< Agalatiya 1 >
1 Paulo mtumwi, osati wosankhidwa ndi anthu kapena kutumidwa ndi munthu ayi, koma Yesu Khristu, ndi Mulungu Atate amene anamuukitsa Yesuyo kwa akufa,
ⲁ̅ⲡⲁⲩⲗⲟⲥ ⲡⲁⲡⲟⲥⲧⲟⲗⲟⲥ ⲡⲉⲃⲟⲗ ϩⲛ ⲣⲱⲙⲉ ⲁⲛ ⲟⲩⲇⲉ ϩⲓⲧⲛ ⲣⲱⲙⲉ ⲁⲛ ⲁⲗⲗⲁ ϩⲓⲧⲛ ⲓⲏⲥ ⲡⲉⲭⲥ ⲙⲛ ⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲡⲉⲓⲱⲧ ⲡⲁⲓ ⲉⲛⲧⲁϥⲧⲟⲩⲛⲟⲥϥ ⲉⲃⲟⲗ ϩⲛ ⲛⲉⲧⲙⲟⲟⲩⲧ
2 pamodzi ndi abale onse amene ali nane, Kulembera mipingo ya ku Galatiya:
ⲃ̅ⲁⲩⲱ ⲛⲉⲥⲛⲏⲩ ⲧⲏⲣⲟⲩ ⲉⲧⲛⲙⲙⲁⲓ ⲉⲛⲥϩⲁⲓ ⲛⲛⲉⲕⲕⲗⲏⲥⲓⲁ ⲛⲧⲅⲁⲗⲁⲧⲓⲁ
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale nanu.
ⲅ̅ⲧⲉⲭⲁⲣⲓⲥ ⲛⲏⲧⲛ ⲙⲛ ϯⲣⲏⲛⲏ ⲉⲃⲟⲗ ϩⲓⲧⲙ ⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲡⲉⲓⲱⲧ ⲙⲛ ⲡⲉⲛϫⲟⲉⲓⲥ ⲓⲏⲥ ⲡⲉⲭⲥ
4 Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
ⲇ̅ⲡⲉⲛⲧⲁϥⲧⲁⲁϥ ϩⲁ ⲛⲉⲛⲛⲟⲃⲉ ϫⲉ ⲉϥⲉⲧⲟⲩϫⲟⲛ ⲉⲡⲉⲓⲁⲓⲱⲛ ⲙⲡⲟⲛⲏⲣⲟⲛ ⲕⲁⲧⲁ ⲡⲟⲩⲱϣ ⲙⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲡⲉⲛⲉⲓⲱⲧ (aiōn )
5 Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
ⲉ̅ⲡⲁⲓ ⲉⲧⲉⲡⲱϥ ⲡⲉ ⲡⲉⲟⲟⲩ ϣⲁ ⲛⲓⲉⲛⲉϩ ⲛⲉⲛⲉϩ ϩⲁⲙⲏⲛ (aiōn )
6 Ine ndikudabwa kuti mukusiya mwamsangamsanga chotere Mulungu amene anakuyitanani mwachisomo cha Khristu ndipo mwatembenuka ndi kutsatira uthenga wina wosiyana,
ⲋ̅ϯⲣϣⲡⲏⲣⲉ ϫⲉ ⲛⲧⲉⲉⲓϩⲉ ϩⲛ ⲟⲩϭⲉⲡⲏ ⲧⲉⲧⲛⲡⲱⲱⲛⲉ ⲛⲧⲙⲡⲉⲛⲧⲁϥⲧⲉϩⲙ ⲧⲏⲩⲧⲛ ϩⲙ ⲡⲉϩⲙⲟⲧ ⲙⲡⲉⲭⲥ ⲓⲏⲥ ⲉⲕⲉⲉⲩⲁⲅⲅⲉⲗⲓⲟⲛ
7 umene si Uthenga Wabwino konse. Pali anthu ena amene akukusokonezani komanso akufuna kupotoza Uthenga Wabwino wa Khristu.
ⲍ̅ⲉⲙⲛⲕⲉⲟⲩⲁ ϣⲟⲟⲡ ⲉⲓⲙⲏⲧⲓ ϫⲉ ⲟⲩⲛ ϩⲟⲓⲛⲉ ⲉⲩϣⲧⲟⲣⲧⲣ ⲙⲙⲱⲧⲛ ⲉⲩⲟⲩⲱϣ ⲉⲡⲉⲛⲉⲡⲉⲩⲁⲅⲅⲉⲗⲓⲟⲛ ⲙⲡⲉⲭⲥ
8 Ngakhale ife kapena mngelo wochokera kumwamba, akalalikira Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene tinakulalikirani uja, iyeyo akhale wotembereredwa!
