< Mateyu 18 >
1 Pa nthawi imeneyo ophunzira anabwera kwa Yesu ndipo anamufunsa kuti, “Wamkulu woposa onse ndani mu ufumu wakumwamba?”
Ho alu lo lvbwlaksu vdwv Jisu gvlo aala, tvvkato, “Nyidomooku gv Karv tolo yvvla kaiyachok jinv ngv?”
2 Iye anayitana kamwana kakangʼono ndi kukayimiritsa pakati pawo.
Vkvlvgabv Jisu vmi go gokla bunugv kaagialo dakmuto,
3 Ndipo Iye anati, “Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti ngati simusintha ndi kukhala ngati tiana tatingʼono, simudzalowa konse mu ufumu wakumwamba.
okv minto, “Ngo nonua milv jidunv vdwlo nonu mvngdinla so vmi so aingbv rima redw, nonu vdwloka Nyidomooku Karv tolo aala mare.
4 Chifukwa chake, aliyense amene adzichepetsa yekha ngati kamwana aka, ameneyo ndiye wamkulu koposa onse mu ufumu wakumwamba.
Yvvdw so vmi aingbv rila nyanyak dunv hv Nyidomooku gv Karv tolo kaiyachok nvgobv rireku.
5 Ndipo aliyense amene alandira kamwana kakangʼono ngati aka mu dzina langa, alandira Ine.
Okv yvvdw svkvnv vmia ngoogv amin bv alvbv naarwk sidunv, hv ngamka naarwk sidunv.”
6 “Koma ngati wina aliyense achimwitsa mmodzi wa ana awa, amene akhulupirira Ine, kuti achimwe, kukanakhala bwino kuti iye amangiriridwe chimwala chachikulu mʼkhosi mwake ndi kumizidwa pansi pa nyanja.
“Yvv akonv so miangnv vdw sokv akonyi nga mvngjing nvnga mva riadunv, ho nyi angv vbvribolo alvyare ninyigv lvngpo lo vlwng pwktv nvgo paklwk sutola svmasa bolo poklwk sunam mv.
7 Tsoka dziko lapansi chifukwa cha zinthu zimene ziyenera kubwera, koma tsoka kwa munthu amene abweretsa zotere!
Achialvbv mvngru runam gubv rire nyiamooku gv nyi vdwa ogulvgavbolo bunugv mvngjwng nga ngoomu jinv ngv achialvdu! Vkv nvngv lokia ribwngre-vbvritola yvvdw um bunua rimudunv hv achialvbv mvngru runam gubv rire!
8 Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha. (aiōnios )
“Noogv laak gunv vmalo lvpa gunv noogv mvngjwng nga mvlamva riadu bolo, hum palin gvrila ora tvka! noogv lvgabv hv alvyare turnamlo laak vmalo lvpa gunv kaamabv vngnam mv, vbvmayabv laak laknyia okv lvpa lvnyia gvtola vmv doobwngnv gula dookulo orlwk komam svnga. (aiōnios )
9 Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, ulichotse ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kuti ukalowe ku moyo wosatha ndi diso limodzi kuposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kukaponyedwa ku moto wa gehena.” (Geenna )
Okv noogv nyik gunv noogv mvngjwng nga nyemu bolo, hum koolin gvrila ora tvka! Noogv lvgabv si alvyare no nyik nyikin tvvla singkulo vngnam mv, vmabvya nyik nyiknyia gvtola uyumooku bolo orlwk komam svnga. (Geenna )
10 “Onetsetsani kuti musanyoze mmodzi wa anawa. Pakuti ndikuwuzani kuti angelo awo kumwamba amakhala pamaso pa Atate anga akumwamba nthawi zonse.”
“Kaatoka nonuno miangnv vdw so gv akonyika mvngnyekalo mabvka. Ngo nonua mindu, bunugv nyidogindung ngv lokia nyidomooku lo doonv ngo Abu gvlo dooming gvnya dunv.
11 (Mwana wa Munthu anabwera kudzapulumutsa chimene chinatayika).
Nyia Kuunyilo ngv nyekunv vdwa ringlin tvkubv aapv kunv.
12 “Kodi mukuganiza bwanji? Ngati munthu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi nʼkusowa, kodi sasiya 99 zija mʼmapiri ndi kupita kukafuna imodzi yosocherayo?
“Nonuno ogugo mvngdu nyi ako svlar lvnggo dooto okv akonv nyetoku? Nw kvvbi chamkia gula kia nga moodw lo nvmwng dvla rimu pila, nw vngla nyenv anga makardu.
