< Yohane 4 >
1 Yesu atazindikira kuti Afarisi amva zoti Iye ankapeza ndi kubatiza ophunzira ambiri kupambana Yohane,
Parisi vdwv Jisu Jonnyi kaiyabv nyi naalwkla okv baptist jidu vla tvvpato.
2 (ngakhale kuti Yesuyo sankabatiza, koma ophunzira ake).
Minje jvbolo Jisu atuv yvvnyika baptisma jimato; ninyigv lvbwlaksu vdwv mvngchik jito.
3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.
Vkvlvgabv vdwlo Jisu ogugo minpvdw tvvtoku, hv Judia nga vngyula okv Galili bv vngkur toku;
4 Ndipo Iye anayenera kudutsa mu Samariya.
ninyigv vngku lamtv ngv Samaria bv vngpitla vngdubv rito.
5 Iye anafika mʼmudzi wa Asamariya wotchedwa Sukari, pafupi ndi malo amene Yakobo anapatsa mwana wake Yosefe.
Samaria lo Sikar vnam banggu lo hv aalwk toku, ho Jakop gv ninyigv kuu Josepnyi jinam rongo lokv adu mato.
6 Chitsime cha Yakobo chinali pamenepo ndipo Yesu atatopa ndi ulendo anakhala pansi pambali pa chitsimecho. Nthawi inali pafupifupi ora lachisanu ndi chimodzi masana.
Jakop gv isikua ngv hoka dooto, okv Jisu, moing vngkunamv anyu kuma toku, isi kua hoka dootungla doonu toku. Vbvrire hoka alu lopo bv rito.
7 Mayi wa Chisamariya atabwera kudzatunga madzi, Yesu anati kwa iye, “Kodi ungandipatse madzi akumwa.”
Samaritan nyimv gonv isi mego tokdubv hoka aato, okv Jisu ninyia minto, “Nga isi tvngse go jilabv,”
8 (Ophunzira ake nʼkuti atapita mʼmudzi kukagula chakudya).
Ninyigv lvbwlaksu vdwv dvnam rvvbv banggu lo vngyu roto.
9 Mayiyo anati kwa Iye, “Inu ndinu Myuda ndipo ine ndine Msamariya. Bwanji mukundipempha madzi akumwa?” (Popeza Ayuda ndi Asamariya sankayanjana).
Nyimv angv mirwksito, “No Jiu go, okv ngo Samaritan nyimv go—vkvlvgabv no oguaingbv nga tvngnamgu koodunv?” (Samaritan vdwgv dvnv tvngnvnv koobu okv bati vdwa Jius vdwv dvnv tvngnv madunv.)
10 Yesu anamuyankha kuti, “Koma iwe ukanadziwa mphatso ya Mulungu ndi Iye amene akukupempha madzi akumwa, ukanamupempha ndipo akanakupatsa madzi amoyo.”
Jisu mirwksito, “No Pwknvyarnv gv jinam a okv nam isi tvngse go koodudw ninyia chinv guilo, no ninyia koya dvnvpv, okv hv nam turgvnv isi a jiri nvpv.”
11 Mayiyo anati, “Ambuye, Inu mulibe kanthu kotungira madzi ndipo chitsime ndi chakuya. Kodi madzi amoyowo mungawatenge kuti?
Nyimv angv minto, “Tamsarnv, no isi toknvnv bvngma, okv isi kua ngv arwng chekwng do. Ogolo no turnvnv isi a paala dubv?
12 Kodi Inu ndinu wamkulu kuposa kholo lathu Yakobo, amene anatipatsa chitsimechi ndipo iye ankamwanso monga anachita ana ake ndi ziweto zake?”
Si ngonugv abuapa Jakob gv ngonua isi kua jinammv; ninyi okv ninyigv kuunyilo, okv ninyigv sonam svnwngsvmin mvnwngngv soka tvngnya pvnv. No atuv Jakobnyi kaiyanv gubv minsu dunvre?”
13 Yesu anayankha kuti, “Aliyense amene amamwa madzi awa amamvanso ludzu,
Jisu mirwksito, “Yvvdw so gv isi a tvngdunv hv tvngnwng nwngkor reku,
14 koma aliyense amene adzamwa madzi amene Ine ndidzamupatsa sadzamvanso ludzu. Ndithudi, madzi amene ndidzamupatsa adzakhala kasupe wamadzi wotumphukira ku moyo wosatha.” (aiōn , aiōnios )
Vbvritola yvvdw ngoogv isi jinam ha tvngdunv hv vdwloka tvngnwng nwngkor kumare, ngoogv ninyia isi jinammv ninyigv lvgabv isi boklin sinv aingbv rila ninyi singnam a turnam jinv isi gubv rire okv ninyi turbwngnv singnam a jire.” (aiōn , aiōnios )
15 Mayiyo anati kwa Iye, “Ambuye, patseni madzi amenewo kuti ndisadzamvenso ludzu ndi kumabwerabe kuno kudzatunga madzi.”
