< Yesaya 12 >

1 Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati: “Ndikukuyamikani, Inu Yehova; chifukwa ngakhale munandipsera mtima, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mwanditonthoza.
I A la la, e olelo aku no oe, E hoolea aku au ia oe, e Iehova, No ka mea, i huhu mai oe ia'u mamua, Aka, ua huli aku kou huhu, A ua hoomaha mai oe ia'u.
2 Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga; ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha. Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.”
Aia hoi, o ke Akua ko'u ola, E hoolana wau, aole au e makau; No ka mea, o ka Haku, o IEHOVA ko'u ikaika a me kuu oli, Ua lilo mai ia i ola no'u.
3 Mudzakondwera popeza Yehova ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
E huki no oukou i ka wai me ka olioli, Mailoko mai o na punawai ola.
4 Tsiku limenelo mudzati: “Yamikani Yehova, tamandani dzina lake; mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu, ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
A i kela la, e olelo ana no oukou, E hoolea ia Iehova, E hookaulana i kona inoa, E hoike aku iwaena o na kanaka, i kana mau hana, E hoomanao aku, no ka mea, na hapaiia kona inoa.
5 Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu; zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
E oli aku ia Iehova, no ka mea, na hana oia i na mea nani; He mea ikea keia ma ka honua a pau.
6 Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni; pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”
E hooho aku, e hookani hoi, e ka mea noho ma Ziona, No ka mea, ua mana maloko ou, ka Mea Hemolele o ka Iseraela.

< Yesaya 12 >