ⲏ̅ⲁⲗⲗⲁ ⲕⲁⲛ ⲁⲛⲟⲛ ⲏ ⲟⲩⲁⲅⲅⲉⲗⲟⲥ ⲉⲃⲟⲗ ϩⲛ ⲧⲡⲉ ⲛϥⲧⲁϣⲉⲟⲉⲓϣ ⲛⲏⲧⲛ ⲡⲃⲟⲗ ⲙⲡⲉⲛⲧⲁⲛⲧⲁϣⲉⲟⲓϣ ⲙⲙⲟϥ ⲛⲏⲧⲛ ⲙⲁⲣⲉϥϣⲱⲡⲉ ⲉϥⲃⲏⲧ
9 Monga tanena kale, tsopano ndikubwereza kunenanso kuti, “Ngati wina aliyense akulalikirani Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene munawulandira, iyeyo akhale wotembereredwa.”
ⲑ̅ⲛⲑⲉ ⲉⲛⲧⲁⲛϣⲣⲡϫⲟⲟⲥ ⲧⲉⲛⲟⲩ ⲟⲛ ϯϫⲱ ⲙⲙⲟⲥ ϫⲉ ⲡⲉⲧⲛⲁⲧⲁϣⲉⲟⲉⲓϣ ⲛⲏⲧⲛ ⲡⲃⲟⲗ ⲙⲡⲉⲛⲧⲁⲧⲉⲧⲛϫⲓⲧϥ ⲙⲁⲣⲉϥϣⲱⲡⲉ ⲉϥⲃⲏⲧ
10 Kodi tsopano ndikufuna kukopa anthu kuti andivomereze, kapena Mulungu? Kapena ndikufuna kukondweretsa anthu? Ngati ine ndikanakhala kuti ndikufunabe kukondweretsa anthu, sindikanakhala mtumiki wa Khristu.
ⲓ̅ⲧⲉⲛⲟⲩ ⲅⲁⲣ ⲉⲓⲡⲓⲑⲉ ⲛⲛⲣⲱⲙⲉ ϫⲛⲙⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲏ ⲉⲉⲓϣⲓⲛⲉ ⲛⲥⲁⲁⲣⲉⲥⲕⲉ ⲛⲣⲱⲙⲉ ⲉⲛⲉⲉⲓⲁⲣⲉⲥⲕⲉ ϭⲉ ⲟⲛ ⲛⲛⲣⲱⲙⲉ ⲛⲉ ⲁⲛⲅ ⲡϩⲙϩⲁⲗ ⲁⲛ ⲙⲡⲉⲭⲥ
11 Abale, ine ndikufuna kuti mudziwe, kuti Uthenga Wabwino umene ndinalalikira si ochokera kwa munthu ayi.
ⲓ̅ⲁ̅ϯⲧⲁⲙⲟ ⲅⲁⲣ ⲙⲙⲱⲧⲛ ⲛⲉⲥⲛⲏⲩ ⲉⲡⲉⲩⲁⲅⲅⲉⲗⲓⲟⲛ ⲉⲛⲧⲁⲩⲧⲁϣⲉⲟⲉⲓϣ ⲙⲙⲟϥ ⲉⲃⲟⲗ ϩⲓ ⲧⲟⲟⲧ ϫⲉ ⲛⲟⲩⲕⲁⲧⲁ ⲣⲱⲙⲉ ⲁⲛ ⲡⲉ
12 Ine sindinawulandire kuchokera kwa munthu aliyense, kapena kuphunzitsidwa; koma ndinawulandira mwa vumbulutso lochokera kwa Khristu.
