< 2 Timoteyo 3 >
1 Koma dziwa izi: Mʼmasiku otsiriza kudzafika nthawi zoopsa kwambiri.
Ama yinno ilenge imone: kubi nimalin ayiri nijasi mayitu.
2 Anthu adzakhala odzikonda, okonda ndalama, odzitama, onyada, achipongwe, osamvera makolo awo, osayamika, wopanda chiyero.
Bara anit yitu anan suu natimine, anan suu nikurfun, anan fonigiri, ufiu nati, anan liru Kutelle nanzang, anan salin lanzun liru narika na ina maru nani, na ima yitu nin godo ba, nin dirun lau.
3 Adzakhala wopanda chikondi, osakhululuka, osinjirira, osadziletsa, ankhanza, osakonda zabwino,
Ima yitu sa unlazung kunekune, anan salin shauzu nin nalapi, anan nanzu tissa, na idinnin minu nati ulau ba, anan nun, na idinin suu nimon icine ba.
4 opereka anzawo kwa adani awo, osaopa zoyipa, odzitukumula, okonda zowasangalatsa mʼmalo mokonda Mulungu.
Ima yitu anan lessu nati, anan gbas, anan lanzu nin nati, anan suun lanzun mang ubun nin suu Kutelle.
5 Adzakhala ndi maonekedwe achipembedzo koma mphamvu yake ndi kumayikana. Anthu amenewa uziwapewa.
Ima yitu nin kulap Kutelle, ama ima nari likara nnin. Kpila usun anit alele.
6 Iwowa ndi anthu aja amene amayendayenda mʼmakomo a anthu nʼkumanyenga akazi ofowoka mʼmaganizo, olemedwa ndi machimo ndiponso otengeka ndi zilakolako zoyipa zamitundumitundu,
Bara among mine anitari na asa ipira nanya kilari iwunno awani alala. Alengene awaniari ale na ikulun nanya nalapi inin din wunu nani nin vat nimon nsuu nibinayi mine.
7 amaphunzira nthawi zonse koma samatha kuzindikira choonadi.
Ale awane kolo liri idin pizurun yinnu, ama na isa yinno udak kitin yinnu kidegene ba.
8 Monga momwe Yanesi ndi Yambere anawukira Mose, momwemonso anthu amenewa amawukira choonadi. Nzeru zawo ndi zowonongeka ndipo pa za chikhulupiriro, ndi okanidwa.
Libau lirume na Jannis ni Jambiris wa yissin nivira ni Musa. Libau lole tutung ale anan dursuzu kinu kane yissin nivira nin kidegen. Inung anitari nan imal kuzu nibinai, na iyinna ninghinu ba kusarin yinnu sa uyenu.
9 Koma sadzapita nazo patali kwambiri zimenezi, pakuti anthu onse adzaona kupusa kwawo monga anachitira Yanesi ndi Yambere.
Ama na iba du piit ba. Bara tilalan mine mayitu kanang kiti kogha, nafo una naleli anite.
10 Tsono iwe, umadziwa zonse zimene ndimaphunzitsa, makhalidwe anga, cholinga changa, chikhulupiriro changa, kuleza mtima kwanga, chikondi changa, ndi kupirira kwanga,
Ama kitife, una dortu udusuzu ning, adu, ukpilizu, uyinnu sa uyenu, uteru nayi ning, usuu, lissosin ncaa,
11 mazunzo anga, masautso anga, monga zinandichitikira ku Antiokeya, ku Ikoniya ndi ku Lusitra. Ndinazunzika kwambiri. Koma Ambuye anandipulumutsa pa zonsezi.
utizin niu ning, uniu, nin nimon ile na iwa sei in Antiyok, in Ikoniyom, a in Listra. Nna teru kibinayi nin tizun niu. Nanya nani vat, Cikilare wa nutuni ucine.
12 Kunena zoona, munthu aliyense amene akufuna kukhala moyo wolemekeza Mulungu mwa Khristu Yesu, adzazunzikadi,
Vat nalenge na idi ninsuu iso lissosin Kutelle ima tizu nani iniu.
13 pomwe anthu oyipa ndi onyenga adzanka nayipirayipira, kunamiza ena, iwo nʼkumanamizidwanso.
Anitin magunta nin nanan tizu nafo among ina rusuzo anit ba su kang. Ima wultunu among. Inung wang ina wultung naneri.
14 Koma iwe pitiriza zimene waziphunzira ndi kuzivomereza, chifukwa ukudziwa amene anakuphunzitsa zimenezi.
Ama bari fe, soo nanya nimong ilenge na una massu nin nile na umal yinnu mung. Uyiru kitin lenge na una massu ku.
15 Kuyambira uli wamngʼono wakhala ukudziwa Malemba Oyera, amene akhoza kukupatsa nzeru zokupulumutsa kudzera mʼchikhulupiriro cha mwa Yesu Khristu.
Uyiru nwo tun tinono una yinnin iyert ilau. Ilengene wasa itafi jijin bara utucufe nanyan yinnu sa uyenu in Kristi Yesu.
16 Malemba onse anawalembetsa ndi Mulungu, ndipo othandiza pophunzitsa, podzudzula, pokonza cholakwika ndi polangiza za chilungamo
Vat ulirun tucu Kutelleri na kyele unin. Ucau bara ukye libau lissosin, bara uyinnu nkpiliu, bara kyelu ntanu, nin dursuzu lidu lilau.
17 kuti munthu wa Mulungu akonzekere bwino lomwe kugwira ntchito iliyonse yabwino.
Udi nene bara unit Kutelle nan yita ning yirru, uceu nimon katwa kacine kibanayi.