< Machitidwe a Atumwi 28 >

1 Titapulumuka choncho, tinamva kuti chilumbacho chimatchedwa Melita.
Tukaisheje ulele kulitaka, gutumumanyi kuti shilambo shitimbililwe mashi shila pushashemwaga Melita.
2 Anthu a pa chilumbacho anatichitira zokoma zimene sizichitika kawirikawiri. Iwo anakoleza moto natilandira tonse chifukwa kumagwa mvula ndipo kumazizira.
Bhashilambo bha kweneko gubhatutendelenje mituka ja kaje. Pabha ula jatendeganya na twashinkukola mmbepo, gubhakumbenyenje moto gubhatushemelenje tubhowe.
3 Paulo anatola mtolo wankhuni, pamene amayika pa moto, munatulukamo njoka chifukwa cha kutentha, ndipo inamuluma pa dzanja.
A Pauli gubhalokwete neng'ene nshigo gumo gubhakwiile pamoto. Bhai, penepo kwa ligongo lya lyoto lya moto gula gwakopweshe lijoka jwa luma nneng'ene mula akwaanyembelaga a Pauli munkono.
4 Anthu a pa chilumbacho ataona njokayo ili lende pa dzanja lake, iwo anawuzana kuti, “Munthu uyu akuyenera kukhala munthu wopha anthu; pakuti ngakhale wapulumuka pa nyanja, chilungamo sichinamulore kuti akhale ndi moyo.”
Bhashilambo bha pepala bhakabhonanjeje lijoka alikwaakwela a Pauli, gubhabhalanjilenenje, “Ipingaga aju munduju ashibhulaga mundu nkali alamile gwangali kuwa mmashi, nnungu jwetu jwankongwe ashemwa Aki akanneka alame!”
5 Koma Paulo anayikutumulira pa moto njokayo, ndipo sanamve kupweteka.
Ikabheje a Pauli gubhampukunyishiye pamoto lijoka jwa luma jula na wala jwangaaluma nkali kashoko.
6 Anthu anayembekezera kuti thupi lake litupa kapena agwa ndi kufa mwadzidzidzi, koma anadikira nthawi yayitali. Ataona kuti palibe kanthu kachilendo kanamuchitikira anasintha maganizo awo nanena kuti iye ndi mulungu.
Bhandunji bhala gubhalinginji nkulolela kuti nkono gula shiguimbe eu a Pauli shibhagwe niwa popo. Bhakalolelanjeje paakabha nibhona wala shakwapi shikwakoposhela a Pauli, gubhatindigenyenje ng'aniyo yabhonji gubhashitenje kuti, jweneju nnungu.
7 Pafupi ndi malowa panali munda wa Popliyo, mkulu wa boma la pa chilumbacho. Iye anatilandira natisamala bwino masiku atatu.
Tome na pepala jashinkupagwa migunda ja bhakulungwa bha shene shilambo shatimbililwe na mashisho lina lyabho pubhashemwaga a Pabhuliashi. Gubhatushemile kunngwabho kwa ntima gwa umbwiga, gututemi ujeni mobha gatatu.
8 Abambo ake anali gone, chifukwa amadwala malungo ndi kamwazi. Paulo analowa mʼchipinda chake kukawaona, ndipo atapemphera, anasanjika manja ake pa iwo nawachiritsa.
Ainabhabho a Pabhuliashi bhashinkusheluka na guluma, bhali bhagonile pa shinanda. A Pauli gubhapite kwalola na gubhajujile Nnungu, gubhaabhishile makono gubhaalamiye.
9 Zitachitika zimenezi, anthu onse odwala a pa chilumbacho anabwera ndipo anachiritsidwa.
Gakatendesheje genego, bhalwelenji bhowe nnepeila pa shilambo pala gubhaaishilenje a Pauli na gubhalamiywenje.
10 Anthuwo anatilemekeza ife mʼnjira zambiri ndipo pamene tinakonzeka kuti tiyambe ulendo, anatipatsa zonse zomwe tinazisowa.
Nabhalabhonji gubhatujogopenje kwa kaje, tukapanganisheje kujabhula, gubhapashilenje indu yaigwinji itwaipinjile.
11 Patapita miyezi itatu, tinanyamuka pa sitima ina imene inakhala pa chilumbacho chifukwa cha kuzizira. Inali sitima ya ku Alekisandriya imene inali ndi chizindikiro cha milungu ya mapasa yotchedwa Kastro ndi Polikisi.
