< Mateyu 16 >
1 Afarisi ndi Asaduki anabwera kwa Yesu ndi kumuyesa pomufunsa kuti awaonetse chizindikiro chochokera kumwamba.
Mapalishayo na Mashadukayo gubhaajendelenje a Yeshu, bhalikwaatejelanga, gubhaajujilenje bhaatendelanje shilangulo kopoka kunnungu.
2 Iye anayankha kuti, “Kunja kukamada, inu mumati, kudzakhala nyengo yabwino popeza thambo ndi lofiira.
A Yeshu gubhaajangwilenje, “Shiikaga shigulogulo mmanganya nkutinji, ‘Malabhi kupingasha ukoto pabha liunde lishishejela!’
3 Ndipo mmawa mumati, ‘Lero kudzakhala mvula yamphepo popeza thambo ndi lofiira ndi mitambo ya mvula.’ Inu mumadziwa kutanthauzira maonekedwe a thambo koma simungathe kutanthauzira zizindikiro za nthawi.
Kulisha nkutinji, ‘Lelo kukasha ukoto mbungo jipinga puga, pabha liunde lishishejela na maunde gashibhindula!’ Bhai, mmanganya nnamanyililanga kujimanya miongwe kwa lola liunde, ikabheje nkakwimanyanga ilangulo ya jene miongwe jino?
4 Mʼbado woyipa ndi wachigololo umafuna chizindikiro chodabwitsa koma palibe ngakhale chimodzi chidzapatsidwa kupatula chizindikiro cha Yona.” Pamenepo Yesu anawasiya nachoka.
Lubheleko lwa lebha na lukakulupalika kwa a Nnungu! Nnapinganga shilangulo, ikabheje lukapegwa shilangulo shoshowe ikabhe shilangulo sha a Yona.” Bhai, gubhaaleshilenje, nigubhaijabhulile.
5 Koma atawoloka nyanja, ophunzira anayiwala kutenga buledi.
Bhaajiganywa bhabho bhakajombokanjeje ng'ambu jabhili ja litanda, gubhang'amulenje kuti bhashilibhalanga kujigala mikate.
6 Yesu anawawuza kuti, “Chenjerani, khalani tcheru ndi yisiti wa Afarisi ndi Asaduki.”
A Yeshu gubhaalugulilenje, “Mwilolesheyanje na mwiteiganje na ngedule ya Mapalishayo na Mashadukayo!”
7 Iwo anakambirana pakati pawo za izi ndipo anati, “Ichi nʼchifukwa chakuti sitinatenge buledi aliyense.”
Ikabheje bhalabhonji gubhataukengenenje ashayenenji, “Bhanabheleketa nneyo pabha twangajigala mikate.”
8 Yesu atadziwa zokambirana zawo, anawafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mukukambirana zakuti, ‘mulibe buledi?’ Inu achikhulupiriro chochepa.
A Yeshu gubhaimanyi ng'aniyo yabhonji, gubhaalugulilenje, “Mmanganya mmandunji bha ngulupai jishoko! Pakuti nnabheleketanga ga ligongo lya ngajigala mikate?
9 Kodi inu simukumvetsetsabe? Kodi simukukumbukira za buledi musanu amene anadya anthu 5,000 ndi madengu amene munadzaza?
Bhuli, nkanabhe ng'amulanga? Bhuli, nkaakumbushilanga punagebhenye mikate nng'ano jila kwa bhanabhalume elupu nng'ano? Bhuli ikapu yaishoko ilingwa imwagumbeyenje ya malepei?
10 Kapena buledi musanu ndi muwiri amene anadya anthu 4,000, nanga ndi madengu angati amene munadzaza?
Eu, mikate shabha jila jibhagabhanishiywenje bhanabhalume elupu nsheshe, bhuli, imwakundikenyenje ikapu yaikulungwa ilingwa ya malepei?
11 Zitheka bwanji kuti inu simukumvetsetsa kuti Ine sindinkayankhula nanu za buledi? Koma inu chenjerani ndi yisiti wa Afarisi ndi Asaduki.”
Pakuti nkang'amulanga kuti ngabheleketaga ga mikate? Ikabheje mwiteiganje na ngedule ya Mapalishayo na Mashadukayo!”
12 Kenaka iwo anazindikira kuti Iye samawawuza kuti achenjere ndi yisiti wa buledi koma ndi chiphunzitso cha Afarisi ndi Asaduki.
Penepo bhaajiganywa gubhamumanyinji kuti bhashikwaalugulilanga bhaiteiganje nngabha na ngedule ya mmikate, ikabheje bhaiteiganje na majiganyo ga Mapalishayo na Mashadukayo.
13 Yesu atafika ku chigawo cha Kaisareya Filipo, Iye anafunsa ophunzira ake kuti, “Kodi anthu amati Mwana wa Munthu ndi ndani?”
A Yeshu bhakaisheje mmbali ja ku Kaishalia Pilipi, gubhaabhushiyenje bhaajiganywa bhabho, “Bhandu bhakutinji Mwana juka Mundu ni gani?”
14 Iwo anayankha kuti, “Ena amati ndi Yohane Mʼbatizi; ena amati ndi Eliya; komanso ena amati Yeremiya kapena mmodzi wa aneneri.”
Gubhaajangwilenje, “Bhananji bhakutinji a Yowana Bhabhatisha, bhananji a Eliya, bhananji a Yelemia, eu jumo munkumbi gwa ashinkulondola bha a Nnungu.”
