< Marko 9 >

1 Ndipo anawawuza kuti, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti ena amene ayimirira pano sadzafa asanaone ufumu wa Mulungu ukubwera mwa mphamvu.”
A Yeshu gubhapundile kwalugulilanga, “Kweli ngunakummalanjilanga, bhapalinji bhananji bhalinginji pepano bhakawanganga bhakanabhe kuubhonanga Upalume gwa a Nnungu ulikwiya kwa mashili.”
2 Patatha masiku asanu ndi limodzi Yesu anatenga Petro, Yakobo ndi Yohane nawatsogolera kupita ku phiri lalitali, kumene anali okhaokha. Kumeneko maonekedwe ake anasinthika pamaso pawo.
Gakapiteje mobha nng'ano na limo, a Yeshu gubhaatolilenje a Petili na a Yakobho na a Yowana, gubhapite nabhonji kushitumbi shashileu kwa jikape. Kweneko gubhapindikwishe lubhombo lwabho, mmujo jabhonji, nibhoneka shinape.
3 Zovala zake zinawala monyezimira kwambiri, kotero kuti palibe sopo wina aliyense amene angaziyeretse monyezimira chotere pa dziko la pansi.
Nngubho yabho yashinkung'anyima niwejela kwa kaje, wala jwakwapi nkushapa jojowe pa shilambolyo akombola kushapa nikwiitenda iwejele malinga nneyo.
4 Ndipo anaonekera Eliya ndi Mose pamaso pawo, amene ankayankhulana ndi Yesu.
Gubhakoposhelenje a Eliya na a Musha gubhakungulukenje na a Yeshu.
5 Petro anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, ndi kwabwino kuti ife tili pano. Tiyeni timange misasa itatu; umodzi wanu, wina wa Mose ndi wina wa Eliya.”
A Petili gubhaalugulile a Yeshu, “Mmajiganya, shankonja uwe kubha apano. Bhai, tushenje itala itatu, shimo shenu mmwe, na shina sha a Musha na shina sha a Eliya.”
6 (Iye sanadziwe choti anene, anali ndi mantha akulu).
Mbena bhakashimanyaga shibhabheleketaga, pabha bhenebho na ashajabhonji bhashinkujogopanga.
7 Pamenepo mtambo unaoneka ndi kuwaphimba, ndipo mawu anamveka kuchokera mu mtambo kuti, “Uyu ndi Mwana wanga wokondedwa. Mvereni Iye!”
Kungai gulyaunishilenje liunde malinga shiwili, lilobhe likupilikanikaga nniundemo “Jweneju Mwanangu jungumpinga, mumpilikanishiyanje.”
8 Mwadzidzidzi, atayangʼanayangʼana, sanaonenso wina aliyense ali ndi iwo kupatula Yesu.
Shangupe bhakang'wang'wayanjeje, bhangammonanga mundu juna ikabhe a Yeshu jikape.
9 Pamene ankatsika kuchokera ku phiri, Yesu anawalamulira kuti asawuze aliyense zimene anaona mpaka Mwana wa Munthu atauka kwa akufa.
Bhai, pubhalinginji nkuelela shitumbi, a Yeshu gubhaalimbiyenje bhanannugulilanje mundu jojowe indu ibhaibhweninji, mpaka Mwana juka Mundujo, pushayushe awaga.
10 Iwo anayisunga nkhaniyo nakambirana za tanthauzo lake la “Kuuka kwa akufa.”
Bhai, gubhalibhishilenje mmitima lyene lilobhelyo, bhalibhuyananga ashaayenenji malombolelo ga yuka kopoka kubhawilenje.
11 Ndipo anamufunsa Iye kuti, “Nʼchifukwa chiyani aphunzitsi amalamulo amati Eliya ayenera kuyamba wabwera?”
Gubhaabhushiyenje a Yeshu, “Pakuti bhaajiganya bha Shalia bhakutinji mpaka bhatandubhe kuika a Eliya?”
12 Yesu anayankha kuti, “Kunena motsimikiza, Eliya ayeneradi kuyamba kubwera kudzakonzanso zinthu zonse. Nʼchifukwa chiyani tsono zinalembedwa, kuti Mwana wa Munthu ayenera kuvutika kwambiri ndi kukanidwa?
A Yeshu gubhaajangwilenje, “Elo, a Eliya bhanakwiyati kualaya yowe. Nkali nneyo, kwandi bhai ishijandikwa Mmajandiko ga Ukonjelo kuti Mwana juka Mundu anapinjikwa potekwa na kanwa?