ⲓ̅ⲃ̅ⲟⲩⲇⲉ ⲅⲁⲣ ⲁⲛⲟⲕ ⲛⲧⲁⲓϫⲓⲧϥ ⲁⲛ ⲛⲧⲛ ⲣⲱⲙⲉ ⲟⲩⲇⲉ ⲛⲧⲁⲩⲧⲥⲁⲃⲟⲓ ⲁⲛ ⲉⲣⲟϥ ⲁⲗⲗⲁ ϩⲓⲧⲛ ⲟⲩϭⲱⲗⲡ ⲉⲃⲟⲗ ⲛⲧⲉ ⲓⲏⲥ ⲡⲉⲭⲥ
13 Pakuti inu munamva za moyo wanga wakale mʼChiyuda, mmene ndinkazunzira mpingo wa Mulungu koopsa ndi kuyesetsa kuwuwononga.
ⲓ̅ⲅ̅ⲁⲧⲉⲧⲛⲥⲱⲧⲙ ⲅⲁⲣ ⲉⲛⲁϩⲃⲏⲩⲉ ⲙⲡⲓⲟⲩⲟⲉⲓϣ ⲉⲓϩⲛⲧⲙⲛⲧⲓⲟⲩⲇⲁⲓ ϫⲉ ⲛⲉⲉⲓⲇⲓⲱⲕⲉ ⲉⲡⲉϩⲟⲩⲟ ⲡⲉ ⲛⲥⲁ ⲧⲉⲕⲕⲗⲏⲥⲓⲁ ⲙⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲁⲩⲱ ⲛⲉⲉⲓϣⲱϥ ⲙⲙⲟⲥ
14 Ine ndinkapambana Ayuda ambiri a msinkhu wanga pochita za Chiyuda, ndipo ndinali wachangu koposa pa miyambo ya makolo athu.
ⲓ̅ⲇ̅ⲉⲓⲡⲣⲟⲕⲟⲡⲧⲉ ϩⲛ ⲧⲙⲛⲧⲓⲟⲩⲇⲁⲓ ⲉϩⲟⲩⲉ ϩⲁϩ ⲛⲛⲁⲧⲁϭⲟⲧ ϩⲙ ⲡⲁⲅⲉⲛⲟⲥ ⲉⲉⲓⲟ ⲛⲣⲉϥⲕⲱϩ ⲛϩⲟⲩⲟ ⲉⲙⲡⲁⲣⲁⲇⲟⲥⲓⲥ ⲛⲛⲁⲉⲓⲟⲧⲉ
15 Koma Mulungu, amene anandipatula ine ndisanabadwe, ndi kundiyitana mwachisomo chake, atakondweretsedwa
ⲓ̅ⲉ̅ⲛⲧⲉⲣⲉϥⲣϩⲛⲁϥ ⲇⲉ ⲛϭⲓ ⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲡⲁⲓ ⲉⲛⲧⲁϥⲡⲟⲣϫⲧ ⲉⲃⲟⲗ ϫⲓⲛⲉⲉⲓⲛϩⲏⲧⲥ ⲛⲧⲁⲙⲁⲁⲩ ⲁⲩⲱ ⲁϥⲧⲁϩⲙⲉⲧ ⲉⲃⲟⲗ ϩⲓⲧⲙ ⲡⲉϥϩⲙⲟⲧ
16 kuvumbulutsa Mwana wake mwa ine, kuti ndikalalikire Khristuyo pakati pa anthu a mitundu ina, ine sindinapemphe nzeru kwa munthu aliyense.
ⲓ̅ⲋ̅ⲉϭⲗⲡ ⲡⲉϥϣⲏⲣⲉ ⲉⲃⲟⲗ ⲛϩⲏⲧ ϫⲉ ⲉⲓⲉⲧⲁϣⲉⲟⲉⲓϣ ⲙⲙⲟϥ ϩⲛ ⲛϩⲉⲑⲛⲟⲥ ⲛⲧⲉⲩⲛⲟⲩ ⲙⲡⲓⲟⲩⲁϩⲧ ⲉⲥⲁⲣⲝ ϩⲓ ⲥⲛⲟϥ
17 Ine sindinapite ku Yerusalemu kukaonana ndi amene anali atumwi ine ndisanakhale mtumwi. Mʼmalo mwake nthawi yomweyo ndinapita ku Arabiya ndi kubwereranso ku Damasiko.
