< Numeri 34 >

1 Yehova anawuza Mose kuti,
LEUM GOD El kaskas nu sel Moses ac fahk,
2 “Lamula Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Pamene mulowa mʼdziko la Kanaani, dziko lomwe lidzaperekedwa kwa inu ngati cholowa chanu, lidzakhale ndi malire awa:
“Sang oakwuk inge nu sin mwet Israel: Ke kowos ac utyak nu Canaan, facl se ma nga asot nu suwos, pa inge masrol nu ke acn lowos.
3 “‘Chigawo cha kummwera kwa dziko lanu chidzayambira ku chipululu cha Zini motsatana ndi malire a Edomu. Kummawa malire anu a kummwera adzayambira kummawa, kumathero a Nyanja ya Mchere.
Masrol ke layen eir ac som nwe ke yen mwesis Zin wi na masrol nu Edom. Siska kutulap pa mutawauk e ke layen eir ke Meoa Misa.
4 Malirewo adzapita kummwera ndipo adzakwera phiri la Akirabimu mpaka ku Zini. Mathero ake adzakhala kummwera kwa Kadesi-Baranea. Ndipo adzapitenso ku Hazari Adari mpaka kukafika ku Azimoni,
Na ac fah kuhfla nu eir nu ke Innek In Utyak Nu Akrabbim, ac som sasla acn Zin na nwe ke sun eir in acn Kadesh Barnea. Na ac fah kuhfwak nu roto epang nu Hazar Addar ac fahla nwe Azmon,
5 kumene malirewo adzakhote kuchokera ku Azimoni mpaka ku khwawa la ku Igupto ndi kukathera ku Nyanja Yayikulu.
yen se ma ac kuhfla nu infahlfal nu ke masrol lun Egypt, ac safla ke Meoa Mediterranean.
6 “‘Malire anu a ku madzulo adzakhala ku gombe la Nyanja Yayikulu. Amenewo ndiwo adzakhale malire anu a ku madzulo.
“Masrol layen nu roto pa Meoa Mediterranean.
7 “‘Malire anu a kumpoto, mzere wake uyambire ku Nyanja Yayikulu mpaka ku phiri la Hori
“Masrol layen nu epang uh ac fah suwosme Meoa Mediterranean nwe Fineol Hor
8 ndi kuchokera ku phiri la Hori mpaka ku Lebo Hamati. Malirewa apite ku Zedadi,
ac ut we lac ke Innek In Utyak Nu Hamath, na sifil fahla nwe Zedad
9 ndi kupitirira mpaka ku Ziforoni ndi kukathera ku Hazari-Enani. Awa ndiwo adzakhale malire anu a kumpoto.
ac nu Ziphron, na fahla safla ke acn Hazar Enan.
10 “‘Za malire anu a kummawa, mulembe mzere kuchokera ku Hazari-Enani mpaka kukafika ku Sefamu.
“Masrol layen nu kutulap ac fah mutawauk Hazar Enan fahla nwe Shepham.
11 Malirewo adzatsikire ku Sefamu mpaka ku Ribila cha kummawa kwa Aini ndi kupitirira mpaka ku matsitso a cha kummawa kwa Nyanja ya Kinereti.
Na ac fah oatui nu eir som nwe Harbel, kutulap in acn Ain, ac suwoslana nu infulan eol kutulap in Lulu Galilee,
12 Tsono malirewo adzatsika motsatana ndi Yorodani ndi kukathera ku Nyanja ya Mchere. “‘Limeneli lidzakhala dziko lanu ndi malire ake mbali zonse.’”
na fahla eir lac ke Infacl Jordan nwe ke Meoa Misa. “Pa inge masrol akosr lun acn suwos uh.”
13 Ndipo Mose analamula Aisraeli kuti, “Limeneli ndi dziko limene mudzalilandira pochita maere kuti likhale cholowa chanu. Yehova analamula kuti liperekedwe ku mafuko asanu ndi anayi ndi theka,
Na Moses el fahk nu sin mwet Israel, “Pa inge facl se su kowos ac eis ke susfa, ma LEUM GOD El sang nu sin sruf eu tafu lun Israel.
14 chifukwa mabanja a fuko la Rubeni, fuko la Gadi, ndi theka la fuko la Manase analandiriratu cholowa chawo.
Sruf lal Reuben ac sruf lal Gad ac tafu sruf lal Manasseh eis tari acn selos, kitakatelik fal nu ke lupan sou lalos,
15 Mafuko awiriwa pamodzi ndi theka la fuko la Manase analandiriratu cholowa chawo patsidya pa mtsinje wa Yorodani ku Yeriko cha kummawa kotulukira dzuwa.”
layen kutulap in Infacl Jordan, tulanang Jericho.”
16 Yehova anawuza Mose kuti,
LEUM GOD El fahk nu sel Moses,
17 “Awa ndi mayina a anthu amene adzakugawireni dzikoli kuti likhale cholowa chanu: wansembe Eliezara ndi Yoswa mwana wa Nuni.
“Eleazar mwet to, ac Joshua wen natul Nun, fah kitalik acn uh nu sin mwet uh.
18 Musankhe mtsogoleri mmodzi kuchokera ku fuko lililonse kuti athandize kugawa dzikolo.
Eis pac kais sie mwet kol ke kais sie sruf in kasrelos kitalik.”
19 Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda,
Pa inge mwet su LEUM GOD El sulela: Sruf Mwet Kol Judah Caleb, wen natul Jephunneh Simeon Shelumiel, wen natul Ammihud Benjamin Elidad, wen natul Chislon Dan Bukki, wen natul Jogli Manasseh Hanniel, wen natul Ephod Ephraim Kemuel, wen natul Shiphtan Zebulun Elizaphan, wen natul Parnach Issachar Paltiel, wen natul Azzan Asher Ahihud, wen natul Shelomi Naphtali Pedahel, wen natul Ammihud
20 Semueli mwana wa Amihudi, wochokera ku fuko la Simeoni;
21 Elidadi mwana wa Kisiloni, wochokera ku fuko la Benjamini;
22 Buki mwana wa Yogili, mtsogoleri wochokera ku fuko la Dani;
23 Hanieli mwana wa Efodi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Manase, mwana wa Yosefe;
24 Kemueli mwana wa Sifitani, mtsogoleri wochokera ku fuko la Efereimu, mwana wa Yosefe.
25 Elizafani mwana wa Parinaki, mtsogoleri wochokera ku fuko la Zebuloni;
26 Palitieli mwana wa Azani, mtsogoleri wochokera ku fuko la Isakara,
27 Ahihudi mwana wa Selomi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Aseri;
28 Pedaheli mwana wa Amihudi, mtsogoleri wochokera ku fuko la Nafutali.”
29 Awa ndiwo mayina a anthu amene Yehova analamula kuti agawe cholowa cha Aisraeli mʼdziko la Kanaani.
Pa inge mwet ma LEUM GOD El srisrngiya in kitalik acn nu sin mwet Israel in facl Canaan.

< Numeri 34 >