13 Koma ndikuwuzani, kuti Eliya wabweradi, ndipo amuchitira iye zonse zimene iwo anafuna, monga momwe zalembedwera za iye.”
Ikabheje ngunakummalanjilanga, a Eliya bhaaishe, nabhalabhonji nigubhaatendelenje yowe ibhapinjilenje, malinga shibhajandishilwe Mmajandiko ga Ukonjelo.”
14 Atafika kwa ophunzira ena aja, anaona gulu lalikulu la anthu litawazungulira ndi aphunzitsi amalamulo akutsutsana nawo.
Bhakaaishilanjeje bhaajiganywa bhananji bhala, gubhalubhweninji lugwinjili lukulungwa lwa bhandu lwaatimbililenje bhalitaukangana na bhaajiganya bha shalia.
15 Nthawi yomweyo anthu onse atamuona, anadabwa kwambiri ndipo anathamanga kukamulonjera.
Shangupe lugwinjili lwa bhandu bhaakabhonanjeje a Yeshu, bhowe bhashinkulapanga kwa kaje, gubhaabhutushilenje kukwalamushila.
16 Iye anafunsa kuti, “Mukukangana nawo chiyani iwowa?”
A Yeshu gubhabhushiyenje, “Nkutaukangana nndi?”
17 Munthu wina mʼgululo anayankha kuti, “Aphunzitsi, ndinakubweretserani mwana wanga wamwamuna, amene ndi ogwidwa ndi mzimu umene umamulepheretsa kuyankhula.
Mundu jumo munkumbi mula gwabhajangwile, “Mmajiganya, njikwiyanajo mwanangu kwenu mmwe, ashikola lioka likuntenda anabhelekete.
18 Nthawi iliyonse ukamugwira umamugwetsa pansi. Amatuluka thovu kukamwa, amakukuta mano ake ndipo amawuma. Ndinapempha ophunzira anu kuti awutulutse mzimuwo, koma sanathe.”
Papagwinji ashikilwaga anakunngwiya pai na kopoka shiulo nkang'wa, alitauna meno na ng'ang'anala shiilu showe. Njinkwaajuganga bhaajiganywa bhenu bhanshoyanje ikabheje bhangakombolanga.”
19 Yesu anayankha kuti, “Haa! Mʼbado osakhulupirira, kodi ndidzakhala nanu mpaka liti? Mubweretseni kwa Ine mnyamatayo.”
A Yeshu gubhaalugulilenje, “Mmanganya lubheleko lwangali ngulupai! Shindame na mmanganya mpaka shakani? Shinikakatimile mpaka shakani? Munnjiyenajonji akuno.”
20 Ndipo anamubweretsa kwa Iye. Mzimu woyipawo utaona Yesu, nthawi yomweyo unamukomola mnyamatayo. Anagwa pansi ndi kumagubuduka, ndi kuchita thovu kukamwa.
Gubhampelekenje. Shangupe lioka jula akaabhoneje a Yeshu, gwanngwishiye nikunng'ungumiya, aligalabhuka na kopoka shiulo nkang'wa.
21 Yesu anafunsa abambo a mnyamatayo kuti, “Kodi wakhala chotere nthawi yayitali bwanji?” Iye anayankha kuti, “Kuyambira ali wamngʼono,
A Yeshu gubhaabhushiye ainamundu, “Genega pugampatile kutandubhila shakani?” Nabhalabho gubhajangwile, “Tandubhila ali mwana.
22 wakhala ukumuponya pa moto kapena mʼmadzi kuti umuphe. Koma ngati mungathe kuchita kanthu, tichitireni chifundo ndipo mutithandize.”
Papagwinji lioka linakunngwishiya pamoto na mmashi, nkupinga limmulaje. Bhai, ibhaga nnakombola, ntubhonele shiya na ntujangutile!”
23 Yesu anati, “‘Ngati mungathe!’ Zinthu zonse ndi zotheka kwa iye amene akhulupirira.”
A Yeshu gubhaalugulile, “Kwa nndi nkuti, nkombolaga? Gowe ganaakomboleka kuka mundu akulupalila.”
24 Nthawi yomweyo abambo a mwanayo anafuwula kuti, “Ndikhulupirira; thandizani kusakhulupirira kwanga!”
Penepo ainamundu bhala gubhagutile bhalinkuti, “Ngulikulupalila! Nnyangutile kwa ungakulupalila gwangu.”
