhuli nkali kutupa shoshowe shina pamo naka jwenejo?
33 Ndani amene adzabweretsa mlandu kutsutsa amene Mulungu anawasankha? Ndi Mulungu amene amalungamitsa.
Gani shabhashitakiyanje bhaagwilwenje na a Nnungu? A Nnungu bhayene bhaabhalanganishiyenje aki.
34 Ndani amene angatipeze ife olakwa? Palibe. Khristu Yesu amene anafa, kuposera pamenepo, amene anaukitsidwa ndi moyo, amene ali kudzanja lamanja la Mulungu ndiye amene akutipempherera.
Gani shabhaukumulanje mboteko? Jwakwa, a Yeshu Kilishitu ni bhawile, na bhayushile, numbe kubhali kunkono nnilo gwa a Nnungu, numbe bhanakutujujila.
35 Ndani amene adzatilekanitsa ife ndi chikondi cha Khristu? Kodi ndi masautso, kapena zowawa, kapena mazunzo, kapena njala, kapena umaliseche, kapena choopsa, kapena lupanga?
Gani shatulekanye na pingana kwetu na a Kilishitu? Nndi, shilaje eu mboteko eu shibhanga eu ukunu eu ya jogoya eu upanga?
36 Monga kwalembedwa: “Chifukwa cha inu, ife tikuphedwa tsiku lonse: ife tikutengedwa ngati nkhosa zoti zikaphedwe.”
Malinga shigalugula Majandiko ga Ukonjelo kuti, “Kwa ligongo lyenu tunabhulagwa na shiwo, mobha gowe. Tunaatendwa mbuti ngondolo ya ingwa.”
37 Ayi, mu zonsezi ife ndife oposa agonjetsi mwa Iye amene anatikonda.
Ikabheje na yene indu yoweyo uwe tunakombola kwa kaje, kwa mashili ga bhene bhatupinjile bhala.
38 Pakuti ine ndatsimikiza ndi mtima wonse kuti ngakhale imfa, kapena moyo, ngakhale angelo, kapena ziwanda, ngakhale zinthu zilipo, kapena zili mʼtsogolo, kapena mphamvu zina,
Pabha nimumanyi kaje kuti, wala shiwo, na wala gumi, na wala ashimalaika eu ashimaoka, na wala indu ipali, na wala indu shiipagwe, na wala mashili gogowe,
39 ngakhale kutalika, kapena kuya, kapena chilichonse mʼchilengedwe chonse, sizingathe kutisiyanitsa ndi chikondi cha Mulungu chimene chili mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
gali kunani, na wala gali pai, na wala shindu shipengenywe shoshowe, shishikombole kutushoya nkupingwa na a Nnungu, kupitila kwa a Yeshu Kilishitu Bhakulungwa bhetu.