Jikapiteje myei jitatu gututandwibhe mwanja gwetu na meli jimo ja ku Alekishandilia jishemwa, “Ashinnungu bha Mmba.” Pujaliji kweneko miongwe jowe ja shipwepwe.
12 Tinakafika ku Surakusa ndipo kumeneko tinakhalako masiku atatu.
Gutuishe shilambo sha ku Shilakusha gututemi mobha gatatu.
13 Kuchokera kumeneko tinayenda ndi kukafika ku Regio. Mmawa mwake mphepo yochokera kummwera inawomba, ndipo tsiku linalo tinakafika ku Potiyolo.
Tukajabhuleje penepo gututimbilile gutuishe ku Legio. Likapiteje lyubha limo, mbungo ja kushi jikutandubhaga kupuga na gakapiteje mobha gatatu gutuishe kubhandali ja Potioli.
14 Kumeneko tinapezako abale amene anatiyitana kuti tikhale nawo sabata limodzi. Ndipo kenaka tinapita ku Roma.
Kweneko gutwaimenenje bhakilishitu ajetunji gubhatujujilenje tutame nabhonji juma jimo. Gutuishe ku Loma shana nneyo.
15 Abale kumeneko atamva kuti tikubwera, anabwera kudzakumana nafe mpaka ku bwalo la Apiyo ndiponso ku nyumba za alendo zitatu. Atawaona anthu amenewa Paulo anayamika Mulungu ndipo analimbikitsidwa.
Bhakilishitu ajetunji bha ku Loma bhakapilikananjeje kuti tushiika, gubhaikengenenje kukutuposhela kumbwani ja Apio na Kunyumba Itatu ya Bhajeninji. A Pauli bhakaabhonanjeje gubhatendile eja kwa a Nnungu, gubhatagwilwe ntima.
16 Titafika ku Roma, Paulo analoledwa kukhala pa yekha ndi msilikali womulondera.
Tukaisheje ku Loma a Pauli gubhaleshelelwe kutama kujika muulinda uka linjola jumo.
17 Patapita masiku atatu, Paulo anasonkhanitsa pamodzi atsogoleri a Ayuda. Atasonkhana, Paulo anawawuza kuti, “Abale anga, ngakhale kuti ine sindinachite kanthu kalikonse kulakwira mtundu wathu kapena miyambo ya makolo athu, koma anandigwira mu Yerusalemu ndi kundipereka mʼmanja mwa Aroma.
Gakapiteje mobha gatatu a Pauli gubhaashemilenje ashikalongolele bha Shiyaudi bha shene shilambosho. Bhakaimananjeje gubhaabhalanjilenje, “Ashapwanga, shakwa shindendile na wala tauka ikubho ya ashinakulubhetu, nashinkukamulwa ku Yelushalemu kula na kamuywa mmakono ga Bhaloma.
18 Iwo anandifufuza ndipo anafuna kundimasula chifukwa sanandipeze wopalamula mlandu woyenera kuphedwa.
Bhakamuyanjeje nibhona kuti shakwa shinebhile, gubhapinjilenje kung'opola bhanekanje.
19 Koma Ayuda atakana, ine ndinakakamizidwa kupempha kuti ndikaonekere pamaso pa Kaisara, sikuti ndinali ndi kanthu konenezera mtundu wanga.
Ikabheje Bhayaudi bhananji gubhakanilenje, gunyujile malobhe gangu gakamaliywe na bhakulungwa bha ku Loma a Kaishali, nkali ngakweteje malobhe gogowe ga kwaalugulanga bhashilambo ajangunji.
20 Pa chifukwa ichi ndapempha kuti ndionane nanu ndi kuyankhula nanu. Pakuti nʼchifukwa cha chiyembekezo cha Israeli ndamangidwa unyolo uwu.”
Bhai, kwa ligongo lya genego, njikunshemanga kunnolanje na tukungulushe, pabha njitabhwa ajino mindololo jino ligongo lya malagano ga a Nnungu ku bha Ishilaeli gala.”
21 Iwo anayankha kuti, “Ife sitinalandire kalata iliyonse yochokera ku Yudeya yonena za iwe, ndipo palibe mmodzi wa abale amene anachokera kumeneko anafotokoza kapena kunena kalikonse koyipa ka iwe.
Bhalabhonji gubhaalugulilenje, “Uwe tukanabhe poshela ntenga eu bhaluwa ja ngani jenu kopoka ku Yudea, wala jwakwa nkilishitu jojowe aishe apano kutubhalanjila lilobhe lyolyowe linnebhile mmwe.
22 Koma ife tikufuna kumva maganizo ako ndi otani, pakuti tikudziwa kuti ponseponse anthu akuyankhula zotsutsana ndi mpatuko umenewu.”