ⲓ̅ⲍ̅ⲟⲩⲇⲉ ⲙⲡⲓⲃⲱⲕ ⲉⲑⲓⲉⲣⲟⲥⲟⲗⲩⲙⲁ ϣⲁⲛⲁⲡⲟⲥⲧⲟⲗⲟⲥ ⲉⲧϩⲁⲧⲁϩⲏ ⲁⲗⲗⲁ ⲁⲓⲃⲱⲕ ⲉⲧⲁⲣⲁⲃⲓⲁ ⲁⲩⲱ ⲟⲛ ⲁⲓⲕⲧⲟⲓ ⲉⲇⲁⲙⲁⲥⲕⲟⲥ
18 Pambuyo pake, patatha zaka zitatu, ndinapita ku Yerusalemu kukaonana ndi Petro ndikukhala naye masiku khumi ndi asanu.
ⲓ̅ⲏ̅ⲙⲛⲛⲥⲁ ϣⲟⲙⲧⲉ ⲇⲉ ⲛⲣⲟⲙⲡⲉ ⲁⲓⲃⲱⲕ ⲉϩⲣⲁⲓ ⲉⲑⲓⲉⲣⲟⲥⲟⲗⲩⲙⲁ ⲉⲛⲁⲩ ⲉⲕⲏⲫⲁ ⲁⲩⲱ ⲁⲓϭⲱ ϩⲁϩⲧⲏϥ ⲙⲙⲛⲧⲏ ⲛϩⲟⲟⲩ
19 Ine sindinaonane ndi atumwi enawo koma Yakobo yekha, mʼbale wa Ambuye.
ⲓ̅ⲑ̅ⲙⲡⲓⲛⲁⲩ ⲇⲉ ⲉϭⲉ ϩⲛ ⲛⲁⲡⲟⲥⲧⲟⲗⲟⲥ ⲉⲓⲙⲏ ⲓⲁⲕⲱⲃⲟⲥ ⲡⲥⲟⲛ ⲙⲡϫⲟⲉⲓⲥ
20 Ine ndikutsimikizira inu pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberani si zonama ayi.
ⲕ̅ⲛⲉϯⲥϩⲁⲓ ⲇⲉ ⲙⲙⲟⲟⲩ ⲛⲏⲧⲛ ⲉⲓⲥ ϩⲏⲏⲧⲉ ⲙⲡⲉⲙⲧⲟ ⲉⲃⲟⲗ ⲙⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ϫⲉ ⲛϯϫⲓϭⲟⲗ ⲁⲛ
21 Pambuyo pake ndinapita ku Siriya ndi ku Kilikiya.
ⲕ̅ⲁ̅ⲙⲛⲛⲥⲱⲥ ⲁⲓⲉⲓ ⲉϩⲣⲁⲓ ⲉⲛⲓⲕⲗⲓⲙⲁ ⲛⲧⲥⲩⲣⲓⲁ ⲙⲛⲧ ⲕⲓⲗⲓⲕⲓⲁ
22 Koma sindimadziwika ndi nkhope ku mipingo ya ku Yudeya imene ili mwa Khristu.
ⲕ̅ⲃ̅ⲛⲉⲩⲥⲟⲟⲩⲛ ⲇⲉ ⲙⲙⲟⲓ ⲁⲛ ⲡⲉ ⲛϩⲟ ⲛϭⲓ ⲛⲉⲕⲕⲗⲏⲥⲓⲁ ⲛϯⲟⲩⲇⲁⲓⲁ ⲉⲧϩⲙ ⲡⲉⲭⲥ
23 Iwo anangomva mbiri yokha yakuti, “Munthu amene poyamba anatizunza ife, tsopano akulalikira chikhulupiriro chimene iyeyo nthawi ina anafuna kuchiwononga.”
ⲕ̅ⲅ̅ⲙⲟⲛⲟⲛ ⲇⲉ ⲛⲉⲩⲥⲱⲧⲙ ϫⲉ ⲡⲉⲧⲇⲓⲱⲕⲉ ⲙⲙⲟⲛ ⲙⲡⲓⲟⲩⲟⲉⲓϣ ⲧⲉⲛⲟⲩ ϥⲧⲁϣⲉⲟⲉⲓϣ ⲛⲧⲡⲓⲥⲧⲓⲥ ⲉⲛⲉϥϣⲱϥ ⲙⲙⲟⲥ ⲛⲛⲓⲧⲉ
24 Ndipo iwo anayamika Mulungu chifukwa cha ine.
ⲕ̅ⲇ̅ⲁⲩⲱ ⲛⲉⲩϯ ⲉⲟⲟⲩ ⲙⲡⲛⲟⲩⲧⲉ ⲛϩⲏⲧ