< Chivumbulutso 22 +
1 Ndipo mngeloyo anandionetsa mtsinje wamadzi amoyo, oyera ngati mwala wa krustalo ukutuluka ku mpando waufumu wa Mulungu ndi wa Mwana Wankhosa,
Penepo Malaika jula, gwanangwile lushi lwa mashi ga mabhutuka, gakwete gumi, ga konja galikoposhela pa shitengu sha ukulungwa sha a Nnungu, na Mwana Ngondolo.
2 Ukuyenda pakati pa msewu waukulu wa mu mzindawo. Mbali iliyonse ya mtsinjewo kunali mtengo wamoyo, utabala zipatso khumi ndi ziwiri. Kubereka zipatso mwezi uliwonse. Ndipo masamba a mtengowo ndi mankhwala wochiritsa anthu a mitundu ina.
Lwene lushilo lwatendaga bhutuka pakatipakati mpanda njindo, gwa shene shilambo shila. Nnyenje lwene lushilo, gwashinkupagwa nkongo gwa gumi kila ng'ambu ja lushi. Gwene nkongogo gwatendaga ogola iepo ya namna likumi limo na ibhili, iepo yakwe yatendaga ogola kila mwei. Na maamba ga gwene nkongogo pugaliji ni ntela gwa lamia bhandunji bha ilambo ina.
3 Sipadzakhalanso temberero lililonse. Mpando waufumu wa Mulungu ndi wa Mwana Wankhosa udzakhala mu mzindawo, ndipo atumiki ake adzamutumikira.
Pene pa shilambopo shikapagwa kabhili shindu shoshowe shiloshilwe, pabha shitengu sha ukulungwa gwa a Nnungu na Mwana Ngondolo shishipagwe mwenemo na bhatumishi bhabho, bhalikwaatindibhalilanga maengo.
4 Iwo adzaona nkhope yake ndipo dzina lake lidzalembedwa pa mphumi zawo.
Na bhalabhonji shibhalubhonanje lubhombo lwabho, numbe lina lyabho shilibhe pa shenyi pa lubhombo lwabhonji.
5 Sipadzakhalanso usiku. Sadzafuna kuwala kwa nyale kapena kwa dzuwa pakuti Ambuye Mulungu adzakhala kuwala kwawo. Ndipo adzalamulira kwamuyaya. (aiōn )
Shilo shikapagwa kabhili, wala bhakapinganga shilangaya sha kandili eu sha lyubha, pabha Bhakulungwa a Nnungu shibhabhe shilangaya shabhonji, na bhene bhanganyabho shibhatagwalanje pitipiti na pitipiti. (aiōn )
6 Mngeloyo anandiwuza kuti, “Mawu awa ndi okhulupirika ndi owona. Ambuye Mulungu wa mizimu ya aneneri anatumiza mngelo wake kudzaonetsa atumiki ake zinthu zimene ziyenera kuchitika posachedwapa.”
Numbe jwene malaika jula nigwanugulile, “Gegano malobhe gano ni gaakulupalika kaje na ga kweli. Bhakulungwa a Nnungu bhakwaapanganga a ashinkulondola Mbumu jwabho, bhashinkutuma malaika jwabho, kukwaalanguyanga bhatumishi babho gene gapinga koposhela shangupe gala.”
7 “Taonani, ndikubwera posachedwa! Wodala ndi amene asunga mawu oneneratu za kutsogolo a mʼbuku ili.”
Nnole, ngwiyajo nnainope, apatile mboka jwene akunda malobhe ga ukulondola ga sheshino shitabhu shino.
8 Ine Yohane, ndine amene ndinamva ndi kuona zinthu izi. Ndipo pamene ndinamva ndi kuona izi ndinagwa pansi kuti ndipembedze mngelo amene amandionetsa zimenezi.
Nne a Yowana ni napilikene na kugabhona gegano. Na nne ngagabhoneje na kugapilikana, ngugwaga pai nkupinga nintindibhalile pa makongono, jwene malaika anangwiye genego.
9 Koma mngeloyo anandiwuza kuti, “Usatero ayi! Ine ndine wotumikira monga iwe pamodzi ndi abale ako aneneri ndi onse amene amasunga mawu a mʼbuku pembedzani Mulungu.”
Ikabheje jwenejo nigwanugulile, “Nnatende nneyo, nne ni ntumishi malinga mmwe, na bhaakulupalila ajenunji ashinkulondola, na bhowe bhaakundanga malobhe ga sheshino shitabhu shino. Mwaatindibhalile a Nnungu.”