13 Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti akayipeza amasangalala kwambiri chifukwa cha nkhosa imodziyo kuposa nkhosa 99 zimene sizinasochere.
Vdwlo nw hum kaapa rekudw, ngo nonua mindu, nw nyenv akin ho lvgabv nyemanv chamkia gula akkia ngam svnga achialv kaiyago mvngpu yareku.
14 Chimodzimodzinso Atate anu akumwamba safuna kuti mmodzi wa anawa atayike.
So gv apiabv noogv Abu nyidomooku tolo doonv so gv miangnv vdw so akonyika ngoomu dubv mvngma dunv.
15 “Ngati mʼbale wako akuchimwira, pita kamuwuze cholakwa chake pa awiri. Ngati akumvera, wamubweza mʼbale wakoyo.
“Noogv achiboru ngv nam rinyingla rimur dubolo, vngla ninyigv rimur a kaatam laka. Vbvritola um nonyi anyi gv pingkolo risila rila ka. Nw noogv minam a tvvdu boloka, no noogv achiboru a ria yaala paakor pvku.
16 Koma ngati sakumvera, katenge wina mmodzi kapena ena awiri, ‘kuti nkhani itsimikizike ndi umboni wa anthu awiri kapena atatu.’
Vbvritola nw noogv minam a tvvma dubolo, no nyi lo ako vmalo anyigo noogv lvkobv vnggv laka, ogulvgavbolo Darwknv Kitaplo minam aingbv ‘Rimur mvnwngnga tvyakaayanv anyi aom lokv tvbwkkalo dukubv.’
17 Ngati iye akana kuwamvera iwo, kaneneni ku mpingo; ndipo ngati sakamvera ngakhale mpingo, muchite naye monga mukanachitira ndi wakunja kapena wolandira msonkho.
Okv nw bunua tvvmabolo, ogumvnwng nga Gvrja lo minpa laka. Ataranyabv nw Gvrja gv minam haka tvvma kubolo, ninyia mvngjwng manv gubv vmalo rimurnv nyi gubv toa lakuka.
18 “Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti chilichonse chimene muchimanga pa dziko lapansi, chidzamangidwanso kumwamba, ndipo chilichonse chimene muchimasula pa dziko chidzamasulidwanso kumwamba.
“Okv vkvlvgabv ngo nonua mindunv: nonu sichingmooku so ogugo maakv vrikudw hum nyido mooku toloka maakv vrikunv, okv nonu sichingmooku so ogu gonyi vkv vrikudw hum nyido mooku toloka vkv vriku.
19 “Komanso ndikukuwuzani inu kuti ngati awiri a inu pa dziko lapansi avomerezana kanthu kalikonse kamene mukapempha, Atate anga akumwamba adzakuchitirani.
“Okv ngo nonua minta jidunv: Vdwlo nonu sichingmooku so anyi gunv tolwk minsula ogugonyi kumridw, hum nonugv lvgabv ngoogv nyidomooku gv Abu ngv rijireku.
20 Pakuti pamene awiri kapena atatu asonkhana pamodzi mʼdzina langa, Ine ndili nawo pomwepo.”
Ogo lo anyi gunv vmalo aom gunv ngoogv amin bv dookum redw, ngo hoka bunua lvkobv dooming gvdunv.
21 Kenaka Petro anabwera kwa Yesu ndi kumufunsa kuti, “Ambuye, kodi mʼbale wanga akandichimwira ndimukhululukire kokwanira kangati? Mpaka kasanu nʼkawiri?”
Vbvrikunamv Pitar Jisu gvlo aatoku okv tvvkato, “Ahtu nga ngoogv boruv rinyingla rimur morbwng bolo, ngo ninyia vdwgo mvngnga jidubv? Kanw guri?”
22 Yesu anayankha kuti, “Ine ndikukuwuza iwe kuti osati kasanu nʼkawiri, koma ka 70 kuchulukitsa ndi kasanu nʼkawiri.
Jisu mirwkto, “Ma, kanw mwngma, kanw hv chaamkanw lo gubv,
23 “Nʼchifukwa chake, ufumu wakumwamba ukufanana ndi mfumu imene inafuna kuti antchito ake abweze ngongole.
ogulvgavbolo Nyidomooku gv Karv ngv svbv ridunv. Kvlokvcho dvbv ako dooto, nw ninyigv pakbu vdwgv narnamha kaaka dukubv mintoku.
