< Masalimo 76 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu. Mulungu amadziwika mu Yuda; dzina lake ndi lotchuka mu Israeli.
KOT me indand mau ren Iuda, o mar a me lingan ren men Israel.
2 Tenti yake ili mu Salemu, malo ake okhalamo mu Ziyoni.
Tanpas a im pwal mi nan Salem, o tanpas a mi Sion.
3 Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka, zishango ndi malupanga, zida zankhondo. (Sela)
I wasa a kotin katip pasang ia kanangan kasik katieu, o pere, o kodlas, o tatan mauin. (Sela)
4 Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.
Komui me lingan o manaman sang dol en mauin kan.
5 Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma, Iwowo amagona tulo tawo totsiriza; palibe mmodzi wamphamvu amene angatukule manja ake.
Me aklapalap akan lodier ong men kul akan o mela, o saunpei komad karos en kidi pa arail.
6 Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo, kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi.
Maing Kot en Iakop os o war kin pupekidi omui masan akan.
7 Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa. Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?
Komui meid kamasapwek. Is me kak u mo’mui ni omui ongiong?
8 Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo, ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete,
Ni omui kotin kasaledar omui kadeik sang nanlang, sappa ap masapwekadar o nenenlar,
9 pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze, kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko. (Sela)
Ni en Kot a kotidar, pwen kadeik, o sauasa me luet akan karos nin sappa. (Sela)
10 Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu.
Pwe makar en aramas kin kalinganada komui, o ma re pan pur ong moromorong, luan omui ongiong pan itar ong irail.
11 Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse; anthu onse omuzungulira abweretse mphatso kwa Iye amene ayenera kuopedwa.
Komail inau ong Ieowa omail Kot o kapwaiada. Komail karos, me mi impa, wa dong ren me kalom omail kisakis akan.
12 Iye amaswa mzimu wa olamulira; amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi.
I me pan atia sang saupeidi kan ar komad, a meid kalom ong nanmarki en sappa kan.