10 Kenaka anandiwuza kuti, “Usabise mawu onena zamʼtsogolo a mʼbuku ili chifukwa nthawi yayandikira.
Numbe gwanugulile, “Nnaiye malobhe ga ukulondola gali amuno nshitabhu muno, pabha malanga gabhandishile ga koposhela kwa genega.
11 Wochita zoyipa apitirire kuchita zoyipazo; wochita zonyansa apitirire kuchita zonyansazo; wochita zabwino apitirire kuchita zabwinozo; ndipo woyera mtima apitirire kukhala woyera mtima.”
Atenda yangali ya mmbone, apunde kutenda yangali ya mmbone, na akwiinyatiya, apunde kwiinyatiya. Atenda ya mmbone, na apunde kutenda ya mmbone, na ali jwa ukonjelo, apunde kubha jwa ukonjelo.”
12 “Taonani, ndikubwera posachedwa! Ndikubwera ndi mphotho zanga kuti ndidzapereke kwa aliyense malinga ndi zimene anachita.
A Yeshu bhakuti, “Nnole! Ngwiyajo nnainope, shinimpe mundu upo, ilingana na itendi yakwe.
13 Ine ndine Alefa ndi Omega, Woyamba ndi Wotsiriza, Chiyambi ndi Chimaliziro ndine.
Nne ni Alpha na Omega, yani, Nantando na Mpelo.”
14 “Odala amene achapa mikanjo yawo, kuti akhale ndi ufulu wopita ku mtengo wamoyo ndi kuti akalowe mʼzipata za mu mzindawo.
Mbaya bhene bhaashapanga nngubho yabhonji, nkupinga bhakolanje aki ja jinjila nshilambo kupitila mmilango, na bhakolanje aki ja lya iepo, ya nkongo gwa gumi.
15 Kunja kuli agalu, amatsenga, achiwerewere, akupha anthu, opembedza mafano ndi aliyense amene amakonda bodza ndi kulichita.
Ikabheje palanga bhapalinji, mmbwa, na bhaabhi, na bha labhalabha, na bha bhulaga, na bha tindibhalila yanamu, na bhowe bha pinganga kubheleketa unami, bhakajinjilanga mwenemo.
16 “Ine Yesu, ndatuma mngelo wanga kuti achitire umboni uwu ku mipingo. Ine ndine Muzu ndi Chipatso cha Davide ndipo ndine Nthanda Yonyezimira.”
“Nne, a Yeshu, njikuntuma malaika jwangu ankong'ondelanje gegano mmakanisha. Nne ni jwa lubheleko lwa shipinga sha a Daudi. Nne ni lutondwa lwa nng'andu luubhala!”
17 Mzimu Woyera ndi mkwatibwi akuti, “Bwerani!” Ndipo amene akumva anena kuti Bwerani! Iye amene ali ndi ludzu abwere, ndipo aliyense amene afuna alandire mphatso yaulere ya madzi amoyo.
Mbumu na a Mwali bhaalombwa, bhakutinji, “Nnjiye,” na kila mundu apilikana genega na abhelekete, “Nnjiye,” Akwete nnjotajo ajiye, na apingajo, apapile mashi ga gumi, gwayoyo.
18 Ndikuchenjeza aliyense amene akumva mawu onena zamʼtsogolo a mʼbukuli kuti, “Ngati wina awonjezerapo kalikonse, Mulungu adzamuwonjezera miliri imene yalembedwa mʼbuku ili.
Nne a Yowana ngunakwaaleyanga bhandu bhowe, bhaapilikananga malobhe ga ukulondola ga shene shitabhu shino. Mundu jojowe ajenjesheyaga shindu shoshowe, a Nnungu shibhannjenjesheye mambukute gajandikwe nshitabhu muno.
19 Ndipo wina akachotsapo mawu onena zamʼtsogolo a mʼbuku ili, Mulungu adzachotsa gawo lake pa mtengo wamoyo ndi la mu mzinda woyera zimene zanenedwa mʼbuku ili.”
Mundu jojowe apunguyaga shoshowe, mmalobhe ga ukulondola ga shene shitabhu shino, a Nnungu shibhampokonyole shipande shakwe sha nkongo gwa gumi, na shipande shakwe sha shilambo sha ukonjelo, malinga shiijandikwe nshitabhu muno.
20 Iye amene akuchitira umboni pa zinthu izi akuti, “Inde, Ine ndikubwera posachedwa.” Ameni. Bwerani Ambuye Yesu.
Na bhene bhaakong'ondela gegano bhakuti, “Kweli ngwiyajo nnainope!” Amina. Nnjiye Mmakulungwa a Yeshu.
21 Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi anthu onse. Ameni.
Ngunakumpinjilanga mmowe nema ja Bhakulungwa a Yeshu. Amina.