24 Atangoyamba kulandira, anamubweretsa munthu kwa iye amene anakongola ndalama 10,000.
Nw vbv rirap kunam gula bunugv lokv pakbu ako, nw gvlo morko kororgo narnv anga aagv toku.
25 Popeza sakanatha kubweza, bwanayo analamula kuti iye, mkazi wake, ana ake ndi zonse anali nazo zigulitsidwe kuti zibweze ngongoleyo.
Pakbu angv morko dvdu nga dorla kuma toku, vkvlvgabv dvbv ngv morko dvdua dordu kubv nw nyila ninyigv nywng umvuu vdwa nyirabv okv ninyigv yikungyira dvdv nga piokdu kubv orto jitoku.
26 “Wantchitoyo anagwada pamaso pake namupempha iye kuti, ‘Lezereni mtima ndipo ndidzabweza zonse.’
Pakbu angv lvbwng kumpvla dvbv gv habolo gipvto. Nw kodwkkrwkla koola minto, ‘Nga achukgo dooria jilabvkv, okv ngo nam ogumvnwng nga dorku nvpv!’
27 Bwana wakeyo anamuchitira chifundo, namukhululukira ngongoleyo ndipo anamulola apite.
Dvbv ngv ninyia aya mvngpa toku, vkvlvgabv dvbv ninyia morko dvdu nga mvngnga jitoku okv ninyia vngmu toku.
28 “Koma wantchito uja atatuluka, anakumana ndi wantchito mnzake amene anakongola kwa iye madinari 100. Anamugwira, nayamba kumukanyanga pa khosi, namuwumiriza nati, ‘Bwezere zimene unakongola kwa ine!’
Vbvrikunamv nyi angv vnglintoku okv ninyigv pakbu ajin gonyi vngrwk suto hv kvvlo nw gvlo morko achukgo narnv go. Nw hum gakbwng gvrila dvngrapto okv minto, “Ngoogvlo narnam a baapubv jikur lakubv.”
29 “Wantchito mnzakeyo anagwada namupempha iye kuti, ‘Lezere mtima ine, ndipo ndidzakubwezera.’
Ninyigv pakbu ajin angv ninyigv lvpa lvkwnglo gipv la ninyia koodwkkrwkla koola minto, ‘Nga ayala achukgo dooya jilabv, ngo nam dvdua dorku nvpv!’
30 “Koma iye anakana. Mʼmalo mwake, anachoka nakamumangitsa kufikira atabweza ngongoleyo.
Vbvritola nw um tvvmato; vmabvya nw nyi anga dvdua dorma dvdvlo doomure vla patwk tumlwk yatoku.
31 Pamene antchito ena anaona zomwe zinachitikazo, anamva chisoni kwambiri ndipo anapita nakawuza bwana wawo zonse zimene zinachitika.
Vdwlo dvbv pakbu gunv vbvrinam a kaapa tokudw, dvbvnyi ogumvnwng nga minpa toku.
32 “Pamenepo bwanayo anayitana wantchitoyo nati, ‘Iwe wantchito woyipa mtima, ndinakukhululukira ngongole yako yonse chifukwa unandipempha.
Vkvlvgabv nw pakbu anga goklwk toku. Nw minto, ‘Arin kaamanv nyira noo! Noogv ngoogvlo morko narnam mvnwngnga ngo nam mvngnga jitoku, noogv nga vbv koonam lvkwngbv.
33 Kodi iwe sukanamuchitira chifundo wantchito mnzako monga momwe ine ndinakuchitira iwe?’
Ngoogv nam aya mvngpanam aingbv, no pakbu ajin a aya mvngpa rungse gui.’
34 Ndi mkwiyo, bwana wakeyo anamupereka kwa oyangʼanira ndende kuti amuzuze mpaka atabweza zonse zimene anakongola.
Dvbv ngv achialvbv haachi toku, vkvlvgabv nw pakbu anga dvdu nga gvma dvdvlo mvrit modubv vla patwklo vngmu toku.”
35 “Umu ndi mmene Atate anga akumwamba adzachitira ndi aliyense wa inu ngati simukhululukira mʼbale wanu ndi mtima wonse.”
Okv Jisu minyabv mintoku, “Vkv aingbv ngoogv Abu nyidomooku tolo doonv, mvnwngnga mvre, vdwlo nonuno haapok raying lokv achiboru gv rimur a mvngnga maridw.”