< Chivumbulutso 3 >

1 “Lembera mngelo wampingo wa ku Sarde kuti: Awa ndi mawu ochokera kwa amene amasunga mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu ndi nyenyezi zisanu ndi ziwiri. Iye akuti: Ndimadziwa ntchito zako; umadziwika kuti ndiwe wamoyo koma ndiwe wakufa.
“Udu kiti nnan kadura Kutelle kutyi nliran in Sardisu: 'Tigbulang nlenge na amere min ti Ruhu kuzor nin niyini kuzor nyiru ile imon na usu udin nfo figiri uu fe dinin nlai, bara nani fe unan kulari.
2 Dzuka! Limbitsa zimene zatsalira zomwe zatsala pangʼono kufa, pakuti ndaona kuti ntchito zako nʼzosakwanira pamaso pa Mulungu.
Fita ukpin agang kiti nile imon na ilawa, idaduru ukuu, bara na nyene katwa fe kulun nanya nyenju kutelle nighe ba.
3 Choncho, kumbukira zimene unalandira ndi kumva; uzisunge ndipo ulape. Koma ngati sudzuka, ndidzabwera ngati mbala ndipo sudzadziwa nthawi imene ndidzabwere kwanu.
Bara nan lizino, ile imon na usere uminin lanza. Dofino inin, udiu kutyin. Meng ba dak nafo ukiri na uba yinnu kubi ko na nba dak kitife ba.
4 Komabe uli ndi anthu angapo mu Sarde amene sanadetse zovala zawo. Amenewa adzayenda ndi Ine atavala zoyera popeza ndi oyenera kutero.
Ama tisa namong duk cinglin nan nya Sardisu alenge na ita imon mine indinong ba. Inung ba cinu nan mi, nin kuyok nimon iboo, bara idi dert.
5 Amene adzapambane adzavala zoyera ngati ena aja. Sindidzafafaniza dzina lake mʼbuku lamoyo, koma ndidzamuchitira umboni pamaso pa Atate anga ndi angelo ake.
Ulenge na ase unasara iba shonghe kulutuk kuboo, tutun na mba wesu lisa mye nanya kaffa nlai ba, mba bellu lisa mye nbun ncif nighe nin nbun nanan kadura mye.
6 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.”
Andi udinin natuf, lanza ile imon na uruhu din bellu nilarin nliran.”
7 “Lembera mngelo wampingo wa ku Filadefiya kuti: Awa ndi mawu ochokera kwa amene ndi woyera ndi woonadi, amene ali ndi kiyi ya Davide. Iye akatsekula palibe amene angatseke; ndipo akatseka palibe amene angatsekule.
Udu kiti nnan kadura in Filidelfiya, Tigbulang nlenge na adi lau nin kidegen, ame min imon npunu kitin Dauda, asa apuno, na umon wasa atursu ba, asa a tursu na umonn wasa apuno ba.
8 Iye akuti, ‘Ine ndimadziwa ntchito zako. Taona, ndakutsekulira pa khomo ndipo palibe wina amene angatseke. Ndikudziwa kuti uli ndi mphamvu zochepa komabe wasunga mawu anga ndipo sunandikane.
Meng yiru imon ile na usu, yene, ubunfe kibulun duku ka na upuno, na umon wasa atursu ba, nyiru likara fe di baat, nin nani udin dortu tigbulang nighe, tutun na uta amusu lisa nighe ba.
9 Amene ndi mpingo wa Satana, amene amadzitcha kuti ndi Ayuda pamene sali choncho, koma ndi onama, ndidzawabweretsa kwa inu ndi kuwagwetsa pansi pa mapazi anu kuti adzazindikire kuti ndimakukondani.
Su ucaa! Alenge na idi anan kutyi nlira shetan, alenge na idin su inug a Yahudawari, ana nanere ba-idin su kinuwari nani, nba ti nani ida tumun nbun nabunu fe, iba da yinnu au meng dinin su fe.
10 Popeza mwasunga mawu anga woti mupirire ndipo mwawugwira mtima, Inenso ndidzakupulumutsani nthawi ya mayesero imene idzabwera pa dziko lonse lapansi kuyesa onse okhala pa dziko lapansi.
Tunda na una ceo uduka nighe, utere kibinai nin hankuri, mba minfi kubi kongo na iba dumunfi, na ku ba dak vat inye, iba dumunu alenge na isosin nan nyya inye.