Nyimv angv ninyia minto, “Tamsarnv, ho isia ngam jilabvkv! vbvrikubolo ngo vdwloka tvngnwng mvngkor kuma dukubv, okv soka isi tokbv aakwng kuma dukubv.”
16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”
Jisu ninyia minto, “No vngyila no gv nyilua gokte kuka, okv aakur lakuka.”
17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.” Yesu anati kwa iye, “Wakhoza ponena kuti ulibe mwamuna.
Hv mirwkto, “Ngo nyilu guka kaama.” Jisu mirwk sutoku, “Noogv ngo nyilu kaama vla minam v no jvjvbv mirungdo.
18 Zoona nʼzakuti iwe wakhala pa banja ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene uli naye tsopano si wako. Zimene wanenazi ndi zoona.”
No nyi angu go nyilubv mvtoku, okv noogv vjak lvkobv doogvnam nyi angvka noogv nyilu jvjvma. No nga jvjvbv minpa gvibv.”
19 Mayiyo anati, “Ambuye, ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri.
Nyimv angv minto, “Tamsarnv, ngo kaanam v no nyijwk go,”
20 Makolo athu ankapembedza mʼphiri ili koma inu Ayuda mumati malo amene tiyenera kupembedzera ali ku Yerusalemu.”
“Ngoogv Samaritan abuapa vdwv Pwknvyarnvnyi so moodw so kumtojotoku, vbvritola nonu Jius vdwv Jerusalem v ngonugv Pwknvyarnvnyi kumjijojiku mooku v vla mindo.”
21 Yesu anati, “Mayi inu khulupirira Ine. Nthawi ikubwera pamene inu simudzapembedza Atate mʼphiri ili kapena mu Yerusalemu.
Jisu ninyia minto, “Nyimv, nga mvngjwng tvka, vkvnv aluv aariku nyi vdwv Abunyi so moodw sokaka kumnyajonya kumare vmalo Jerusalem loka kumnyajonya kumare.
22 Inu Asamariya mumapembedza chimene simukuchidziwa. Ife timapembedza chimene tikuchidziwa, pakuti chipulumutso nʼchochokera kwa Ayuda.
Nonu Samaritan vdwv jvjv rungbv chima nonu yvvnyi kumdujodu nvdw; vbvritola ngonu Jius vdwv chindu ngonu yvvnyi kumdujodu nvdw, ogulvgavbolo so si Jius lokv ringlinbaalin v aadu.
23 Koma nthawi ikubwera ndipo yafika kale tsopano pamene opembedza woona adzapembedza Atate mu mzimu ndi mʼchoonadi, pakuti opembedza otere ndiwo amene Atate akuwafuna.
Vbvritola aluv aariku okv vjak si doopv, Pwknvyarnv gv Dow gv jwkrw lokv nyi vdwv Abunyi jvjvbv kumlajola, ninyigv mvnglwk kaalwkbv kumrejoreku.
24 Mulungu ndi Mzimu, ndipo omupembedza Iye ayenera kumupembedza mu mzimu ndi mʼchoonadi.”
Pwknvyarnv Dowbv ridunv, okv yvv ninyia kumdujodunv hv jvjv rungbv okv dow bv kumlajola rirung sego.”
25 Mayiyo anati, “Ine ndikudziwa kuti Mesiya (wotchedwa Khristu) akubwera. Akabwera, Iye adzafotokoza zonse kwa ife.”
Nyimv angv ninyia minto, “Ngo chindu Kristo aariku, okv vdwlo hv aarikudw, hv ogumvnwng nga ngonua minbwk jireku.”
26 Ndipo Yesu anamuwuza kuti, “Amene ndikukuyankhulane, ndine amene.”
Jisu mirwk sutoku, “Hv dv ngo mabv, nam lvkobv raamisidunv.”
27 Pa nthawi yomweyo ophunzira ake anabwerera ndipo anadabwa kupeza Iye akuyankhula ndi mayi. Koma palibe amene anamufunsa kuti, “Kodi mukufuna chiyani?” kapena, “Nʼchifukwa chiyani mukuyankhula naye?”
