< Aroma 6 >
1 Nanga tinene chiyani? Kodi tipitirire kuchimwa kuti chisomo chichulukebe?
Bhai tujile bhuli? Tupunde kutenda yambi, nkupinga nema ja a Nnungu jipunde jenjesheka?
2 Ayi. Mʼnjira iliyonse! Popeza tinafa ku tchimo, nanga tidzapitirira bwanji kukhalabe mʼmenemo?
Ng'oo, wala kashoko! Uwe ga yambi iilu yetu iiwilile, shitupunde bhuli kabhili kutama na yambi?
3 Kodi simukudziwa kuti tonse amene tinabatizidwa mwa Khristu Yesu tinabatizidwa mu imfa yake?
Eu, nkakumumanyanga kuti uwe tubhatishwe na lundana na a Yeshu Kilishitu, nneila peila tushilundanywa nshiwo shabho?
4 Chifukwa chake ife tinayikidwa mʼmanda pamodzi ndi Iye mwa ubatizo. Tinalowa mu imfa ndi cholinga choti monga momwe Khristu anaukitsidwa kwa akufa ndi ulemerero wa Atate, ifenso tikakhale mʼmoyo watsopano.
Bhai putwabhatishwe twashinkulundana nabho, gutushishilwe pamo na bhenebho, nkupinga malinga a Kilishitu pubhayushiywe kwa ukonjelo gwa Atati, nneyo peyo na uwe tutame nndamo ja ambi.
5 Pakuti ngati ife tinakhala amodzi ndi Iye mu imfa yake, tidzakhalanso ndithu amodzi ndi Iye mu kuuka kwake.
Pabha, malinga shitulundene nabho nkuwa malinga bhenebho, nneyo peyo shitulundane nabho kwa yuka, malinga bhenebho.
6 Ife tikudziwa kuti umunthu wathu wakale unapachikidwa pamodzi ndi Iye kuti thupi la uchimo likhale lopanda mphamvu ndi kuti tisakakhalenso akapolo a tchimo
Tumumanyi kuti nkubho gwetu gwa bhukala gwa tenda yambi, gwashinkukomelwa munshalabha pamo na bhenebho, nkupinga tunapunde kubha bhatumwa bha yambi, nkupinga maisha getu ga bhukala ga shambi gapele.
7 chifukwa aliyense amene anafa anamasuka ku tchimo.
Pabha aiwilile ga yambi, ashitendwa nngwana niembuywa na yambi.
8 Koma ngati tinafa pamodzi ndi Khristu, tikhulupirira kuti tidzakhalanso ndi moyo pamodzi ndi Iye.
Bhai monaga tuwile pamo na a Kilishitu, tunakulupalila kuti, shitutame pamo na bhenebho.
9 Pakuti tikudziwa kuti popeza Khristu anaukitsidwa kwa akufa, Iye sangafenso. Imfa ilibenso mphamvu pa Iye.
Pabha tumumanyi kuti a Kilishitu bhakayusheje, bhakawa kabhili.
10 Imfa imene Iye anafa, anafa ku tchimo kamodzi kokha, koma moyo umene akhala ndi wa kwa Mulungu.
Pabha kuwa kwabho kula, bhashinkuwila yambi kamope, na nnaino tama kwabho, bhanatama pamo na a Nnungu.
11 Kotero inunso, mudzione nokha ngati akufa ku tchimo koma a moyo kwa Mulungu mwa Khristu Yesu.
Nneyo peyo na mmanganyanji mwiibhikanje mbuti bhaiwililenje bhakaatendanga yambi, ikabhe bhabhakotonji kwa lundana na a Nnungu kupitila a Yeshu Kilishitu.
12 Nʼchifukwa chake, musalole tchimo lilamulire matupi anu amene anafa kuti mumvere zilakolako zonyansa.
Bhai yambi inatagwale iilu yenunji ya wai, mpaka nikagula ilokoli yakwe.
13 Musapereke ziwalo zathupi lanu ku tchimo, ngati zipangizo zamakhalidwe oyipa. Mʼmalo mwake, mudzipereke kwa Mulungu, ngati amene achoka ku imfa kupita ku moyo. Ndipo mupereke ziwalo zathupi lanu ngati zipangizo zachilungamo.