11 Ine ndikubwera msanga. Gwiritsitsa chimene uli nacho kuti wina angakulande chipewa chako chaufumu.
Meng din cinu deddei. Minno ile imon na udumun gangang bara na umong wa bullu litapa fe ba.
12 Iye amene adzapambane ndidzamusandutsa mzati wa mʼNyumba ya Mulungu wanga. Sadzatulukamonso. Pa iye ndidzalemba dzina la Mulungu wanga ndi dzina la mzinda wa Mulungu wanga, Yerusalemu watsopano, umene ukubwera pansi kuchokera kumwamba kwa Mulungu wanga; ndipo pa iye ndidzalembanso dzina langa latsopano.
Meng ba ti ulenge na ase unasara aso litino nanya kilari nliran Kutelle, na aba nuzu nanye ba, nba nyertin ghe lisa Kutelle nighe, lisa kipin Kutelle (Urushalima upese ule na utolo unuzu kitene kani kiti Kutelle), nin lisa lipese nighe.
13 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.’”
Ame ulenge na adumun natuf, na alanza ile unon na Uruhu din belle niliran nlirag.'
14 “Lembera mngelo wampingo wa ku Laodikaya kuti: Awa ndi mawu ochokera kwa Ameni, mboni yokhulupirika ndi yoona, gwero la zolengedwa zonse za Mulungu.
“Nyerte Udu kiti nanan kadura kilari nliran nanya in Lawudikiya: 'Tigbulang uso nani, iyizi nba in kidegen udya nanya makeke Kutelle.
15 Ine ndimadziwa ntchito zako, kuti sindiwe wozizira kapena wotentha. Ndikanakonda ukanakhala wozizira kapena wotentha!
Meng yiru ile imon na udin su, nafe di cancam ba, ana udin npiu ba, ndi nyenju nafo uwadi cancam sa npiu!
16 Tsono popeza ndiwe wofunda chabe, sindiwe wotentha kapena wozizira, ndatsala pangʼono kuti ndikulavule mʼkamwa mwanga.
Nani, bara na udi bidibidi-na udi cancam ba ana udin piu ba-Meng ba tuffunfi nanya nnuu nighe.
17 Iwe umati: ‘Ndine wolemera, ndine wachuma ndipo sindisowa kanthu.’ Koma sudziwa kuti ndiwe wovutika, womvetsa chisoni, waumphawi, wosaona ndi wamaliseche.
Bara fe nworo, “Meng dimun nimon nacara, na ndira imomon ba.” Anafe yiru fere di ba fere di hem, unan kunekune, ukimon, uduu, nin lenge na adi fisere.
18 Ndikukulangiza kuti ugule kwa Ine golide woyengedwa ndi moto kuti ukhale wolemera. Ugule zovala zoyera kuti uvale ndi kuphimba umaliseche wako wochititsa manyaziwo. Ndiponso ugule kwa Ine mankhwala a mʼmaso kuti uwone.
Lanza ushawara nighe: Sere azurfa kiti nighe, alle na ina dumun anin kiti nlah, bara unan so unan nimon nacara, nin njinjin, nin kulutuk kulau, ishon bara iwa yenefi fisere ulanza ncin, a ukan uti niyizife unan yene kiti.
19 Amene ndimawakonda ndimawadzudzula ndi kuwalanga. Choncho chita changu ndipo lapa.
Vat nlenge na ndinin su mye, asa ntaghe libau ndursuzoghe inda na aba su lisosin, bara nani, ta dedei udiu kutyin.
20 Taonani ndayima pa khomo ndikugogoda. Ngati wina amva mawu anga natsekula chitseko, Ine ndidzalowamo ndi kudya naye, Ine ndi iyeyo.
Yene, Meng yisin kibulun ndi fowe, asa umon nlanza liwui nighe apuno kibulughe, Meng ba dak nan nya kilari mye, nba lii umonli nighe nighe, amye nin nmi.
21 Amene adzapambana, ndidzamupatsa ufulu wokhala nane pamodzi pa mpando wanga waufumu monga mmene Ine ndinapambana ndi kukhala pansi ndi Atate anga pa mpando wawo waufumu.
Ulenge na ase unasara, Meng ba yinin ghe aso nin mye, kuteet tigo nighe, nafo na Meng nasu unasara nmini sosin nin ncif nighe kuteet tigoo mye.
22 Amene ali ndi makutu, amve zimene Mzimu akuwuza mipingo.”
Andi udinin natuf, lanza ile imon na uruhu din bellu nilari nlira.”

< Chivumbulutso 3 >