Vbvrire hoka Jisu gv lvbwlaksu vdwv aakur toku, okv bunu ninyia nyimv gonyi raami sudubv kaala kairungbv lamrwpanya toku. Vbvritola bunugv lokv yvvka nyimv anga “No ogugo mvngdu?” Vla minv kaamato, vmalo Jisu nyika “No ogubv nyimv anga raami sudunv?” vla tvvka nvgoka kaamato.
28 Kenaka mayiyo anasiya mtsuko wamadzi, nabwerera ku mzinda ndipo anati kwa anthu,
Vbvrikunamv nyimv angv isi pvchwng nga kayupila, banggubv vngkur toku, okv hoka nyi vdwa mintoku,
29 “Tiyeni mukaone munthu amene wandiwuza ine zilizonse zimene ndinazichita. Kodi ameneyu sangakhale Khristu?”
“Aato okv nyi anga kaakwto ngoogv ogugo rikunam mvnwngnga minpa nvgo. Kristo vnammv v bri?”
30 Iwo anatuluka mʼmudziwo ndi kupita kumene kunali Iye.
Vkvlvgabv bunu banggu a kayupila okv Jisu gvlo vngtoku.
31 Pa nthawi imeneyi ndi kuti ophunzira ake akumukakamiza kuti, “Rabi idyani.”
Vbvridung rilo lvbwlaksu vdwv Jisunyi dinchi rungbv minto, “Tamsarnv, dvnam go dvlakv!”
32 Koma Iye anawawuza kuti, “Ine ndili ndi chakudya choti ndidye chimene inu simukuchidziwa.”
Vbvritola hv mirwkto, “Ngoogvlo nonugv chimanam dvnam v doodu.”
33 Ndipo ophunzira ake anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi alipo wina amene anamubweretsera Iye chakudya?”
Vkvlvgabv lvbwlaksu vdwv bunugv aralo tvka minsunyato “Nyi gunv ninyia dvnamgu bvnglwk jipv nvgu bri?”
34 Yesu anati, “Chakudya changa ndikuchita chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi kumaliza ntchito yake.
Jisu bunua minto, “Ngoogv dvnam hv Pwknvyarnv gv mvngkubv rinam angv nw ngam vngmunv okv ngo ninyigv rimidubv jinam ha rirungre.
35 Kodi inu simunena kuti, ‘Kwatsala miyezi inayi ndipo kenaka kukolola?’ Ine ndikukuwuzani kuti, tsekulani maso anu ndipo muyangʼane mʼminda! Mbewu zacha kale kuti zikololedwe.
Nonu mimbwng namgo doodu, ‘Poolu pwpi go doodvdu aam nvdwv’vla. Vbvritola ngo nonua mindunv, rongo nga alvbv kaatoka; rongo gv aam hv nginduku okv nvvdubv riduku!
36 Ngakhale tsopano amene akukolola akulandira malipiro ake, ndipo akututa mbewu ku moyo wosatha kuti wofesa ndi wokolola asangalale pamodzi. (aiōnios )
Yvvnyiv aam nvvpvdw nvvjo nga paadu okv turbwng gvnv dubv nvvchingla vvpvdu, ho hv lvvlwk nvla nvvchingnv lvkobv himpu pubam dubv vla. (aiōnios )
37 Nʼchifukwa chake mawu akuti, ‘Wina amafesa ndipo wina amakolola’ ndi woona.
‘Nyi akonv lvvriare nyi akonv nvvching riare’ vnam si jvjv rungdo.
38 Ine ndinakutumani kukakolola zimene simunagwirire ntchito. Ena anagwira ntchito yolemetsa ndipo inu mwatuta phindu la ntchito yawo.”
Ngo nonugv rongo nyingma kolo nonua aam nvdubv vngmuto; kvvbi vdwv hoka nyingdu okv nonuno boksi paayadu.”
39 Asamariya ambiri ochokera mʼmudziwo anakhulupirira Iye chifukwa cha umboni wa mayiyo wakuti, “Iye anandiwuza ine zonse ndinazichita.”
Achialvnv Samaritan nyi vdwv Jisu nyi mvngjwng toku ogulvgavbolo nyimv angv minto, “Ngoogv ogumvnwng riku nama hv ngam minpa toku.”
40 Choncho Asamariya atabwera kwa Iye, anamuwumiriza Iye kuti akhale nawo, ndipo Iye anakhala nawo masiku awiri.
Vkvlvgabv vdwlo Samaritan vdwv hv golo aatokudw bunu ninyia dinchi rungbv minto bunua lvkobv dooming gvdubv, okv Jisu hoka alu lonyi go dootoku.