Wala nnalekanje iilu yenunji kutenda yambi, ikabhe mwiishoyanje kwa a Nnungu malinga bhandu bhayushilenje, mwiishoyanje kwa a Nnungu kwa itendi ya aki.
14 Tchimo silidzakhalanso ndi mphamvu pa inu, chifukwa Malamulo sakulamulira moyo wanu koma chisomo.
Numbe yambi ikantagwalanga kabhili, pabha munninginji nngabha nkulongoywa na shalia ja a Musha, ikabhe kwa nema ja a Nnungu.
15 Nʼchiyani tsono? Kodi tidzichimwa chifukwa sitikulamulidwa ndi Malamulo koma chisomo? Ayi. Mʼnjira iliyonse ayi!
Bhai, tujile bhuli? Tutende yambi pabha tukaukumulwa na shalia ja a Musha, ikabhe kwa nema? Ng'oo!
16 Kodi inu simudziwa kuti pamene mudzipereka kwa wina wake, kumumvera ngati akapolo, ndinu akapolo a amene mumumvera? Ngati ndinu akapolo a tchimo mudzafa. Koma ngati ndinu akapolo akumvera, mudzakhala olungama pamaso pake.
Bhuli nkakumumanyanga kuti, punkwiibhikanga malinga utumwa kuka mundu nikunkunda, mmangangaga bhatumwa bha yambi mpelo gwake ni kuwa, mmangangaga bhatumwa bha kwaakunda a Nnungu, mpelo gwakwe aki.
17 Koma ayamikidwe Mulungu pakuti ngakhale munali akapolo a tchimo, munamvera ndi mtima wonse chiphunzitso chimene munalandira.
Ikabheje bhatendelwe eja a Nnungu, nkali mwalinginji bhatumwa bha yambi, nshikundanga kwa mitima jenunji jowe majiganyo gumwajigenywenje.
18 Inu munamasulidwa ku tchimo ndipo tsopano mwasanduka akapolo achilungamo.
Gunngombolwenje kopoka kuutumwa gwa yambi, nibhanganga bhatumwa bha aki.
19 Ine ndikufanizira zinthu za tsiku ndi tsiku chifukwa chikhalidwe chanu nʼchofowoka. Monga momwe munkapereka ziwalo za matupi kukhala akapolo a zonyansa ndi makhalidwe oyipa, zimene zimanka zichulukirabe, choncho tsopano dziperekeni ziwalozo kuti zikhale akapolo achilungamo ndi a kuyera mtima.
Ngunabheleketa shigundu kwa ligongo lya ungashimilika gwenunji. Malinga shimwaishoshiyenje ibhalo yenunji muitendi ya utumwa na ya nyata na yambi gumwinyatiyenje, nneyo peyo, nnaino mwiishoyanje ibhalo yenunji muutumwa gwa tenda aki muukonjelo.
20 Pomwe munali akapolo atchimo, simunkalabadira za chilungamo.
Pumwalinginji bhatumwa bha yambi, aki jikantagwalangaga.
21 Kodi munapeza phindu lanji pochita zinthu zimenezi, zomwe tsopano mukuchita nazo manyazi? Zinthu zimenezo zotsatira zake ndi imfa!
Mwapatilenjeje nndi, kwa itendi yenunji ya bhukala inkwiibhonelanga oni nnaino? Pabha mpelo gwa yeneyo kuwa.
22 Koma tsopano pakuti inu mwamasulidwa ku tchimo ndipo mwasanduka akapolo a Mulungu, phindu lomwe mulipeza ndi kuyera mtima ndipo chotsatira chake ndi moyo wosatha. (aiōnios )
Ikabheje nnaino, nngombolwenje kopoka kuutumwa gwa yambi, nitendwa bhatumwa bha a Nnungu, nkwetenje pwaida ja ukonjelo, na mpelo gwakwe gumi gwa pitipiti. (aiōnios )
23 Pakuti malipiro a tchimo ndi imfa, koma mphatso yaulere imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha mwa Khristu Yesu Ambuye athu. (aiōnios )
Pabha nshaala gwa yambi kuwa, ikabheje upo ibhashoya a Nnungu, gumi gwa pitipiti nkulundana na a Yeshu Kilishitu, Bhakulungwa bhetu. (aiōnios )