< Masalimo 87 >

1 Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
مزمور و سرود بنی قورح اساس او در کوههای مقدس است.۱
2 Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
خداوند دروازه های صهیون رادوست می‌دارد، بیشتر از جمیع مسکن های یعقوب.۲
3 Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
سخنهای مجید درباره تو گفته می‌شود، ای شهر خدا! سلاه.۳
4 “Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
رهب و بابل را ازشناسندگان خود ذکر خواهم کرد. اینک فلسطین و صور و حبش، این در آنجا متولد شده است.۴
5 Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
ودرباره صهیون گفته خواهد شد که این و آن در آن متولد شده‌اند. و خود حضرت اعلی آن را استوارخواهد نمود.۵
6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
خداوند چون امت‌ها رامی نویسد، ثبت خواهد کرد که این در آنجا متولدشده است، سلاه.۶
7 Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
مغنیان و رقص کنندگان نیز. جمیع چشمه های من در تو است.۷

< Masalimo 87 >