25 Yesu ataona kuti gulu la anthu likuthamangira kumalowo, anadzudzula mzimu woyipawo kuti, “Iwe mzimu wolepheretsa kuyankhula ndi kumva, ndikulamulira tuluka mwa iye ndipo usadzalowenso.”
A Yeshu bhakalubhoneje lugwinjili lwa bhandu lulikwaajiila shibhutuka, gubhankalipile lioka jula bhalinkuti, “Lioka ukuntenda mwanaju anabhelekete na anapilikane, ngunakuamulisha gunshoshe nshandaju na unannjinjile kabhili!”
26 Mzimuwo unafuwula ndi kumugubuduza kwambiri ndipo unatuluka. Mnyamatayo anaoneka ngati mtembo ndipo ambiri anati, “Wafa.”
Lioka jula gwagutile, gwanng'ungumiye kwa kaje, kungai gwanshoshile. Nshanda jula paliji mbuti ashiwa, na bhananji gubhashitenje kuti, “Awile!”
27 Koma Yesu anamugwira dzanja ndipo anamuyimiritsa, ndipo anayimirira.
Ikabheje a Yeshu gubhankamwile nkono, gubhannjinwile na jwalakwe gwajimi.
28 Yesu atalowa mʼnyumba, ophunzira ake anamufunsa ali pa okha kuti, “Kodi ndi chifukwa chiyani ife sitinathe kutulutsa chiwandacho?”
Bhai, a Yeshu bhakajinjileje nnyumba, bhaajiganywa bhabho gubhaabhushiyenje pajika, “Pakuti uwe twangakombola kunshoya?”
29 Iye anayankha kuti, “Mtundu uwu umatuluka pokhapokha mwapemphera ndi kusala kudya.”
Na bhalabho a Yeshu gubhaabhalanjilenje, “Lioka lya malinga lyeneli nkakombolanga kulishoya, ikabhe kwa juga Nnungupe.”
30 Anachoka malo amenewo nadutsa ku Galileya. Yesu sanafune kuti wina aliyense adziwe kumene anali,
A Yeshu na bhaajiganywa bhabho gubhashoshilenje pepala, gubhapelengenyenje na mwanja gwabhonji pitila ku Galilaya. Na bhalabho a Yeshu bhakapinjileje mundu amumanye kubhali,
31 chifukwa amaphunzitsa ophunzira ake. Anati kwa iwo, “Mwana wa Munthu adzaperekedwa mʼmanja mwa anthu. Adzamupha, ndipo patatha masiku atatu adzauka.”
pabha bhatendaga kwaajiganyanga bhaajiganywa bhabho. Gubhaalugulilenje, “Nne Mwana juka Mundu shingamuywe kubhandu na shibhammulaganje, ikabheje lyubha lya tatu shinyushe.”
32 Koma sanazindikire chimene amatanthauza, ndipo anachita mantha kuti amufunse.
Bhaajiganywa bhabho bhangalimanyanga lyenelyo. Ikabheje gubhajogopenje kwaabhuya.
33 Anafika ku Kaperenawo. Pamene anali mʼnyumba, anawafunsa kuti, “Kodi mumatsutsana chiyani mʼnjira muja?”
Bhai, gubhaikengenenje ku Kapalanaumu. Pubhaliji nnyumba, a Yeshu gubhaabhushiyenje, “Mwataukanganaga nndi mumpanda?”
34 Koma anakhala chete chifukwa ali mʼnjira amatsutsana za kuti wamkulu kuposa onse ndani.
Ikabheje bhanganyabho gubhatemingenenje ilili, pabha mumpanda bhatenda taukangana ga gani ali nkulungwa jwabhonji.
35 Atakhala pansi, Yesu anayitana khumi ndi awiriwo nati, “Ngati wina aliyense afuna kukhala woyamba, ayenera kukhala wotsiriza ndi wotumikira onse.”
A Yeshu gubhatemi pai, gubhaashemilenje likumi limo na bhabhili bhala, gubhalugulilenje, “Mundu apinga kubha nkulungwa, anapinjikwa abhe jwa kumpelo na ntumishi jwa bhowe.”
36 Anatenga kamwana nakayimiritsa pakati pawo ndipo anawawuza kuti,
Kungai gubhantolile mwana jwa nshoko, gubhannjimishe pakatipakati jabhonji, gubhannjambete, gubhaalugulilenje,
37 “Aliyense wolandira mmodzi wa ana angʼono awa mʼdzina langa alandira Ine; ndipo aliyense wolandira Ine salandira Ine koma amene anandituma.”
