< Masalimo 136 >

1 Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
O give praise to the Lord, for he is good: for his mercy is unchanging for ever.
2 Yamikani Mulungu wa milungu.
O give praise to the God of gods: for his mercy is unchanging for ever.
3 Yamikani Ambuye wa ambuye,
O give praise to the Lord of lords: for his mercy is unchanging for ever.
4 Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
To him who only does great wonders: for his mercy is unchanging for ever.
5 Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
To him who by wisdom made the heavens: for his mercy is unchanging for ever.
6 Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
To him by whom the earth was stretched out over the waters: for his mercy is unchanging for ever.
7 Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
To him who made great lights: for his mercy is unchanging for ever.
8 Dzuwa lilamulire usana,
The sun to have rule by day: for his mercy is unchanging for ever.
9 Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
The moon and the stars to have rule by night: for his mercy is unchanging for ever.
10 Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
To him who put to death the first-fruits of Egypt: for his mercy is unchanging for ever:
11 Natulutsa Israeli pakati pawo,
And took out Israel from among them: for his mercy is unchanging for ever:
12 Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
With a strong hand and an outstretched arm: for his mercy is unchanging for ever.
13 Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
To him who made a way through the Red Sea: for his mercy is unchanging for ever:
14 Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
And let Israel go through it: for his mercy is unchanging for ever:
15 Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
By him Pharaoh and his army were overturned in the Red Sea: for his mercy is unchanging for ever.
16 Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
To him who took his people through the waste land: for his mercy is unchanging for ever.
17 Amene anakantha mafumu akuluakulu,
To him who overcame great kings: for his mercy is unchanging for ever:
18 Napha mafumu amphamvu,
And put noble kings to death: for his mercy is unchanging for ever:
19 Siloni mfumu ya Aamori,
Sihon, king of the Amorites: for his mercy is unchanging for ever:
20 Ogi mfumu ya Basani,
And Og, king of Bashan: for his mercy is unchanging for ever:
21 Napereka dziko lawo ngati cholowa,
And gave their land to his people for a heritage: for his mercy is unchanging for ever.
22 Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
Even a heritage for his servant Israel: for his mercy is unchanging for ever.
23 Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
Who kept us in mind when we were in trouble: for his mercy is unchanging for ever.
24 Amene anatimasula kwa adani athu,
And has taken us out of the hands of our haters: for his mercy is unchanging for ever.
25 Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
Who gives food to all flesh: for his mercy is unchanging for ever.
26 Yamikani Mulungu wakumwamba,
O give praise to the God of heaven: for his mercy is unchanging for ever.

< Masalimo 136 >