Ikabheje tunapinga tupilikane shinkuganishiya mmwe, pabha uwe tumumanyi kuti mmbali yowe gwene nkumbigo unalugulwa mwangali mwambone.”
23 Iwo anakonza tsiku lina loti akumane ndi Paulo, ndipo anabwera anthu ambiri ku nyumba kumene amakhala. Kuyambira mmawa mpaka madzulo, Paulo anawafotokozera ndi kuwawuza za ufumu wa Mulungu ndipo anayesa kuwakopa kuti akhulupirire Yesu kuchokera mʼMalamulo a Mose ndiponso mʼmabuku a Aneneri.
Bhakalagananjeje lyubha lya imana, gubhaikengenenje bhandunji bhabhagwinji nnyumba jibhatamaga. Tandubhila lyamba mpaka ligulo a Pauli gubhaatalashiyenje ga Ukulungwa gwa a Nnungu, bhalilinga kwaatendanga bhakundanje ngani ja a Yeshu kwa talashiya shalia ja a Musha na ashinkulondola bha a Nnungu.
24 Ena anakopeka ndi zimene Paulo ananena, koma enanso sanakhulupirire.
Bhananji gubhakundilenje malobhe gala, ikabheje bhananji bhangakulupalilanga.
25 Ndipo anayamba kuchoka popeza sanagwirizane pakati pawo Paulo atanena mawu awa omaliza akuti, “Mzimu Woyera anayankhula zoona za makolo anu pamene Iye ananena kudzera mwa Mneneri Yesaya kuti,
Bhai, gubhajabhulengene akuno bhali bhalekenenje ng'aniyo ga malobhe ga a Pauli ga kuti, mbena Mbumu jwa Ukonjelo abhelekete mwa mmbone na ashinakulubhenunji kwa kang'wa ja ankulondola bha a Nnungu a Ishaya,
26 “Pita kwa anthu awa ndi kuwawuza kuti, ‘Kumva mudzamva, koma osamvetsetsa; kupenya mudzapenya, koma osaona kanthu.’
bhalinkuti, “‘Jenda kubhandunjibha ukaabhalanjilanje. Kupilikana shimpilkananje, ikabheje nkamumanyanga, Kulola shinnolanje, ikabheje nkaibhonanga.
27 Pakuti mtima wa anthu ndi wokanika; mʼmakutu mwawo ndi mogontha, ndipo atsinzina kuti asaone kanthu. Mwina angapenye ndi maso awo, angamve ndi makutu awo, angamvetse ndi nzeru zawo ndi kutembenuka, Ineyo nʼkuwachiritsa.
Pabha mitima ja bhene bhandunjibha jishitopa, bhashiibhanga makutu gabhonji meyo gabhonji bhashikupilanga. Gwangali nneyo, bhakalolilenje na meyo gabhonji, bhakapilikenenje na makutu gabhonji. Bhakaelewenje mmitima jabhonji, bhakaandendebhushilenje, bhashite Bhakulungwa, ngaalamiyenje.’”
28 “Chifukwa chake ine ndikufuna mudziwe kuti chipulumutso cha Mulungu chatumizidwa kwa anthu a mitundu ina, ndipo iwo adzamvera.”
Kungai a Pauli gubhashite, “Bhai, mmumanyanje kuti ntenga gwa a Nnungu gwa ngani ja ntapulo upelekwe ku bhandu bha ilambo ina. Bhalabhonji shibhapilikanilanje!”
29 Paulo atanena mawu amenewa, Ayuda aja anachoka akutsutsana kwambiri.
Bhakabheleketeje genego, Bhayaudi gubhajabhulenje, bhalipita taukangana ashaayenenji.
30 Paulo anakhala kumeneko zaka ziwiri zathunthu mʼnyumba yobwereka yomwe amalipira ndipo ankalandira aliyense amene amabwera kudzamuona.
A Pauli gubhatemi ku Loma yaka ibhili nnyumba jibhapoleshe bhayene kwalipila mbiya, bhatendaga kwaposhelelanga bhowe bhaowelangaga.
31 Molimba mtima ndi popanda womuletsa, Paulo analalikira za ufumu wa Mulungu ndi kuphunzitsa za Ambuye Yesu Khristu.
Bhatenda lunguya ga Ukulungwa gwa a Nnungu na jiganya ngani ja Bhakulungwa a Yeshu Kilishitu gwangali bhoga na jwakwa mundu abhalimbiyaga.

< Machitidwe a Atumwi 28 >