“Akumposhela mwana jwa nshoko malinga jweneju kwa lina lyangu, anamboshela nne, na amboshela nne, akaamboshela nnepe, ikabheje na bhandumile bhala.”
38 Yohane anati, “Aphunzitsi, tinaona munthu akutulutsa ziwanda mʼdzina lanu ndipo ife tinamuwuza kuti aleke, chifukwa sanali mmodzi wa ife.”
A Yowana gubhaalugulile a Yeshu, “Mmajiganya, tushikummona mundu jumo alishoya maoka kwa lina lyenu, na uwe gutulinjile kunnimbiya pabha nngabha jwa munkumbi gwetu.”
39 Yesu anati, “Musamuletse, palibe amene amachita chodabwitsa mʼdzina langa ndipo kenaka nanena zoyipa za Ine,
Ikabheje a Yeshu gubhashite, “Nnannimbiyanje, pabha jwakwapi mundu atenda ilapo kwa lina lyangu, popo pepo nimeleketela yangali ya mmbone.
40 pakuti aliyense amene satsutsana nafe ali mbali yathu.
Pabha akakututauka, pali na uwe.
41 Zoonadi, Ine ndikuwuzani kuti aliyense amene akupatsani chikho cha madzi mʼdzina langa chifukwa ndinu ake a Khristu, sadzataya konse mphotho yake.”
Mundu jojowe shampanganje mashi ga ng'wa, ligongo nshibhanganga bhandu bha a Kilishitu, kweli ngunakummalanjilanga akapelela upo yakwe.
42 “Ndipo ngati wina aliyense achimwitsa mmodzi wa ana angʼono awa amene akhulupirira Ine, kukanakhala bwino kwa iye kuti aponyedwe mʼnyanja atamangiriridwa mwala waukulu mʼkhosi mwake.
“Mundu jojowe shannebhye jumo jwa munkumbi gwa bhashokonji bhangulupalilangabha, kaliji mbaya jwene mundujo, atabhilwe liganga likulungwa lya yajila nnukoi lwakwe nileshelwa mmaali.
43 Ngati dzanja lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo ndi dzanja limodzi kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri ndi kupita ku gehena, kumene moto wake suzima. (Geenna g1067)
Nkono gwenu unnebhyaga muukate! Mbaya jinjila mugumi gwangali nkono gumo, nngalingana na kola makono ganaabhili, nileshelwa kumoto gwa ku Jeanamu. (Geenna g1067)
44 (Kumene mphutsi zake sizifa ndipo moto wake suzima).
Mwenemo mbiu yakwe ikawa, wala moto gwake ukaimika.
45 Ndipo ngati phazi lako likuchimwitsa, lidule. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa mʼmoyo olumala kusiyana ndi kukhala ndi mapazi awiri ndi kuponyedwa mu gehena. (Geenna g1067)
Na lukongono lwenu lunnebhyaga, nnukate! Mbaya jinjila mugumi nni na lukongono lumo, nngalingana kola makongono ganaabhili, nileshelwa kumoto gwa ku Jeanamu. (Geenna g1067)
46 (Kumene mphutsi zake sizifa ndipo moto wake suzima).
Mwenemo mbiu yakwe ikawa, wala moto gwake ukaimika.
47 Ndipo ngati diso lako likuchimwitsa, likolowole. Ndi kwabwino kwa iwe kulowa ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi, kusiyana ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa mu gehena, (Geenna g1067)
Na liyo lyenu linnebhyaga nnishoye! Mbaya jinjila mu Upalume gwa a Nnungu nninkwete shongo, nngalingana kola meyo ganaabhili, nileshelwa kumoto gwa ku Jeanamu. (Geenna g1067)
48 kumene “‘mphutsi zake sizifa ndipo moto wake suzima.’
Mwenemo mbiu yakwe ikawa, wala moto gwakwe ukaimika.
49 Aliyense adzayesedwa ndi moto.
“Pabha kila mundu shaukangwe na moto malinga mbepei puiukangwa na nnjete.
50 “Mchere ndi wabwino, koma ngati utasukuluka, mungawukoleretsenso bwanji? Mukhale nawo mchere mwa inu nokha, ndipo mukhale pa mtendere wina ndi mnzake.”
Nnjete ni ja mmbone, ikabheje jikanonye jitagwe indi nkupinga jinonye? Ntamangane kwa ulele munkumbi gwenunji, nkupinga kunong'aya shilongani.”

< Marko 9 >