15 Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?”
A Yeshu gubhaabhushiyenje, “Na mmanganyanji bhuli, nkutinji nne gani?”
16 Simoni Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.”
A Shimoni Petili gubhajangwile, “Mmwe a Kilishitu, Bhanabhabho a Nnungu, bhali bhabhakoto.”
17 Yesu anati kwa iye, “Ndiwe wodala Simoni mwana wa Yona, popeza si munthu amene anakuwululira izi koma Atate anga akumwamba.
A Yeshu gubhashite, “Mbaya mmwe a Shimoni bhanabhabho a Yona, pabha nngabha mundu anng'ibhulile yenei, ikabhe Atati bhali kunnungu.
18 Ndipo Ine ndikuwuza iwe kuti ndiwe Petro ndipo pa thanthwe ili Ine ndidzamangapo mpingo wanga ndipo makomo a ku gehena sadzawugonjetsa. (Hadēs )
Nne ngunakunnugulila mmwe a Petili, mmwe lindandawe na panani lindandawe ngupinga shenga likanisha lyangu, wala mashili ga kundamo ja bhawilenje gakalikombola. (Hadēs )
19 Ine ndidzakupatsa makiyi a Ufumu wakumwamba, ndipo chilichonse chimene iwe udzachimanga pansi pano chidzamangidwanso kumwamba.”
Shinimpe punguo ya Upalume gwa Kunnungu, shoshowe shishintabhe pa shilambolyo, shishitabhwe kunnungu na shoshowe shishinngopole pa shilambolyo, shishigopolwe kunnungu.”
20 Pamenepo Iye anachenjeza ophunzira ake kuti asawuze wina aliyense kuti ndi Khristu.
Kungai gubhaalimbiyenje bhaajiganywa bhabho, bhanannugulilanje mundu jojowe kuti bhenebho a Kilishitu.
21 Kuyambira nthawi imeneyo Yesu anayamba kuwafotokozera ophunzira ake kuti Iye ayenera kupita ku Yerusalemu ndi kukazunzidwa kwambiri mʼmanja mwa akulu a ansembe ndi aphunzitsi amalamulo kuti ayenera kuphedwa, ndi kuti tsiku lachitatu adzaukitsidwa.
Tandubhila gene malangago a Yeshu gubhatandwibhe kwaalugulilanga bhaajiganywa bhabho gwangali nng'iyo kuti bhanapinjikwa kwenda ku Yelushalemu, na kweneko bhapinga potekwa na bhanangulungwa na bhakulungwanji bhaabhishila na bhaajiganya bha Shalia. Kuti, bhapinga bhulagwa na lyubha lya tatu shibhayuywe.
22 Petro anamutengera Iye pambali nayamba kumudzudzula kuti, “Dzichitireni chifundo Ambuye, sizingachitike kwa Inu ayi.”
A Petili gubhaatolile kuntemela, gubhatandwibhe kwaakalipila, “Inabhe nneyo Mmakulungwa! Lyeneli likankoposhela!”
23 Yesu anatembenuka nati kwa Petro, “Choka pamaso panga Satana! Iwe ndi chokhumudwitsa kwa Ine; iwe suganizira zinthu za Mulungu koma zinthu za anthu.”
Ikabheje a Yeshu gubhatendebhwishe, gubhaalugulile a Petili, “Nnyabhulile apano, Lishetani! Mmwe nnang'ibhilila. Ng'aniyo yenu nngabha ya a Nnungu ikabhe ya shigundu!”
24 Pamenepo Yesu anati kwa ophunzira ake, “Ngati wina aliyense abwera pambuyo panga ayenera kudzikana ndi kutenga mtanda wake ndi kunditsata Ine.
Kungai a Yeshu gubhaalugulilenje bhaajiganywa bhabho, “Mundu jojowe apinga ngagula nne, anapinjikwa aikane nnyene, ajigale nshalabha gwakwe angagule.
25 Pakuti aliyense amene afuna kupulumutsa moyo wake adzawutaya koma aliyense amene ataya moyo wake chifukwa cha Ine adzawupeza.
Pabha, mundu apinga kulama gwangali ngulupalila nne, akakola gumi gwa pitipiti, ikabheje shakunde bhulagwa kwa ligongo lya ngulupalila nne, shakole gumi gwa pitipiti.
26 Kodi munthu adzapindula chiyani ngati atapeza zonse za dziko lapansi nataya moyo wake? Kapena munthu angapereke chiyani chosinthana ndi moyo wake?
Mundu shiimpwaile nndi apataga indu yowe ya pa shilambolyo na akuno aliobhya gumi gwakwe gwa pitipiti? Eu, mundu shashoye shindu shashi pa gumi gwakwe gwa pitipiti?
27 Pakuti Mwana wa Munthu adzabwera mu ulemerero wa Atate ake ndi angelo ake ndipo pamenepo Iye adzapereka mphotho kwa munthu mofanana ndi zimene anachita.
Pabha, Mwana juka Mundu shaishe na ukonjelo gwa Ainagwe pamo na ashimalaika bhakwe, penepo shannipe kila mundu malinga shashite tenda.
28 “Ine ndikuwuzani inu choonadi, ena amene akuyimirira pano sadzalawa imfa asanaone Mwana wa Munthu akudza mu ufumu.”
Kweli ngunakummalanjilanga, bhapalinji bhananji pepano bhakawanganga bhakanabhe kummonanga Mwana juka Mundu alikwiiya malinga Mpalume.”