41 Ndipo chifukwa cha mawu ake, ena ambiri anakhulupirira.
Achialv nyi go ninyia mvngjwng toku ninyigv doin a tvgvrila.
42 Iwo anati kwa mayiyo, “Ife sitikukhulupirira chifukwa cha mawu ako okha, koma tsopano ife tadzimvera tokha, ndipo tikudziwa kuti munthu uyu ndithu ndi Mpulumutsi wa dziko lapansi.”
Okv bunu nyimv anga mintoku, “Ngonu vjak mvngjwng dukunv, noogv minam lokvma, ngonu atuv ninyi gvlo tvvnam lokv okv ngonu chinduku jvjvbv hv nyiamooku gv Ringnvbaanv gorung.”
43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya.
Hoka alu lonyi go dooro kochingbv, Jisu vngraplaku okv Galili bv vngtoku.
44 (Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).
Hv atubongv minsuto, “Nyijwk ka atubogv mooku lo mvngdv madunv.”
45 Iye atafika ku Galileya, Agalileya anamulandira. Iwo anali ataona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pa phwando la Paska, pakuti iwonso anali komweko.
Vdwlo hv Galili lo vngchi tokudw, nyi vdwv ninyia alvrungbv aamu toku, ogulvgavbolo bunu Jerusalem lo vngbo pumja hoka vngtoku okv ho pumja hoka bunu ninyigv rinam mvnwngnga kaatoku.
46 Iye anakafikanso ku Kana wa ku Galileya, kumene anasanduliza madzi kukhala vinyo. Ndipo kumeneko kunali nduna ina ya mfumu imene mwana wake wamwamuna anali chigonere akudwala ku Kaperenawo.
Vbvrikunamv Jisu Galili gv Kana nampum lo vngkur toku, ninyigv isi ha anggor ala bv mvku hoka. Sorkari nyigam go hoka dooto ninyigv kuunyilo ngv Kaparnaum lo lvvma toku.
47 Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.
Vdwlo hv Jisu Judia lokv Galili lo aapv vla tvvpa pvkudw, hv Jisu gvlo aala okv ninyia tvvkato Kaparnaum bv vngla ninyigv kuunyilo sida svngv bv rinv nga mvpu jilabv vla dinchi rungbv minto.
48 Yesu anawawuza iwo kuti, “Anthu inu pokhapokha mutaona zizindikiro zodabwitsa, simudzakhulupirira.”
Jisu ninyia minto, “Nonu, yvvka mvngjwng mare vdwlo nonu kaasartabo okv lamrwpanam go kaama dvdvlo.”
49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”
Nyigam angv mirwkto, “Tamsarnv, nga lvkobv vngming gvcholabv ngoogv kuunyilo ngv sitv madvlo.”
50 Yesu anayankha kuti, “Pita. Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Munthuyo anakhulupirira mawu a Yesu ndipo ananyamuka.
Jisu ninyia minto, “Vngnyila, no gv kuunyilo ngv turriku!” Nyi angv Jisu gv minam a mvngjwngto okv vngtoku.
51 Iye ali pa njira, antchito ake anakumana naye, namuwuza kuti mwana wanu uja wachira.
Ninyigv nampum lamtv hoka ninyigv pakbu vdwv ninyia kaarwksula yunying nga gvjito, “No gv kuunyilo ngv turduku!”
52 Iye atafunsa kuti ndi nthawi yanji imene mwana wake anapeza bwino, iwo anati kwa iye, “Malungo anamusiya iye dzulo pa ora lachisanu ndi chiwiri.”
Hv bunua tvvkato vdwlola ninyigv kuunyilo ngv alvyakunamv, okv bunu mirwkto, “Doonyi hv chaanyala tabv rilo tamiramhv ninyia liu toku.”
53 Ndipo bamboyo anazindikira kuti iyi inali nthawi yomweyo imene Yesu anati kwa iye, “Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Choncho iye ndi onse a pa banja lake anakhulupirira.
Vbvrikunamv abu angv mvngpa toku, ho dw lo Jisu gv ninyia “No gv kuunyilo ngv turriku,” vla mindwbv ritoku. Vkvlvgabv hv la okv ninyigv nyimv kuu vdwv mvngjwng nyatoku.
54 Ichi ndiye chinali chizindikiro chodabwitsa chachiwiri chimene Yesu anachita atafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya.
Judia lokv Galili bv aaro kochingbv si Jisu lvnyi naabv lamrwpadubv rila kaatam namv.