< 2 Yohane 1 >

1 Ndine mkulu wampingo, kulembera: Mayi wosankhidwa ndi Mulungu ndi kwa ana ake amene ndimawakonda mʼchoonadi. Ndipo sindine ndekha amene ndimawakonda, komanso onse odziwa choonadi.
Jene bhaluwa jino kujikopoka kwangu nne nkulungwa jwa likanisha. Ngunakunnjandishila mmanganya bhandunji bha likanisha, bhungumpinganga mpaka muntima. Nngabha nne jikape ngumpinganga, ikabheje nneila peila na bhowe bhakujimanyanga kweli, bhanakumpinganga.
2 Timakukondani chifukwa cha choonadi chimene chimakhala mwa ife ndipo chidzakhala mwa ife mpaka muyaya. (aiōn g165)
Pabha jene kweliji jinatama nkati jetu, na shijilonjeye tama na uwe pitipiti. (aiōn g165)
3 Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi kwa Yesu Khristu, Mwana wa Atate, zikhale ndi ife mʼchoonadi ndi mʼchikondi.
Atati a Nnungu pamo na a Yeshu Kilishitu bhana bhabho, bhanakutupa nema na shiya na ulele, bhene bhatama nkweli na pingana bhala.
4 Ndinakondwera kwambiri nditapeza ana anu ena akuyenda mʼchoonadi, monga Atate anatilamulira.
Njiangalala kwa kaje kubhona kuti bhananji munkumbi gwa ashibhana bhenu, bhanatamangananga nkweli malinga Atati shibhashite kutuamulisha.
5 Ndipo tsopano, amayi wokondedwa, sindikukulemberani lamulo latsopano koma lomwe lija takhala nalo kuyambira pachiyambi. Ine ndikukupemphani kuti tidzikondana wina ndi mnzake.
Na nnaino a mama ngunakunshondelesheya, nngabha kuti ngunakunnjandishila amuli ja ambi, ikabheje ni amuli jituposhele kuumila ku ndandubho, tupingane.
6 Ndipo chikondi ndiye kuyenda momvera malamulo ake. Lamulo lake ndi lakuti mukhale moyo wachikondi monga munamva kuyambira pachiyambi.
Na kupingana ni kutama nkukagulila amuli ya a Nnungu. Jeneji ni amuli jinnjipilikenenje kuumila ku ndandubho, ntamangane nkupingana.
7 Ndikunena zimenezi chifukwa anthu ambiri onyenga, amene savomereza kuti Yesu Khristu anabwera monga munthu, akuyenda mʼdziko lapansi. Munthu aliyense otere ndi wonyenga ndiponso wokana Khristu.
Bhaunaminji bhabhagwinji bhakaakundanga kuti a Yeshu Kilishitu bhaaishe bhali na shiilu shabho, bhakoposhelenje pa shilambolyo. Mundu jwa nneyo analambila na akakwaakunda a Kilishitu.
8 Chenjerani kuti mungataye chimene mwagwirira ntchito, koma chitani khama kuti mukalandire mphotho yanu yonse.
Mwiiteiganje nnaobhianga shene shintendelenje maengo shila, ikabhe mpatanje upo itimilile.
9 Aliyense amene sasunga chiphunzitso cha Khristu, alibe Mulungu. Koma amene amasunga chiphunzitsochi, ameneyo alinso ndi Atate ndi Mwana.
Mundu jojowe akaatama mmajiganyo ga a Kilishitu, jwenejo jwangali a Nnungu. Na jojowe akalonjeya mmajiganyo ga a Kilishitu na kugaleka, jwenejo jwangali a Nnungu. Jojowe atama mmajiganyo, akwete Atati na Mwana nneila peila.
10 Ngati wina aliyense abwera kwa inu osaphunzitsa zimenezi, musamulandire mʼnyumba mwanu kapena kumupatsa moni.
Nnamposhelanje mundu jojowe akunjiilanga gwangali kumpeleshelanga gene majiganyo gano, numbe nnaposhelanje mmajumba genunji.
11 Aliyense wolandira munthu wotere ndiye kuti akuvomerezana nazo ntchito zake zoyipa.
Jojowe akumposhela mundu jwa nneyo, na jwalakwe anakwiilunda mwiitendi yangali ya mmbone.
12 Ndili nazo zambiri zoti ndikulembereni, koma sindikufuna kuzilemba mʼkalata. Mʼmalo mwake, ndikuyembekeza kufika kwanuko kuti tidzakambirane nanu pamaso ndi pamaso, potero chimwemwe chathu chidzakhala chathunthu.
Ngwete indu yaigwinji, ikabhe ngaapinga kunnjandishilanga kwa kalatashi na wino, ikabheje kuengwa kwangu ninng'owelanje kutukungulushe pamo na mmanganya tulibhonegana, nkupinga kuangalala kwetu kutimilile.
13 Ana a mlongo wanu wosankhidwa ndi Mulungu akupereka moni.
Bhana bha alumbu bhenu bhaagwilwe na a Nnungu, bhanakunnamushilanga.

< 2 Yohane 1 >